Add parallel Print Page Options

Atumiki a Khristu

Choncho tsono anthu atione ife monga atumiki a Khristu, ndiponso ngati osunga zinsinsi za Mulungu. Chofunika kwambiri nʼchakuti amene apatsidwa udindo oyangʼanira aonetse kukhulupirika. Ine ndilibe nazo kanthu ngati ndiweruzidwa ndi inu kapena khothi lina lililonse. Ndithu, inenso sindidziweruza ndekha. Chikumbumtima changa sichikunditsutsa, koma sikuti ndine wolungama. Wondiweruza ine ndi Ambuye. Chomwecho musaweruze nthawi yoweruza isanakwane. Dikirani mpaka Ambuye atabwera. Iye adzaonetsa poyera zimene zabisika mu mdima ndipo adzaonetsa maganizo a mʼmitima ya anthu. Pa nthawi imeneyo aliyense adzalandira kwa Mulungu chiyamiko.

Tsono abale, ndapereka chitsanzo cha ine mwini ndi Apolo kuti mupindule. Phunzirani kwa ife tanthauzo la mawu akuti, “Musamapitirire zimene Malemba akunena,” kuti musamanyade pamene wina aposa mnzake. Pakuti ndani amakusiyanitsani ndi wina aliyense? Nʼchiyani muli nacho chimene simunalandire? Ndipo ngati munalandira, bwanji mumadzitukumula ngati kuti simunalandire?

Inu muli nazo kale zonse zimene mufuna! Inu mwalemera kale! Inu mwayamba kale kulamulira ife! Ndilakalaka mukanakhaladi mafumu kuti ife tikhale nawo mafumu pamodzi ndi inu. Pakuti kwa ine zikuoneka ngati kuti Mulungu watiyika ife atumwi pachionetsero, kumapeto kwa mndandanda, monga anthu oweruzidwa kuti akaphedwe mʼmabwalo. Ife tayikidwa kuti tionekere ku dziko lonse, kwa angelo ndi anthu. 10 Ife ndife opusa chifukwa cha Khristu, koma inu ndinu anzeru mwa Khristu! Ife ndife ofowoka koma inu ndinu amphamvu! Inu ndinu olemekezeka koma ife ndife opeputsidwa! 11 Mpaka pano tili ndi njala ndi ludzu, tili ndi sanza, tikuzunzidwa, tilibe nyumba. 12 Timagwira ntchito molimbika ndi manja athu. Akamatitemberera, ife timadalitsa; tikasautsidwa, ife timapirira. 13 Pamene atilalatira timayankha mwachifundo. Mpaka pano takhala ngati zinyalala za dziko, monga zakudzala za dziko lapansi.

Pempho ndi Chenjezo

14 Sindikulemba izi kuti ndikuchititseni manyazi, koma kukuchenjezani monga ana anga okondedwa. 15 Ngakhale muli ndi anthu 10,000 okutsogolerani mwa Khristu, mulibe abambo ambiri, popeza mwa Khristu Yesu, ine ndakhala abambo anu kudzera mu Uthenga Wabwino. 16 Chifukwa chake ndikukupemphani kuti munditsanze ine. 17 Chifukwa cha ichi ndikutumiza kwa inu Timoteyo, mwana wanga amene ndimamukonda, amene ndi wokhulupirika mwa Ambuye. Adzakukumbutsani inuyo za moyo wanga mwa Khristu Yesu, umene ukugwirizana ndi zimene ndimaphunzitsa paliponse mu mpingo uliwonse.

18 Ena mwa inu mukudzitukumula, ngati kuti sindingabwere kwanu. 19 Koma ndibwera kwanuko posachedwapa, ngati Ambuye alola, ndipo ndi pamene ndidzadziwe osati zimene anthu odzitukumulawa akuyankhula, koma kuti mphamvu zawo nʼzotani. 20 Pakuti ufumu wa Mulungu si mawu chabe koma mphamvu. 21 Kodi musankha chiyani? Kodi ndidzabwere ndi chikwapu, kapena mu chikondi ndiponso mwa mzimu wofatsa?

The Nature of True Apostleship

This, then, is how you ought to regard us: as servants(A) of Christ and as those entrusted(B) with the mysteries(C) God has revealed. Now it is required that those who have been given a trust must prove faithful. I care very little if I am judged by you or by any human court; indeed, I do not even judge myself. My conscience(D) is clear, but that does not make me innocent.(E) It is the Lord who judges me.(F) Therefore judge nothing(G) before the appointed time; wait until the Lord comes.(H) He will bring to light(I) what is hidden in darkness and will expose the motives of the heart. At that time each will receive their praise from God.(J)

Now, brothers and sisters, I have applied these things to myself and Apollos for your benefit, so that you may learn from us the meaning of the saying, “Do not go beyond what is written.”(K) Then you will not be puffed up in being a follower of one of us over against the other.(L) For who makes you different from anyone else? What do you have that you did not receive?(M) And if you did receive it, why do you boast as though you did not?

Already you have all you want! Already you have become rich!(N) You have begun to reign—and that without us! How I wish that you really had begun to reign so that we also might reign with you! For it seems to me that God has put us apostles on display at the end of the procession, like those condemned to die(O) in the arena. We have been made a spectacle(P) to the whole universe, to angels as well as to human beings. 10 We are fools for Christ,(Q) but you are so wise in Christ!(R) We are weak, but you are strong!(S) You are honored, we are dishonored! 11 To this very hour we go hungry and thirsty, we are in rags, we are brutally treated, we are homeless.(T) 12 We work hard with our own hands.(U) When we are cursed, we bless;(V) when we are persecuted,(W) we endure it; 13 when we are slandered, we answer kindly. We have become the scum of the earth, the garbage(X) of the world—right up to this moment.

Paul’s Appeal and Warning

14 I am writing this not to shame you(Y) but to warn you as my dear children.(Z) 15 Even if you had ten thousand guardians in Christ, you do not have many fathers, for in Christ Jesus I became your father(AA) through the gospel.(AB) 16 Therefore I urge you to imitate me.(AC) 17 For this reason I have sent to you(AD) Timothy,(AE) my son(AF) whom I love, who is faithful in the Lord. He will remind you of my way of life in Christ Jesus, which agrees with what I teach everywhere in every church.(AG)

18 Some of you have become arrogant,(AH) as if I were not coming to you.(AI) 19 But I will come to you very soon,(AJ) if the Lord is willing,(AK) and then I will find out not only how these arrogant people are talking, but what power they have. 20 For the kingdom of God is not a matter of(AL) talk but of power.(AM) 21 What do you prefer? Shall I come to you with a rod of discipline,(AN) or shall I come in love and with a gentle spirit?

Let a man so account of us, as of the ministers of Christ, and stewards of the mysteries of God.

Moreover it is required in stewards, that a man be found faithful.

But with me it is a very small thing that I should be judged of you, or of man's judgment: yea, I judge not mine own self.

For I know nothing by myself; yet am I not hereby justified: but he that judgeth me is the Lord.

Therefore judge nothing before the time, until the Lord come, who both will bring to light the hidden things of darkness, and will make manifest the counsels of the hearts: and then shall every man have praise of God.

And these things, brethren, I have in a figure transferred to myself and to Apollos for your sakes; that ye might learn in us not to think of men above that which is written, that no one of you be puffed up for one against another.

For who maketh thee to differ from another? and what hast thou that thou didst not receive? now if thou didst receive it, why dost thou glory, as if thou hadst not received it?

Now ye are full, now ye are rich, ye have reigned as kings without us: and I would to God ye did reign, that we also might reign with you.

For I think that God hath set forth us the apostles last, as it were appointed to death: for we are made a spectacle unto the world, and to angels, and to men.

10 We are fools for Christ's sake, but ye are wise in Christ; we are weak, but ye are strong; ye are honourable, but we are despised.

11 Even unto this present hour we both hunger, and thirst, and are naked, and are buffeted, and have no certain dwellingplace;

12 And labour, working with our own hands: being reviled, we bless; being persecuted, we suffer it:

13 Being defamed, we intreat: we are made as the filth of the world, and are the offscouring of all things unto this day.

14 I write not these things to shame you, but as my beloved sons I warn you.

15 For though ye have ten thousand instructers in Christ, yet have ye not many fathers: for in Christ Jesus I have begotten you through the gospel.

16 Wherefore I beseech you, be ye followers of me.

17 For this cause have I sent unto you Timotheus, who is my beloved son, and faithful in the Lord, who shall bring you into remembrance of my ways which be in Christ, as I teach every where in every church.

18 Now some are puffed up, as though I would not come to you.

19 But I will come to you shortly, if the Lord will, and will know, not the speech of them which are puffed up, but the power.

20 For the kingdom of God is not in word, but in power.

21 What will ye? shall I come unto you with a rod, or in love, and in the spirit of meekness?