Yohane 15
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Mpesa ndi Nthambi
15 “Ine ndine mpesa weniweni, ndipo Atate anga ndiye mwini munda. 2 Iye amadula nthambi iliyonse ya mwa Ine imene sibala chipatso, koma nthambi iliyonse imene imabala chipatso amayisadzira bwino kuti ibale zipatso zambiri. 3 Inu ndinu oyera kale chifukwa cha mawu amene ndayankhula inu. 4 Khalani mwa Ine, monga Ine ndili mwa inu. Palibe nthambi imene ingabereke chipatso pa yokha ngati sinalumikizike ku mpesa. Chomwechonso inu simungathe kubereka chipatso pokhapokha mutakhala mwa Ine.
5 “Ine ndine mpesa; inu ndinu nthambi zake. Ngati munthu akhala mwa Ine ndi Ine mwa iye, adzabereka zipatso zambiri; popanda Ine simungathe kuchita kanthu. 6 Ngati wina aliyense sakhala mwa Ine, iyeyo ali ngati nthambi imene yatayidwa ndi kufota. Nthambi zotero zimatoledwa, kuponyedwa pa moto ndi kupsa. 7 Ngati inu mukhala mwa Ine ndipo mawu anga akhala mwa inu, pemphani chilichonse chimene mukufuna ndipo mudzapatsidwa. 8 Atate anga amalemekezedwa mukamabereka zipatso zochuluka, ndipo potero mudzionetsa kuti ndinu ophunzira anga.
9 “Monga momwe Atate amandikondera Ine, Inenso ndakukondani. Tsopano khalani mʼchikondi changa. 10 Ngati mumvera malamulo anga, mudzakhala mʼchikondi changa, monga Ine ndimamvera malamulo a Atate anga, ndipo ndimakhala mʼchikondi chawo. 11 Ine ndakuwuzani izi kuti chimwemwe changa chikhale mwa Inu, kuti chimwemwe chanu chikhale chokwanira. 12 Lamulo langa ndi ili: ‘Kondanani wina ndi mnzake monga Ine ndakonda inu.’ 13 Palibe munthu ali ndi chikondi choposa ichi, choti munthu nʼkutaya moyo wake chifukwa cha abwenzi ake. 14 Inu ndinu abwenzi anga ngati muchita zimene Ine ndikulamulani. 15 Ine sindikutchulaninso antchito, chifukwa wantchito sadziwa zimene bwana wake akuchita. Mʼmalo mwake Ine ndakutchani abwenzi pakuti zilizonse zimene ndinaphunzira kwa Atate, Ine ndakudziwitsani. 16 Inu simunandisankhe Ine, koma Ine ndinakusankhani kuti mupite ndi kukabereka zipatso, zipatso zake za nthawi yayitali. Choncho Atate adzakupatsani chilichonse chimene mudzapempha mʼdzina langa. 17 Lamulo langa ndi ili: ‘Muzikondana.’
Dziko Lapansi Limada Ophunzira a Yesu
18 “Ngati dziko lapansi lidana nanu, dziwani kuti linayamba kudana ndi Ine. 19 Inu mukanakhala anthu a dziko lapansi, dziko lapansi likanakukondani ngati anthu ake omwe. Koma mmene zilili, inu si anthu a dziko lapansi. Ine ndakusankhani kuchokera mʼdziko lapansi, nʼchifukwa chake dziko lapansi limakudani. 20 Kumbukirani mawu amene ndinayankhula nanu akuti, ‘Palibe wantchito amene amaposa bwana wake.’ Ngati anandizunza Ine, iwo adzakuzunzaninso inu. Ngati anamvera chiphunzitso changa, iwo adzamvera chanunso. 21 Iwo adzakuchitani zimenezi chifukwa cha dzina langa, popeza sakudziwa amene anandituma Ine. 22 Ine ndikanapanda kubwera ndi kuyankhula nawo, sakanakhala ndi mlandu. Koma tsopano alibe choti nʼkukanira mlandu wawo. 23 Iye amene amadana ndi Ine amadananso Atate anga. 24 Ine ndikanapanda kuchita pakati pawo zinthu zimene wina aliyense sanachitepo, iwo sakanakhala ochimwa. Koma tsopano aona zodabwitsa izi, komabe akundida Ine pamodzi ndi Atate anga. 25 Koma zatere kuti zikwaniritse zimene zinalembedwa mʼmalamulo awo: ‘Iwo anandida Ine popanda chifukwa.’
Ntchito ya Mzimu Woyera
26 “Nkhoswe ikadzabwera imene Ine ndidzakutumizireni kuchokera kwa Atate, ndiye Mzimu Woyera wachoonadi amene achokera kwa Atate, Iyeyo adzandichitira umboni Ine. 27 Inunso mudzandichitira umboni Ine, popeza mwakhala nane kuchokera pachiyambi.”
John 15
English Standard Version
I Am the True Vine
15 “I am the (A)true vine, and my Father is (B)the vinedresser. 2 (C)Every branch in me that does not bear fruit (D)he takes away, and every branch that does bear fruit he prunes, (E)that it may bear more fruit. 3 Already (F)you are clean (G)because of the word that I have spoken to you. 4 (H)Abide (I)in me, and I in you. As the branch cannot bear fruit by itself, unless it abides in the vine, neither can you, unless you abide in me. 5 I am the vine; (J)you are the branches. Whoever abides in me and I in him, he it is that (K)bears much fruit, for apart from me you can do nothing. 6 If anyone does not abide in me, (L)he is thrown away like a branch and withers; (M)and the branches are gathered, thrown into the fire, and burned. 7 If (N)you abide in me, and my words abide in you, (O)ask whatever you wish, and it will be done for you. 8 (P)By this my Father is glorified, that you (Q)bear much fruit and so prove to be my disciples. 9 (R)As the Father has loved me, (S)so have I loved you. Abide in my love. 10 (T)If you keep my commandments, you will abide in my love, just as (U)I have kept (V)my Father's commandments and abide in his love. 11 These things I have spoken to you, (W)that my joy may be in you, and that (X)your joy may be full.
12 (Y)“This is my commandment, that you love one another as I have loved you. 13 (Z)Greater love has no one than this, (AA)that someone lay down his life for his friends. 14 You are (AB)my friends (AC)if you do what I command you. 15 (AD)No longer do I call you servants,[a] for the servant (AE)does not know what his master is doing; but I have called you friends, for (AF)all that I have heard from my Father (AG)I have made known to you. 16 You did not choose me, but (AH)I chose you and appointed you that you should go and (AI)bear fruit and that your fruit should abide, so that (AJ)whatever you ask the Father in my name, he may give it to you. 17 These things I command you, (AK)so that you will love one another.
The Hatred of the World
18 (AL)“If the world hates you, know that it has hated me before it hated you. 19 (AM)If you were of the world, the world would love you as its own; but because (AN)you are not of the world, but I chose you out of the world, therefore the world hates you. 20 Remember the word that I said to you: (AO)‘A servant is not greater than his master.’ If they persecuted me, (AP)they will also persecute you. (AQ)If they kept my word, they will also keep yours. 21 But (AR)all these things they will do to you (AS)on account of my name, (AT)because they do not know him who sent me. 22 If I had not come and spoken to them, (AU)they would not have been guilty of sin,[b] but now they have no excuse for their sin. 23 (AV)Whoever hates me hates my Father also. 24 (AW)If I had not done among them the works that no one else did, (AX)they would not be guilty of sin, but now they have (AY)seen and hated both me and my Father. 25 But (AZ)the word that is written in their Law must be fulfilled: (BA)‘They hated me without a cause.’
26 “But (BB)when the Helper comes, whom I will send to you from the Father, the Spirit of truth, who proceeds from the Father, (BC)he will bear witness about me. 27 And (BD)you also will bear witness, (BE)because you have been with me (BF)from the beginning.
Footnotes
- John 15:15 Or bondservants, or slaves (for the contextual rendering of the Greek word doulos, see Preface); likewise for servant later in this verse and in verse 20
- John 15:22 Greek they would not have sin; also verse 24
John 15
New International Version
The Vine and the Branches
15 “I am(A) the true vine,(B) and my Father is the gardener. 2 He cuts off every branch in me that bears no fruit,(C) while every branch that does bear fruit(D) he prunes[a] so that it will be even more fruitful. 3 You are already clean because of the word I have spoken to you.(E) 4 Remain in me, as I also remain in you.(F) No branch can bear fruit by itself; it must remain in the vine. Neither can you bear fruit unless you remain in me.
5 “I am the vine; you are the branches. If you remain in me and I in you, you will bear much fruit;(G) apart from me you can do nothing. 6 If you do not remain in me, you are like a branch that is thrown away and withers; such branches are picked up, thrown into the fire and burned.(H) 7 If you remain in me(I) and my words remain in you, ask whatever you wish, and it will be done for you.(J) 8 This is to my Father’s glory,(K) that you bear much fruit, showing yourselves to be my disciples.(L)
9 “As the Father has loved me,(M) so have I loved you. Now remain in my love. 10 If you keep my commands,(N) you will remain in my love, just as I have kept my Father’s commands and remain in his love. 11 I have told you this so that my joy may be in you and that your joy may be complete.(O) 12 My command is this: Love each other as I have loved you.(P) 13 Greater love has no one than this: to lay down one’s life for one’s friends.(Q) 14 You are my friends(R) if you do what I command.(S) 15 I no longer call you servants, because a servant does not know his master’s business. Instead, I have called you friends, for everything that I learned from my Father I have made known to you.(T) 16 You did not choose me, but I chose you and appointed you(U) so that you might go and bear fruit(V)—fruit that will last—and so that whatever you ask in my name the Father will give you.(W) 17 This is my command: Love each other.(X)
The World Hates the Disciples
18 “If the world hates you,(Y) keep in mind that it hated me first. 19 If you belonged to the world, it would love you as its own. As it is, you do not belong to the world, but I have chosen you(Z) out of the world. That is why the world hates you.(AA) 20 Remember what I told you: ‘A servant is not greater than his master.’[b](AB) If they persecuted me, they will persecute you also.(AC) If they obeyed my teaching, they will obey yours also. 21 They will treat you this way because of my name,(AD) for they do not know the one who sent me.(AE) 22 If I had not come and spoken to them,(AF) they would not be guilty of sin; but now they have no excuse for their sin.(AG) 23 Whoever hates me hates my Father as well. 24 If I had not done among them the works no one else did,(AH) they would not be guilty of sin.(AI) As it is, they have seen, and yet they have hated both me and my Father. 25 But this is to fulfill what is written in their Law:(AJ) ‘They hated me without reason.’[c](AK)
The Work of the Holy Spirit
26 “When the Advocate(AL) comes, whom I will send to you from the Father(AM)—the Spirit of truth(AN) who goes out from the Father—he will testify about me.(AO) 27 And you also must testify,(AP) for you have been with me from the beginning.(AQ)
Footnotes
- John 15:2 The Greek for he prunes also means he cleans.
- John 15:20 John 13:16
- John 15:25 Psalms 35:19; 69:4
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
The ESV® Bible (The Holy Bible, English Standard Version®), © 2001 by Crossway, a publishing ministry of Good News Publishers. ESV Text Edition: 2025.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.

