Add parallel Print Page Options

Tsiku la Ambuye

Tsono abale, za nthawi ndi nyengo yake nʼkosafunikira kuti tikulembereni, chifukwa mukudziwa bwino lomwe kuti tsiku la Ambuye lidzafika ngati mbala usiku. Pamene anthu akunena kuti, “Mtendere ndi chitetezo,” chiwonongeko chidzafika pa iwo mwadzidzidzi, monga zowawa za amayi pobereka, ndipo sadzathawa.

Koma inu abale, simuli mu mdima kuti tsiku limeneli lidzakudzidzimutseni ngati mbala. Nonse ndinu ana a kuwunika ndi ana a usana. Sindife anthu a usiku kapena mdima. Chomwecho tsono, tisafanane ndi ena amene akugona koma tikhale maso ndi odzisunga. Pakuti amene akugona, amagona usiku, ndi amene amaledzera, amaledzera usiku. Koma popeza ndife a usana, tikhale odzisunga, titavala chikhulupiriro ndi chikondi ngati chovala pachifuwa, ndi chiyembekezo cha chipulumutso ngati chipewa. Pakuti Mulungu sanatisankhe kuti tikavutike ndi mkwiyo koma kuti tilandire chipulumutso kudzera mwa Ambuye athu Yesu Khristu. 10 Iye anatifera ndi cholinga chakuti, kaya tili ndi moyo kapena tagona, tikhale naye pamodzi. 11 Choncho limbikitsanani wina ndi mnzake ndi kuthandizana kukula mu mzimu, monga momwe mukuchitira.

Malangizo Otsiriza

12 Tsopano tikukupemphani abale kuti muziwalemekeza amene akugwira ntchito pakati panu, amene amakuyangʼanirani mwa Ambuye ndi amene amakulimbikitsani. 13 Muziwachitira ulemu kwambiri mwachikondi chifukwa cha ntchito yawo. Mukhale pa mtendere wina ndi mnzake. 14 Ndipo tikukupemphani abale, muwachenjeze amene akungokhala osagwira ntchito, alimbikitseni amanyazi, thandizani ofowoka ndipo muzilezera mtima aliyense. 15 Onetsetsani kuti wina asabwezere choyipa kwa omuchitira choyipa koma nthawi zonse yesetsani kukhala okoma mtima kwa wina ndi mnzake; ndiponso ndi kwa anthu ena onse.

16 Kondwerani nthawi zonse. 17 Pempherani kosalekeza. 18 Yamikani mu zonse, pakuti ichi ndi chifuniro cha Mulungu kwa inu mwa Khristu Yesu.

19 Musazimitse moto wa Mzimu Woyera. 20 Musanyoze mawu a uneneri. 21 Yesani zinthu zonse. Gwiritsitsani chimene ndi chabwino. 22 Mupewe choyipa cha mtundu wina uliwonse.

23 Mulungu mwini, Mulungu wamtendere, akuyeretseni kotheratu. Mzimu wanu wonse, moyo ndi thupi zisungidwe zopanda cholakwa mpaka kubwera kwa Ambuye athu Yesu Khristu. 24 Amene anakuyitanani ndi wokhulupirika ndipo Iye adzachita zimenezi.

25 Abale, mutipempherere. 26 Perekani moni wachikondi kwa onse. 27 Pamaso pa Ambuye ndikulamula kuti kalatayi iwerengedwe kwa abale onse.

28 Chisomo cha Ambuye athu Yesu Khristu chikhale nanu.

The Day of the Lord

Now, brothers and sisters, about times and dates(A) we do not need to write to you,(B) for you know very well that the day of the Lord(C) will come like a thief in the night.(D) While people are saying, “Peace and safety,”(E) destruction will come on them suddenly,(F) as labor pains on a pregnant woman, and they will not escape.(G)

But you, brothers and sisters, are not in darkness(H) so that this day should surprise you like a thief.(I) You are all children of the light(J) and children of the day. We do not belong to the night or to the darkness. So then, let us not be like others, who are asleep,(K) but let us be awake(L) and sober.(M) For those who sleep, sleep at night, and those who get drunk, get drunk at night.(N) But since we belong to the day,(O) let us be sober, putting on faith and love as a breastplate,(P) and the hope of salvation(Q) as a helmet.(R) For God did not appoint us to suffer wrath(S) but to receive salvation through our Lord Jesus Christ.(T) 10 He died for us so that, whether we are awake or asleep, we may live together with him.(U) 11 Therefore encourage one another(V) and build each other up,(W) just as in fact you are doing.

Final Instructions

12 Now we ask you, brothers and sisters, to acknowledge those who work hard(X) among you, who care for you in the Lord(Y) and who admonish you. 13 Hold them in the highest regard in love because of their work. Live in peace with each other.(Z) 14 And we urge you, brothers and sisters, warn those who are idle(AA) and disruptive, encourage the disheartened, help the weak,(AB) be patient with everyone. 15 Make sure that nobody pays back wrong for wrong,(AC) but always strive to do what is good for each other(AD) and for everyone else.

16 Rejoice always,(AE) 17 pray continually,(AF) 18 give thanks in all circumstances;(AG) for this is God’s will for you in Christ Jesus.

19 Do not quench the Spirit.(AH) 20 Do not treat prophecies(AI) with contempt 21 but test them all;(AJ) hold on to what is good,(AK) 22 reject every kind of evil.

23 May God himself, the God of peace,(AL) sanctify you through and through. May your whole spirit, soul(AM) and body be kept blameless(AN) at the coming of our Lord Jesus Christ.(AO) 24 The one who calls(AP) you is faithful,(AQ) and he will do it.(AR)

25 Brothers and sisters, pray for us.(AS) 26 Greet all God’s people with a holy kiss.(AT) 27 I charge you before the Lord to have this letter read to all the brothers and sisters.(AU)

28 The grace of our Lord Jesus Christ be with you.(AV)

But of the times and the seasons, brethren, ye have no need that I write unto you.

For yourselves know perfectly that the day of the Lord so cometh as a thief in the night.

For when they shall say, Peace and safety; then sudden destruction cometh upon them, as travail upon a woman with child; and they shall not escape.

But ye, brethren, are not in darkness, that that day should overtake you as a thief.

Ye are all the children of light, and the children of the day: we are not of the night, nor of darkness.

Therefore let us not sleep, as do others; but let us watch and be sober.

For they that sleep sleep in the night; and they that be drunken are drunken in the night.

But let us, who are of the day, be sober, putting on the breastplate of faith and love; and for an helmet, the hope of salvation.

For God hath not appointed us to wrath, but to obtain salvation by our Lord Jesus Christ,

10 Who died for us, that, whether we wake or sleep, we should live together with him.

11 Wherefore comfort yourselves together, and edify one another, even as also ye do.

12 And we beseech you, brethren, to know them which labour among you, and are over you in the Lord, and admonish you;

13 And to esteem them very highly in love for their work's sake. And be at peace among yourselves.

14 Now we exhort you, brethren, warn them that are unruly, comfort the feebleminded, support the weak, be patient toward all men.

15 See that none render evil for evil unto any man; but ever follow that which is good, both among yourselves, and to all men.

16 Rejoice evermore.

17 Pray without ceasing.

18 In every thing give thanks: for this is the will of God in Christ Jesus concerning you.

19 Quench not the Spirit.

20 Despise not prophesyings.

21 Prove all things; hold fast that which is good.

22 Abstain from all appearance of evil.

23 And the very God of peace sanctify you wholly; and I pray God your whole spirit and soul and body be preserved blameless unto the coming of our Lord Jesus Christ.

24 Faithful is he that calleth you, who also will do it.

25 Brethren, pray for us.

26 Greet all the brethren with an holy kiss.

27 I charge you by the Lord that this epistle be read unto all the holy brethren.

28 The grace of our Lord Jesus Christ be with you. Amen.