Font Size
Readings for Celebrating Advent
Scripture passages that focus on the meaning of Advent and Christmas.
Duration: 35 days
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (CCL)
Masalimo 89:3-4
3 Inu munati, “Ndachita pangano ndi wosankhidwa wanga,
ndalumbira kwa Davide mtumiki wanga kuti,
4 ‘Ndidzakhazikitsa zidzukulu zako mpaka muyaya.
Ndidzachititsa kuti mpando wako waufumu ukhazikike ku mibado yonse,’ ”
Sela.
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (CCL)
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.