Add parallel Print Page Options

“Masiku anga ndi othamanga kupambana makina wolukira nsalu,
    ndipo amatha wopanda chiyembekezo.
Inu Mulungu kumbukirani kuti moyo wanga uli ngati mpweya;
    sindidzaonanso masiku achisangalalo.
Amene akundiona tsopano akundiona;
    mudzandifunafuna koma sindidzapezekanso.

Read full chapter