Font Size
Readings for Celebrating Advent
Scripture passages that focus on the meaning of Advent and Christmas.
Duration: 35 days
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (CCL)
Genesis 3:14-15
14 Choncho Yehova Mulungu anati kwa njokayo, “Popeza wachita zimenezi,
“Ndiwe wotembereredwa kuposa ziweto zonse
ndi nyama zakuthengo zonse.
Udzayenda chafufumimba
ndipo udzadya fumbi
masiku onse a moyo wako.
15 Ndipo ndidzayika chidani
pakati pa iwe ndi mkaziyo,
pakati pa mbewu yako ndi mbewu yake;
Iye adzaphwanya mutu wako
ndipo iwe udzaluma chidendene chake.”
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (CCL)
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.