Add parallel Print Page Options

Yesu Ayesedwa Mʼchipululu

Pambuyo pake Yesu anatsogozedwa ndi Mzimu Woyera kupita ku chipululu kukayesedwa ndi mdierekezi. Ndipo atasala kudya masiku makumi anayi usana ndi usiku, anamva njala. Woyesayo anadza kwa Iye nati, “Ngati ndinu mwana wa Mulungu, sandutsani miyala iyi kuti ikhale buledi.”

Yesu anayankha kuti, “Zalembedwa, ‘Munthu sadzakhala ndi moyo ndi chakudya chokha, koma ndi mawu aliwonse ochokera mʼkamwa mwa Mulungu.’ ”

Pamenepo mdierekezi anapita naye ku mzinda woyera namuyimiritsa pamwamba penipeni pa Nyumba ya Mulungu. Ndipo anati, “Ngati ndinu Mwana wa Mulungu, dziponyeni nokha pansi. Pakuti kwalembedwa:

“ ‘Adzalamulira angelo ake za iwe,
    ndipo adzakunyamula ndi manja awo
    kuti phazi lako lisagunde pa mwala.’ ”

Yesu anamuyankha kuti, “Kwalembedwanso: ‘Musamuyese Yehova Mulungu wanu.’ ”

Kenaka mdierekezi anamutengera Yesu ku phiri lalitali kwambiri namuonetsa maufumu onse a dziko lapansi ndi ulemerero wawo. Ndipo anati kwa Iye, “Zonsezi ndidzakupatsani ngati mutandiweramira ndi kundipembedza ine.”

10 Yesu anati kwa iye, “Choka Satana! Zalembedwa, ‘Pembedza Yehova Mulungu wako ndi kumutumikira Iye yekha.’ ”

11 Pamenepo mdierekezi anamusiya ndipo angelo anamutumikira Iye.

Yesu Ayamba Kulalikira

12 Yesu atamva kuti Yohane anamutsekera mʼndende, anabwerera ku Galileya. 13 Ndipo atachoka ku Nazareti anapita ku Kaperenawo ndi kukhala mʼmbali mwa nyanja, mʼdera la Zebuloni ndi Nafutali; 14 pokwaniritsa zimene zinanenedwa kudzera mwa mneneri Yesaya kuti,

15 “Dziko la Zebuloni ndi dziko la Nafutali,
    njira ya ku nyanja, kutsidya lija la Yorodani,
    Galileya wa anthu a mitundu ina,
16 anthu okhala mu mdima
    awona kuwala kwakukulu;
ndi kwa iwo okhala mʼdziko la mthunzi wa imfa
    kuwunika kwawafikira.”

17 Kuyambira nthawi imeneyo, Yesu anayamba kulalikira nati, “Tembenukani mtima ufumu wakumwamba wayandikira.”

Yesu Ayitana Ophunzira ake Oyamba

18 Pamene Yesu ankayenda mʼmbali mwa nyanja ya Galileya, anaona abale awiri, Simoni wotchedwa Petro ndi mʼbale wake Andreya akuponya khoka mʼnyanja popeza anali asodzi. 19 Yesu anati, “Bwerani, tsateni Ine ndipo ndidzakusandutsani asodzi a anthu.” 20 Nthawi yomweyo anasiya makoka awo namutsata Iye.

21 Atapita patsogolo, anaona abale ena awiri, Yakobo ndi mʼbale wake Yohane ana a Zebedayo. Iwowa anali mʼbwato ndi abambo awo, Zebedayo, akukonza makoka awo ndipo Yesu anawayitana. 22 Nthawi yomweyo anasiya bwato ndi abambo awo namutsata Iye.

Yesu Achiritsa Odwala

23 Yesu anayendayenda mu Galileya kuphunzitsa mʼmasunagoge awo, nalalikira Uthenga Wabwino wa ufumu ndi kuchiritsa matenda onse pakati pa anthu. 24 Mbiri yake yonse inawanda ku Siriya konse ndipo anthu anabweretsa kwa Iye onse amene anali odwala nthenda zosiyanasiyana, womva maululu aakulu, ogwidwa ndi ziwanda, odwala matenda akugwa ndi olumala ndipo Iye anawachiritsa. 25 Magulu ambiri a anthu anachokera ku Galileya, Dekapoli, Yerusalemu, Yudeya ndi ku madera a kutsidya la mtsinje wa Yorodani namutsata Iye.

耶稣经受诱惑

圣灵把耶稣带到旷野,让他经受魔鬼的诱惑。 在禁食四十昼夜后,他感到非常饥饿。 这时,魔鬼来了,对他说∶“如果你是上帝之子,就命令这些石头变成面包吧。”

耶稣回答说∶“《经》上说:

‘人不能只靠面包活着,
人还要听从上帝说的每一句话才能够生存!’” (A)

魔鬼又把耶稣带到圣城耶路撒冷,让他站在大殿院上一个很高的地方,对他说: “如果你是上帝之子,就跳下去吧,因为《经》上说:

‘上帝将吩咐天使帮助你,
他们会用手接住你,
使你的脚不会跌到石头上。’” (B)

耶稣回答说∶“《经》上还说:

‘不可试探主—你的上帝。’” (C)

然后,魔鬼又把耶稣领到一座高山上,把世间万国和它们的荣华富贵都展现在他眼前。 魔鬼说∶“只要你崇拜我,我就把这一切都给你。”

10 耶稣对他说∶“撒旦,走开!《经》上写道:

‘你必须崇拜主—你的上帝,
并且只侍奉他!’” (D)

11 于是,魔鬼便离开了耶稣。天使们前来照顾他。

耶稣在加利利开始传教

12 耶稣听说约翰被捕入狱,就返回了加利利。 13 他没有在拿撒勒停留,而是在迦百农安顿下来。迦百农离西布伦和拿弗他利地区的加利利湖很近。 14 这就应验了先知以赛亚的预言:

15 “西布伦和拿弗他利的土地,
在约旦河西岸,
是通向大海的道路—
加利利,非犹太人的土地!
16 生活在黑暗中的人民将会看到巨光,
在死亡阴影笼罩的土地上的人民,光明将会照耀他们。” (E)

17 耶稣从此开始传教。他向人们宣告∶“悔改吧,上帝的天国临近了。”

耶稣挑选门徒

18 当耶稣沿着加利利湖边行走时,看见兄弟两人—西门(又叫彼得)和他兄弟安得烈。他们是渔夫,正在湖边撒网捕鱼。 19 耶稣对他们说∶“来跟从我,我要使你们成为另一种渔夫,你们将得人而不是得鱼。” 20 兄弟俩听了这话,立刻扔下鱼网,跟随了耶稣。

21 耶稣继续沿湖行走,他看见另外俩兄弟,他们是西庇太的儿子雅各和约翰。他们正在船上和父亲西庇太一起准备鱼网。耶稣召唤他们。 22 兄弟俩立刻离开鱼船和父亲,跟着耶稣走了。

耶稣治病救人

23 耶稣走遍加利利地区,在各会堂里讲教,传播上帝王国的福音,为人们治愈各种疾病。 24 他的事迹传遍了整个叙利亚。人们把病人送到他那里,这些人被不同的疾病和痛苦折磨着,有些人被鬼缠身,有些人患有癫痫症,还有些人瘫痪不起。耶稣为他们一一治好了病。 25 有许多人跟随着耶稣,他们分别来自加利利、低加波利 [a]、耶路撒冷、犹太和约旦河两岸地区。

Footnotes

  1. 馬 太 福 音 4:25 低加波利: 希腊文。在加利利湖东边的一个地区。它曾有主要的十座城镇。

Then was Jesus led up of the Spirit into the wilderness to be tempted of the devil.

And when he had fasted forty days and forty nights, he was afterward an hungred.

And when the tempter came to him, he said, If thou be the Son of God, command that these stones be made bread.

But he answered and said, It is written, Man shall not live by bread alone, but by every word that proceedeth out of the mouth of God.

Then the devil taketh him up into the holy city, and setteth him on a pinnacle of the temple,

And saith unto him, If thou be the Son of God, cast thyself down: for it is written, He shall give his angels charge concerning thee: and in their hands they shall bear thee up, lest at any time thou dash thy foot against a stone.

Jesus said unto him, It is written again, Thou shalt not tempt the Lord thy God.

Again, the devil taketh him up into an exceeding high mountain, and sheweth him all the kingdoms of the world, and the glory of them;

And saith unto him, All these things will I give thee, if thou wilt fall down and worship me.

10 Then saith Jesus unto him, Get thee hence, Satan: for it is written, Thou shalt worship the Lord thy God, and him only shalt thou serve.

11 Then the devil leaveth him, and, behold, angels came and ministered unto him.

12 Now when Jesus had heard that John was cast into prison, he departed into Galilee;

13 And leaving Nazareth, he came and dwelt in Capernaum, which is upon the sea coast, in the borders of Zabulon and Nephthalim:

14 That it might be fulfilled which was spoken by Esaias the prophet, saying,

15 The land of Zabulon, and the land of Nephthalim, by the way of the sea, beyond Jordan, Galilee of the Gentiles;

16 The people which sat in darkness saw great light; and to them which sat in the region and shadow of death light is sprung up.

17 From that time Jesus began to preach, and to say, Repent: for the kingdom of heaven is at hand.

18 And Jesus, walking by the sea of Galilee, saw two brethren, Simon called Peter, and Andrew his brother, casting a net into the sea: for they were fishers.

19 And he saith unto them, Follow me, and I will make you fishers of men.

20 And they straightway left their nets, and followed him.

21 And going on from thence, he saw other two brethren, James the son of Zebedee, and John his brother, in a ship with Zebedee their father, mending their nets; and he called them.

22 And they immediately left the ship and their father, and followed him.

23 And Jesus went about all Galilee, teaching in their synagogues, and preaching the gospel of the kingdom, and healing all manner of sickness and all manner of disease among the people.

24 And his fame went throughout all Syria: and they brought unto him all sick people that were taken with divers diseases and torments, and those which were possessed with devils, and those which were lunatick, and those that had the palsy; and he healed them.

25 And there followed him great multitudes of people from Galilee, and from Decapolis, and from Jerusalem, and from Judaea, and from beyond Jordan.

Jesus Is Tested in the Wilderness(A)

Then Jesus was led by the Spirit into the wilderness to be tempted[a](B) by the devil.(C) After fasting forty days and forty nights,(D) he was hungry. The tempter(E) came to him and said, “If you are the Son of God,(F) tell these stones to become bread.”

Jesus answered, “It is written: ‘Man shall not live on bread alone, but on every word that comes from the mouth of God.’[b](G)

Then the devil took him to the holy city(H) and had him stand on the highest point of the temple. “If you are the Son of God,”(I) he said, “throw yourself down. For it is written:

“‘He will command his angels concerning you,
    and they will lift you up in their hands,
    so that you will not strike your foot against a stone.’[c](J)

Jesus answered him, “It is also written: ‘Do not put the Lord your God to the test.’[d](K)

Again, the devil took him to a very high mountain and showed him all the kingdoms of the world and their splendor. “All this I will give you,” he said, “if you will bow down and worship me.”

10 Jesus said to him, “Away from me, Satan!(L) For it is written: ‘Worship the Lord your God, and serve him only.’[e](M)

11 Then the devil left him,(N) and angels came and attended him.(O)

Jesus Begins to Preach

12 When Jesus heard that John had been put in prison,(P) he withdrew to Galilee.(Q) 13 Leaving Nazareth, he went and lived in Capernaum,(R) which was by the lake in the area of Zebulun and Naphtali— 14 to fulfill(S) what was said through the prophet Isaiah:

15 “Land of Zebulun and land of Naphtali,
    the Way of the Sea, beyond the Jordan,
    Galilee of the Gentiles—
16 the people living in darkness
    have seen a great light;
on those living in the land of the shadow of death
    a light has dawned.”[f](T)

17 From that time on Jesus began to preach, “Repent, for the kingdom of heaven(U) has come near.”

Jesus Calls His First Disciples(V)

18 As Jesus was walking beside the Sea of Galilee,(W) he saw two brothers, Simon called Peter(X) and his brother Andrew. They were casting a net into the lake, for they were fishermen. 19 “Come, follow me,”(Y) Jesus said, “and I will send you out to fish for people.” 20 At once they left their nets and followed him.(Z)

21 Going on from there, he saw two other brothers, James son of Zebedee and his brother John.(AA) They were in a boat with their father Zebedee, preparing their nets. Jesus called them, 22 and immediately they left the boat and their father and followed him.(AB)

Jesus Heals the Sick

23 Jesus went throughout Galilee,(AC) teaching in their synagogues,(AD) proclaiming the good news(AE) of the kingdom,(AF) and healing every disease and sickness among the people.(AG) 24 News about him spread all over Syria,(AH) and people brought to him all who were ill with various diseases, those suffering severe pain, the demon-possessed,(AI) those having seizures,(AJ) and the paralyzed;(AK) and he healed them. 25 Large crowds from Galilee, the Decapolis,[g] Jerusalem, Judea and the region across the Jordan followed him.(AL)

Footnotes

  1. Matthew 4:1 The Greek for tempted can also mean tested.
  2. Matthew 4:4 Deut. 8:3
  3. Matthew 4:6 Psalm 91:11,12
  4. Matthew 4:7 Deut. 6:16
  5. Matthew 4:10 Deut. 6:13
  6. Matthew 4:16 Isaiah 9:1,2
  7. Matthew 4:25 That is, the Ten Cities