Yobu 25
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Mawu a Bilidadi
25 Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
2 “Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu,
Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.
3 Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka?
Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?
4 Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu?
Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?
5 Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni,
ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,
6 nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi,
mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”
Job 25
New International Version
Bildad
25 Then Bildad the Shuhite(A) replied:
2 “Dominion and awe belong to God;(B)
he establishes order in the heights of heaven.(C)
3 Can his forces be numbered?
On whom does his light not rise?(D)
4 How then can a mortal be righteous before God?
How can one born of woman be pure?(E)
5 If even the moon(F) is not bright
and the stars are not pure in his eyes,(G)
6 how much less a mortal, who is but a maggot—
a human being,(H) who is only a worm!”(I)
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.