Print Page Options
Previous Prev Day Next DayNext

Readings for Celebrating Advent

Scripture passages that focus on the meaning of Advent and Christmas.
Duration: 35 days
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (CCL)
Version
Yesaya 9:6-7

Chifukwa mwana watibadwira,
    mwana wamwamuna wapatsidwa kwa ife,
    ndipo ulamuliro udzakhala pa phewa lake.
Ndipo adzamutcha dzina lake lakuti
    Phungu Wodabwitsa, Mulungu Wamphamvu,
    Atate Amuyaya, ndi Mfumu ya Mtendere.
Ulamuliro ndi mtendere wake
    zidzakhala zopanda malire.
Iye adzalamulira ufumu wake ali pa
    mpando waufumu wa Davide,
ndipo adzawukhazikitsa ndi kuwuchirikiza
    mwa chiweruzo cholungama ndi pochita zachilungamo
    kuyambira nthawi imeneyo mpaka muyaya.
Ndi mtima wake wonse, Yehova Wamphamvuzonse
    watsimikiza kuchita zimenezi.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (CCL)

The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.