Add parallel Print Page Options

保罗在帖撒罗尼迦的工作

弟兄们,你们自己知道我们来到你们那里并不是徒然的。 我们从前在腓立比蒙难受辱,这是你们知道的,可是我们还是靠着 神给我们的勇气,在强烈反对中把 神的福音传给你们。 我们的劝勉不是出于错误,也不是出于污秽,也不是用诡诈。 但 神既然认定我们经得起考验,把福音托付我们,我们就照着传讲,不是要讨人喜欢,而是要讨那考验我们的心的 神喜欢。 因为我们从来没有用过谄媚的话,这是你们知道的,也没有藏着贪心,这是 神可以作证的。 6-7 我们作为基督的使徒,虽然可以受人尊重,却没有向你们或向别人求荣耀,反而在你们当中心存温柔,如同母亲哺乳自己的孩子。 既然我们这样爱你们,不但乐意将 神的福音给你们,连自己的性命也乐意给你们,因为你们是我们所疼爱的。 弟兄们,你们记念我们的辛苦劳碌,昼夜做工,传 神的福音给你们,免得你们任何人受累。 10 我们对你们信主的人是何等圣洁、正直、无可指责,这有你们作证,也有 神作证。 11 正如你们知道,我们待你们好像父亲待自己的儿女一样。 12 我们劝勉你们,安慰你们,嘱咐你们,使你们行事对得起那召你们进他自己的国、得他荣耀的 神。

13 为此,我们也不断地感谢 神,因为你们听见我们所传 神的道的时候,你们领受了,不以为这是人的道,而以为这确实是 神的道,而且在你们信主的人当中运行着。 14 弟兄们,你们与犹太地区 神的各教会,就是在基督耶稣里的各教会,有同样的遭遇,因为你们也受了同胞的迫害,像他们受了犹太人的迫害一样。 15 这些犹太人不但杀了主耶稣和先知们,又把我们赶出去。他们令 神不悦,且与众人为敌, 16 阻挠我们传道给外邦人,使他们得救,以致常常恶贯满盈,但 神的愤怒终于临到他们身上。

保罗希望再访问帖撒罗尼迦教会

17 弟兄们,我们被迫暂时与你们分离,身体离开,心却没有;我们极力想法子,渴望见你们的面。 18 所以我们很想到你们那里去。我—保罗有一两次要去,只是撒但阻挡了我们。 19 当我们的主耶稣再来,我们站在他面前的时候,我们的盼望、喜乐和所夸的冠冕是什么呢?不正是你们吗? 20 你们就是我们的荣耀和喜乐!

Utumiki wa Paulo ku Atesalonika

Abale, mukudziwa kuti kudzacheza kwathu kwa inu sikunali kosapindulitsa. Monga mukudziwa, ife nʼkuti titazunzika ndi kunyozedwa ku Filipi. Koma mothandizidwa ndi Mulungu wathu, tinalimba mtima mpaka kukulalikirani uthenga wake wabwino ngakhale ambiri ankatsutsana nafe. Pakuti kulalikira kumene tikuchita, sitikuchita ndi maganizo olakwika kapena zolinga zoyipa, kapenanso kufuna kukunamizani. Koma timayankhula monga anthu ovomerezeka ndi Mulungu ndi osungitsidwa Uthenga Wabwino. Ife sitikufuna kukondweretsa anthu koma Mulungu, amene amasanthula mitima yathu. Monga mukudziwa kuti sitinagwiritse ntchito mawu oshashalika kapena mtima wofuna phindu, Mulungu ndiye mboni yathu. Ife sitinafune kutamidwa ndi anthu, kapena ndi inu, kapena wina aliyense mwa inu. Ngati atumwi a Khristu tikanatha kukhala cholemetsa kwa inu, mʼmalo mwake tinali ngati ana aangʼono pakati panu.

Monga mmene amayi amasamalira ana awo angʼono, moteronso tinakusamalirani. Chifukwa tinakukondani kwambiri, tinali okondwa kugawana nanu osati Uthenga Wabwino wa Mulungu wokha, komanso miyoyo yathu. Abale, pakuti mukumbukira kugwira ntchito kwathu kwambiri ndi kuvutika; ife tinagwira ntchito usana ndi usiku ndi cholinga chakuti tisakhale cholemetsa, kwa aliyense pamene ife tinkalalikira Uthenga Wabwino wa Mulungu kwa inu.

10 Inu ndinu mboni, ndiponso Mulungu, kuti tinali oyera mtima, olungama ndi wopanda chifukwa pakati panu amene munakhulupirira. 11 Monga mudziwa kuti ife tinkasamala aliyense wa inu monga abambo amasamalira ana ake, 12 kulimbikitsa, kutonthoza ndi kukupemphani kuti mukhale moyo oyenera Mulungu amene anakuyitanani kuti mulowe mu ufumu wake ndi ulemerero.

13 Ndipo ifenso tikuyamika Mulungu kosalekeza chifukwa mutalandira Mawu a Mulungu, amene munawamva kuchokera kwa ife, munawalandira osati ngati mawu a anthu, koma monga momwe alili, Mawu a Mulungu, amene akugwira ntchito mwa inu amene mukhulupirira. 14 Pakuti inu abale, munakhala otsanzira mipingo ya Mulungu ya ku Yudeya, imene ili mwa Khristu Yesu. Munasautsidwa kuchokera kwa anthu a mtundu wanu, zinthu zomwezo zimene mipingo imeneyi inasautsidwa ndi Ayuda, 15 amene anapha Ambuye Yesu ndi aneneri ndipo anatithamangitsanso ife. Iwo sakondweretsa Mulungu ndipo amadana ndi anthu onse 16 ndikutiretsa ife kuti tisayankhule ndi a mitundu ina kuti angapulumuke. Motero iwo amadziwunjikira okha machimo awo. Mkwiyo wa Mulungu wa afikira tsopano.

Paulo Afunitsitsa Kuonanso Atesalonika

17 Koma abale, titasiyana kwa nthawi pangʼono (mʼthupi osati mʼmaganizo), tinayesetsa koposa kuti tikuoneni. 18 Pakuti ife tinafuna kubweranso kwa inu, makamaka ine Paulo, ndinayesa kangapo koma Satana anatiletsa. 19 Nanga chiyembekezo chathu, chimwemwe chathu kapena chaufumu chimene ife tidzanyadira pamaso pa Ambuye athu Yesu Khristu pamene abwere ndi chiyani? Kodi si inu? 20 Indedi, inu ndinu ulemerero wathu ndi chimwemwe.

Pavlova služba u Solunu

Sami doista znate, braćo: naš dolazak k vama nije bio zaludan. Premda, kao što znate, prethodno štošta pretrpjesmo i bijasmo zlostavljani u Filipima, uz tešku borbu odvažismo vam se, u Bogu našemu, navješćivati Evanđelje Božje. Doista, naše ohrabrivanje nije iz zablude, niti je iz nečistote, niti je iz prijevare; nego, kao što nas je Bog smatrao valjanima da nam povjeri Evanđelje, tako govorimo - ne kao oni koji nastoje ugoditi ljudima, nego Bogu koji preispituje naša srca. Jer nikada, kao što znate, ne nastupismo ni laskavom riječju, ni pritajenom pohlepom - Bog je svjedok - niti smo od ljudi tražili slave - ni od vas, ni od drugih - premda smo vam mogli nametnuti svoj ugled, kao apostoli Kristovi. Naprotiv, bijasmo dječica među vama. Kao što majka hrani i njeguje svoju djecu,[a] tako vam, ispunjeni ljubavlju prema vama, htjedosmo udijeliti ne samo Evanđelje Božje nego i svoje duše, jer ste nam omiljeli. Sjećate se, doista, braćo, našega truda i muke: noću i danju radeći - da ne bismo koga od vas opteretili - propovijedali smo vam Evanđelje Božje. 10 Svjedoci ste vi i Bog kako smo se sveto i pravedno i besprijekorno vladali prema vama, vjernicima. 11 Kao što znate, svakoga smo od vas, kao otac svoju djecu, 12 hrabrili i tješili i zahtijevali da živite dostojno Boga koji vas poziva u svoje kraljevstvo i slavu.

13 I mi neprestance zahvaljujemo Bogu i zato što primivši od nas riječ poruke Božje prihvatiste ju ne kao riječ ljudsku, nego - kao što uistinu i jest - riječ Božju koja i djeluje u vama, vjernicima. 14 Vi, braćo, doista postadoste nasljedovatelji Božjih crkava koje su u Judeji u Kristu Isusu: i vi pretrpjeste od svojih sunarodnjaka isto kao i oni od Židova, 15 koji su ubili i Gospodina Isusa i proroke, i nas progonili, te Bogu ne ugađaju i suprote se svim ljudima[b] 16 priječeći nam navješćivati poganima da se spase, dopunjujući uvijek grijehe svoje. Ali se na njih konačno sručio gnjev Božji.

Pavlova čežnja za ponovnim susretom

17 A mi, braćo, odijeljeni od vas zakratko - licem, ne srcem - u svojoj velikoj čežnji još više pohitasmo da ugledamo vaše lice. 18 Jer smo htjeli doći k vama - a ja, Pavao, i jedanput, i dvaput - no Sotona nas spriječi. 19 Jer što je naša nada ili radost ili vijenac dični pred Gospodinom našim Isusom o njegovu dolasku, ako ne vi? 20 Jer vi ste naša slava i radost.

Footnotes

  1. 1Sol 2,7 Neki rukopisi umjesto »dječica /grč. nepioi/«, imaju: »nježni /grč. epioi/«.
  2. 1Sol 2,15 Umjesto »proroke«, neki rukopisi imaju: »svoje (vlastite) proroke«