Add parallel Print Page Options

Mʼbusa Wabwino ndi Nkhosa Zake

10 “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani inu Afarisi, kuti munthu amene salowera pa khomo mʼkhola la nkhosa, koma amalowera pena pake ndi wakuba ndi wachifwamba. Munthu amene amalowera pa khomo ndi mʼbusa wankhosazo. Mlonda amamutsekulira khomo, ndipo nkhosa zimamvera mawu ake. Iye amaziyitana mayina nkhosa zakezo, nazitulutsa. Akazitulutsa nkhosa zake zonse, iye amazitsogolera, ndipo nkhosa zakezo zimamutsata chifukwa zimadziwa mawu ake. Koma nkhosazo sizidzatsatira mlendo. Izo zidzamuthawa chifukwa sizizindikira mawu a mlendo.” Yesu ananena mawu ophiphiritsawa, koma Afarisi sanazindikire zimene ankawawuza.

Choncho Yesu anatinso, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Ine ndine khomo la nkhosa. Onse amene anadza ndisanabwere Ine ndi akuba ndi achifwamba, ndipo nkhosa sizinawamvere. Ine ndine khomo, aliyense amene alowa kudzera mwa Ine adzapulumuka. Iye adzalowa ndi kutuluka ndi kupeza msipu. 10 Mbala sibwera chabe koma kuti idzabe, kupha ndi kuwononga. Ine ndabwera kuti iwo akhale ndi moyo, ndi kukhala nawo wochuluka.

11 “Ine ndine Mʼbusa wabwino. Mʼbusa wabwino amataya moyo wake chifukwa cha nkhosa zake. 12 Wantchito ndi mʼbusa amene nkhosazo si zake. Choncho, pamene aona mmbulu ukubwera, iye amazisiya nkhosazo ndi kuthawa. Ndipo mmbulu umagwira nkhosazo ndikuzibalalitsa. 13 Munthuyo amathawa chifukwa ndi wantchito ndipo sasamalira chilichonse cha nkhosazo.

14 “Ine ndine mʼbusa wabwino. Ine ndimazidziwa nkhosa zanga ndipo nkhosa zangazo zimandidziwa, 15 monga momwe Atate amandidziwa Ine, ndiponso Ine kudziwira Atatewo. Ndimapereka moyo wanga chifukwa cha nkhosa. 16 Ine ndili ndi nkhosa zina zimene sizili za gulu ili. Ine ndiyenera kuzibweretsanso. Izonso zidzamvera mawu anga, ndipo zidzakhala gulu limodzi ndi mʼbusa mmodzi. 17 Nʼchifukwa chake Atate anga amandikonda, popeza Ine ndikupereka moyo wanga kuti ndiwutengenso. 18 Palibe amene angawuchotse mwa Ine, koma ndikuwupereka mwakufuna kwanga. Ine ndili ndi ulamuliro wa kuwupereka ndi ulamuliro wakuwutenganso. Lamulo ili ndinalandira kwa Atate anga.”

19 Pa mawu awa Ayuda anagawikananso. 20 Ambiri a iwo anati, “Iye ndi wogwidwa ndi ziwanda ndi wamisala. Chifukwa chiyani mukumvera Iye?”

21 Koma ena anati, “Awa si mawu a munthu wogwidwa ndi ziwanda. Kodi ziwanda zingathe bwanji kutsekula maso a wosaona?”

Kusakhulupirira kwa Ayuda

22 Ku Yerusalemu kunali chikondwerero chokumbukira kupatulidwa kwa Nyumba ya Mulungu. Inali nthawi yozizira, 23 ndipo Yesu ankayenda mʼbwalo la Nyumbayo ku malo a Solomoni. 24 Ayuda anamuzungulira Iye akunena kuti, “Kodi iwe udzazunguza malingaliro athu mpaka liti? Ngati iwe ndi Khristu, tiwuze momveka.”

25 Yesu anayankha kuti, “Ine ndimakuwuzani, koma inu simukhulupirira. Ntchito zimene ndikuchita mʼdzina la Atate anga zikundichitira umboni, 26 koma inu simukhulupirira chifukwa simuli a gulu lankhosa zanga. 27 Nkhosa zanga zimamva mawu anga, Ine ndimazidziwa, ndipo zimanditsata Ine. 28 Ine ndimazipatsa moyo wosatha ndipo sizidzawonongeka. Palibe amene adzazikwatula mʼdzanja langa. 29 Atate anga, amene anandipatsa Ine, ndi akulu kuposa onse. Palibe amene angazikwatule mʼdzanja la Atate anga. 30 Ine ndi Atate ndife amodzi.”

31 Ayuda anatolanso miyala kuti amugende Iye, 32 koma Yesu anawawuza kuti, “Ine ndakuonetsani zinthu zambiri zabwino zodabwitsa kuchokera kwa Atate. Nʼchifukwa chiti mwa izi chimene mukundigendera?”

33 Ayuda anayankha kuti, “Ife sitikukugenda chifukwa cha izi, koma popeza ukunyoza Mulungu, chifukwa iwe, munthu wamba, ukuti ndiwe Mulungu.”

34 Yesu anawayankha kuti, “Kodi sizinalembedwa mʼmalamulo anu kuti, ‘Ine ndanena kuti ndinu milungu?’ 35 Ngati anawatcha milungu anthu amene analandira mawu a Mulungu, pajatu Malemba sangasweke, 36 nanga bwanji uyu amene Atate anamuyika padera monga wake weniweni ndi kumutuma ku dziko lapansi? Nanga ndi chifukwa chiyani mukundinena Ine kuti ndikuchita chipongwe? Kodi nʼchifukwa choti ndanena kuti, ‘Ine ndine Mwana wa Mulungu?’ 37 Musandikhulupirire Ine ngati sindichita ntchito za Atate anga. 38 Koma ngati Ine ndikuchita zimenezi, ngakhale kuti simundikhulupirira, khulupirirani ntchito zodabwitsazo, ndipo mudziwe ndi kuzindikira kuti Atate ali mwa Ine, ndiponso Ine ndili mwa Atate.” 39 Iwo anafuna kumugwiranso koma anawapulumuka mʼmanja mwawo.

40 Kenaka Yesu anabwereranso kutsidya la mtsinje wa Yorodani kumalo kumene Yohane ankabatiza mʼmasiku akale. Iye anakhala kumeneko 41 ndipo anthu ambiri anabwera kwa Iye. Iwo anati, “Ngakhale kuti Yohane sanachite chizindikiro chodabwitsa, zonse zimene Yohane ananena za munthu uyu zinali zoona.” 42 Ndipo pamalo amenewo ambiri anakhulupirira Yesu.

Jesus the True Shepherd

10 “Most assuredly, I say to you, he who does not enter the sheepfold by the door, but climbs up some other way, the same is a thief and a robber. But he who enters by the door is the shepherd of the sheep. To him the doorkeeper opens, and the sheep hear his voice; and he calls his own sheep by (A)name and leads them out. And when he brings out his own sheep, he goes before them; and the sheep follow him, for they know his voice. Yet they will by no means follow a (B)stranger, but will flee from him, for they do not know the voice of strangers.” Jesus used this illustration, but they did not understand the things which He spoke to them.

Jesus the Good Shepherd

Then Jesus said to them again, “Most assuredly, I say to you, I am the door of the sheep. All who ever came [a]before Me are thieves and robbers, but the sheep did not hear them. (C)I am the door. If anyone enters by Me, he will be saved, and will go in and out and find pasture. 10 The thief does not come except to steal, and to kill, and to destroy. I have come that they may have life, and that they may have it more abundantly.

11 (D)“I am the good shepherd. The good shepherd gives His life for the sheep. 12 But a [b]hireling, he who is not the shepherd, one who does not own the sheep, sees the wolf coming and (E)leaves the sheep and flees; and the wolf catches the sheep and scatters them. 13 The hireling flees because he is a hireling and does not care about the sheep. 14 I am the good shepherd; and (F)I know My sheep, and (G)am known by My own. 15 (H)As the Father knows Me, even so I know the Father; (I)and I lay down My life for the sheep. 16 And (J)other sheep I have which are not of this fold; them also I must bring, and they will hear My voice; (K)and there will be one flock and one shepherd.

17 “Therefore My Father (L)loves Me, (M)because I lay down My life that I may take it again. 18 No one takes it from Me, but I lay it down of Myself. I (N)have power to lay it down, and I have power to take it again. (O)This command I have received from My Father.”

19 Therefore (P)there was a division again among the Jews because of these sayings. 20 And many of them said, (Q)“He has a demon and is [c]mad. Why do you listen to Him?”

21 Others said, “These are not the words of one who has a demon. (R)Can a demon (S)open the eyes of the blind?”

The Shepherd Knows His Sheep

22 Now it was the Feast of Dedication in Jerusalem, and it was winter. 23 And Jesus walked in the temple, (T)in Solomon’s porch. 24 Then the Jews surrounded Him and said to Him, “How long do You keep us in [d]doubt? If You are the Christ, tell us plainly.”

25 Jesus answered them, “I told you, and you do not believe. (U)The works that I do in My Father’s name, they (V)bear witness of Me. 26 But (W)you do not believe, because you are not of My sheep, [e]as I said to you. 27 (X)My sheep hear My voice, and I know them, and they follow Me. 28 And I give them eternal life, and they shall never perish; neither shall anyone snatch them out of My hand. 29 (Y)My Father, (Z)who has given them to Me, is greater than all; and no one is able to snatch them out of My Father’s hand. 30 (AA)I and My Father are one.”

Renewed Efforts to Stone Jesus

31 Then (AB)the Jews took up stones again to stone Him. 32 Jesus answered them, “Many good works I have shown you from My Father. For which of those works do you stone Me?”

33 The Jews answered Him, saying, “For a good work we do not stone You, but for (AC)blasphemy, and because You, being a Man, (AD)make Yourself God.”

34 Jesus answered them, “Is it not written in your law, (AE)‘I said, “You are gods” ’? 35 If He called them gods, (AF)to whom the word of God came (and the Scripture (AG)cannot be broken), 36 do you say of Him (AH)whom the Father sanctified and (AI)sent into the world, ‘You are blaspheming,’ (AJ)because I said, ‘I am (AK)the Son of God’? 37 (AL)If I do not do the works of My Father, do not believe Me; 38 but if I do, though you do not believe Me, (AM)believe the works, that you may know and [f]believe (AN)that the Father is in Me, and I in Him.” 39 (AO)Therefore they sought again to seize Him, but He escaped out of their hand.

The Believers Beyond Jordan

40 And He went away again beyond the Jordan to the place (AP)where John was baptizing at first, and there He stayed. 41 Then many came to Him and said, “John performed no sign, (AQ)but all the things that John spoke about this Man were true.” 42 And many believed in Him there.

Footnotes

  1. John 10:8 M omits before Me
  2. John 10:12 hired man
  3. John 10:20 insane
  4. John 10:24 Suspense
  5. John 10:26 NU omits as I said to you
  6. John 10:38 NU understand

Jésus, le bon berger

10 »En vérité, en vérité, je vous le dis, celui qui n'entre pas dans l'enclos des brebis par la porte mais s'y introduit par un autre endroit est un voleur et un brigand. Mais celui qui entre par la porte est le berger des brebis. Le gardien lui ouvre et les brebis écoutent sa voix; il appelle par leur nom les brebis qui lui appartiennent et il les conduit dehors. Lorsqu'il les a [toutes] fait sortir, il marche devant elles et les brebis le suivent, parce qu'elles connaissent sa voix. Elles ne suivront pas un étranger, mais elles fuiront au contraire loin de lui, parce qu'elles ne connaissent pas la voix des étrangers.» Jésus leur dit cette parabole[a], mais ils ne comprirent pas de quoi il leur parlait.

Jésus leur dit encore: «En vérité, en vérité, je vous le dis, je suis la porte des brebis. Tous ceux qui sont venus avant moi sont des voleurs et des brigands, mais les brebis ne les ont pas écoutés. C’est moi qui suis la porte. Si quelqu'un entre par moi, il sera sauvé; il entrera et sortira, et il trouvera de quoi se nourrir. 10 Le voleur ne vient que pour voler, égorger et détruire; moi, je suis venu afin que les brebis aient la vie et qu'elles l'aient en abondance.

11 »Je suis le bon berger. Le bon berger donne sa vie pour ses brebis. 12 Le simple salarié, quant à lui, n'est pas le berger et les brebis ne lui appartiennent pas. Lorsqu'il voit venir le loup, il abandonne les brebis et prend la fuite; alors le loup s'en empare et les disperse. 13 [Le simple salarié s'enfuit] car il travaille pour de l’argent et ne se soucie pas des brebis. 14 Moi, je suis le bon berger. Je connais mes brebis et elles me connaissent, 15 tout comme le Père me connaît et comme je connais le Père. Je donne ma vie pour mes brebis. 16 J'ai encore d'autres brebis, qui ne sont pas de cet enclos; celles-là aussi, il faut que je les amène; elles écouteront ma voix et il y aura un seul troupeau, un seul berger. 17 Le Père m'aime, parce que je donne ma vie pour la reprendre ensuite. 18 Personne ne me l'enlève, mais je la donne de moi-même. J'ai le pouvoir de la donner et j'ai le pouvoir de la reprendre. Tel est l'ordre que j'ai reçu de mon Père.»

19 Ces paroles provoquèrent de nouveau une division parmi les Juifs. 20 Beaucoup d'entre eux disaient: «Il a un démon, il est fou. Pourquoi l'écoutez-vous?» 21 D'autres disaient: «Ce ne sont pas les paroles d'un démoniaque. Un démon peut-il ouvrir les yeux des aveugles?»

22 On célébrait alors à Jérusalem la fête de la dédicace. C'était l'hiver. 23 Jésus marchait dans le temple, sous le portique de Salomon. 24 Les Juifs l'entourèrent et lui dirent: «Jusqu'à quand nous laisseras-tu dans l'incertitude? Si tu es le Messie, dis-le-nous franchement.»

25 Jésus leur répondit: «Je vous l'ai dit et vous ne croyez pas. Les œuvres que je fais au nom de mon Père témoignent en ma faveur, 26 mais vous ne croyez pas parce que vous ne faites pas partie de mes brebis, [comme je vous l'ai dit]. 27 Mes brebis écoutent ma voix, je les connais et elles me suivent. 28 Je leur donne la vie éternelle. Elles ne périront jamais et personne ne pourra les arracher à ma main. 29 Mon Père, qui me les a données, est plus grand que tous et personne ne peut les arracher à la main de mon Père. 30 Le Père et moi, nous sommes un.»

31 Alors les Juifs prirent de nouveau des pierres pour le lapider. 32 Jésus leur dit: «Je vous ai fait voir beaucoup de belles œuvres qui viennent de mon Père. A cause de laquelle me lapidez-vous?» 33 Les Juifs lui répondirent: «Ce n'est pas pour une belle œuvre que nous te lapidons, mais pour un blasphème, parce que toi, qui es un être humain, tu te fais Dieu.» 34 Jésus leur répondit: «N'est-il pas écrit dans votre loi: J'ai dit: ‘Vous êtes des dieux’[b]? 35 S’il est vrai qu’elle a appelé dieux ceux à qui la parole de Dieu a été adressée et si l'Ecriture ne peut pas être annulée, 36 comment pouvez-vous dire à celui que le Père a consacré et envoyé dans le monde: ‘Tu blasphèmes’, et cela parce que j'ai affirmé: ‘Je suis le Fils de Dieu’? 37 Si je ne fais pas les œuvres de mon Père, ne me croyez pas! 38 Mais si je les fais, même si vous ne me croyez pas, croyez à ces œuvres afin de savoir et de reconnaître que le Père est en moi et que je suis en lui.» 39 Voilà pourquoi ils cherchaient encore à l'arrêter, mais il leur échappa.

40 Jésus retourna de l'autre côté du Jourdain, à l'endroit où Jean avait d'abord baptisé, et il y resta. 41 Beaucoup de gens vinrent vers lui; ils disaient: «Jean n'a fait aucun signe miraculeux, mais tout ce qu'il a dit à propos de cet homme était vrai.» 42 Et là, beaucoup crurent en lui.

Footnotes

  1. Jean 10:6 Parabole: histoire visant à faire comprendre une vérité spirituelle au moyen d’un exemple tiré de la vie courante.
  2. Jean 10:34 J’ai dit… dieux: citation du Psaume 82.6.