Font Size
Yobu 7:6-8
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Yobu 7:6-8
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
6 “Masiku anga ndi othamanga kupambana makina wolukira nsalu,
ndipo amatha wopanda chiyembekezo.
7 Inu Mulungu kumbukirani kuti moyo wanga uli ngati mpweya;
sindidzaonanso masiku achisangalalo.
8 Amene akundiona tsopano akundiona;
mudzandifunafuna koma sindidzapezekanso.
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (CCL)
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.