Add parallel Print Page Options

Chiweruzo ndi Chipulumutso

65 “Ndinali wokonzeka kumva mapemphero a amene sankandipempha kanthu;
    ndipo ndinalola kuti anthu amene ankandifunafuna kuti andipeze.
Kwa mtundu wa anthu umene sunkapempha chithandizo kwa Ine,
    ndinati, ‘Ine ndili pano, Ine ndili pano.’
Tsiku lonse ndatambasulira manja anga
    anthu owukira aja,
amene amachita zoyipa,
    natsatira zokhumba zawo.
Ndatambasulira manja anga anthu aja amene nthawi zonse amandikwiyitsa
    mopanda manyazi.
Iwo amapereka nsembe mʼminda
    ndi kufukiza lubani pa maguwa ansembe a njerwa.
Amakatandala ku manda
    ndipo amakachezera usiku wonse kumalo obisika.
Amadya nyama ya nkhumba,
    ndipo mʼmiphika mwawo muli msunzi wa nyama yodetsedwa.
Amawuza ena kuti, ‘Khala patali usandiyandikire,
    chifukwa ungatengere kupatulika kwanga!’
Ukali wanga pa anthu otere uli ngati utsi mphuno zanga,
    ngati moto umene umayaka tsiku lonse.

“Taonani, ndatsimikiza kale mlandu ndi chilango chawo;
    sindidzakhala chete koma ndidzawalanga kwathunthu
    chifukwa cha machimo awo
ndi a makolo awo,”
    akutero Yehova.
“Chifukwa anapereka nsembe zopsereza pa mapiri
    ndi kundinyoza Ine pa zitunda zawo,
Ine ndidzawalanga kwathunthu potsata
    zimene anachita kale.”

Yehova akuti,

“Pamene madzi akanapezeka mu phava la mphesa
    ndipo anthu amati, ‘Musawononge phavalo,
    popeza madzi ena abwino akanalimobe mʼphavalo,’
Inenso chifukwa cha mtumiki wanga;
    sindidzawononga onse.
Ndidzatulutsa zidzukulu mʼbanja la Yakobo,
    ndipo a banja la Yuda adzalandira mapiri anga ngati cholowa chawo.
Anthu anga osankhidwa adzalandira zimenezi,
    ndipo atumiki anga adzakhala kumeneko.
10 Chigwa cha Saroni chidzakhala kodyetserako nkhosa,
    ndipo chigwa cha Akori chidzakhala malo opumirako ngʼombe
    kwa anthu anga ondifunafuna Ine.

11 “Koma inu amene mumasiya Yehova
    ndi kuyiwala phiri langa lopatulika,
amene munamukonzera Gadi chakudya
    ndi kuthirira Meni chakumwa,
12 ndidzakuperekani ku lupanga ngati nsembe,
    ndipo nonse mudzaphedwa;
chifukwa simunayankhe pamene ndinakuyitanani,
    ndinayankhula koma simunamvere.
Munachita zoyipa pamaso panga
    ndipo munasankha kuchita zoyipa zomwe sindikondwera nazo.”

13 Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti,

“Atumiki anga adzadya,
    koma inu mudzakhala ndi njala;
atumiki anga adzamwa,
    koma inu mudzakhala ndi ludzu;
atumiki anga adzakondwa,
    koma inu mudzakhala ndi manyazi.
14 Atumiki anga adzayimba
    mosangalala,
koma inu mudzalira kwambiri
    chifukwa chovutika mu mtima
    ndipo mudzalira mofuwula chifukwa mudzamva kuwawa mu mtima.
15 Anthu anga osankhidwa
    adzatchula dzina lanu potemberera.
Ambuye Yehova adzakuphani,
    koma atumiki ake adzawapatsa dzina lina.
16 Aliyense wopempha dalitso mʼdzikomo
    adzachita zimenezo kwa Mulungu woona;
ndipo aliyense wochita malumbiro mʼdzikomo
    adzalumbira mwa Mulungu woona.
Pakuti mavuto akale adzayiwalika
    ndipo adzachotsedwa pamaso panga.

Chilengedwe Chatsopano

17 “Taonani, ndikulenga
    mlengalenga mwatsopano ndi dziko lapansi latsopano.
Zinthu zakale sizidzakumbukika,
    zidzayiwalika kotheratu.
18 Koma inu mukhale osangalala ndi okondwa mpaka muyaya
    chifukwa cha zimene ndikulenga,
pakuti ndikulenga Yerusalemu kukhala malo wosangalatsa
    ndipo anthu ake adzakhala achimwemwe.
19 Ine ndidzakondwa chifuwa cha Yerusalemu
    ndipo ndidzasangalala chifukwa cha anthu anga.
Kumeneko sikudzamvekanso kulira
    ndi mfuwu wodandaula.

20 “Ana sadzafa ali akhanda
    ndipo nkhalamba zonse zidzakwaniritsa zaka zawo zonse.
    Wamngʼono mwa iwo
adzafa ali ndi zaka 100.
    Amene adzalephere kufika zaka 100
adzatengedwa kukhala
    wotembereredwa.
21 Anthu adzamanga nyumba ndi kukhalamo,
    adzadzala mpesa ndipo adzadya zipatso zake.
22 Sadzamanganso nyumba anthu ena nʼkukhalamo,
    kapena kudzala ndi ena nʼkudya.
Pakuti anthu anga adzakhala ndi moyo
    wautali ngati mitengo.
Osankhidwa anga adzakondwera ndi ntchito
    ya manja awo nthawi yayitali.
23 Sadzagwira ntchito pachabe
    kapena kubereka ana kuti aone tsoka;
chifukwa adzakhala anthu odalitsidwa ndi Yehova,
    iwowo pamodzi ndi adzukulu awo omwe.
24 Ndidzawayankha ngakhale asanathe nʼkupempha komwe.
    Pamene akuyankhula kumene Ine ndidzakhala nditamva kale.
25 Mʼmbulu ndi mwana wankhosa wamkazi zidzadyera pamodzi.
    Mkango udzadya udzu monga ngʼombe,
    koma fumbi ndiye chidzakhale chakudya cha njoka.
Pa phiri langa lopatulika sipadzakhala
    chinthu chopweteka kapena chowononga,”
            akutero Yehova.

懲罰與拯救

65 耶和華說:「我向沒有求問我的人顯現,
讓沒有尋找我的人尋見,
對沒有求告我的國家說,
『我在這裡,我在這裡!』
我整天伸出雙手招呼一群悖逆的百姓,
他們卻任意妄為,
不走正路,
不斷地當面惹我發怒。
他們在園中獻祭,
在磚臺上燒香,
坐在墳場裡,
宿在隱秘處。
他們吃豬肉,
用不潔之物做湯,
還對人說,『站遠點,
別挨近我,因為我比你聖潔!』
我被這些人氣得鼻孔冒煙,
整天怒火難息。
看啊,這些都記錄在我面前,
我不會再保持緘默,
我要報應他們,
按他們和他們祖先的罪報應他們。
我必按他們的所作所為報應他們,
因為他們在山上燒香,
在丘陵上褻瀆我。
這是耶和華說的。」

耶和華說:「人發現一串葡萄尚可釀造新酒時,
一定會說,『不要毀壞它,
裡面還有好葡萄。』
同樣,因我僕人的緣故,
我也不會把他們全部毀滅。

「我必使雅各的後裔興起,
使猶大人興起,
繼承我的群山。
我揀選的子民必擁有那片土地,
我的僕人必在那裡安居。
10 沙崙必成為牧放羊群的草場,
亞割谷必成為牛群休憩的地方,
這些地方必屬於尋求我的人。
11 但至於你們這些背棄我、
忘記我的聖山、
擺宴供奉幸運之神、
調酒祭奠命運之神的人,
12 我要使你們註定被殺,
喪身刀下。
因為我呼喚你們,你們不回應;
我講話,你們不聆聽。
你們做我視為惡的事,
專行令我不悅的事。」

13 所以主耶和華說:
「看啊,我的僕人必有吃有喝,
你們卻要饑渴交加;
我的僕人必歡喜,
你們卻要受羞辱;
14 我的僕人必歡喜快樂,
揚聲歌唱,
你們卻要傷心欲絕,
嚎啕大哭。
15 我的選民必用你們的名字作咒詛,
主耶和華必殺死你們,
給祂的僕人另起名字。
16 因此,在地上求福祉的人都必向信實的上帝祈求,
在地上起誓的人都必憑信實的上帝起誓。
因為過去的苦難已經被遺忘,
從我眼前消失了。

新天新地

17 「看啊,我要創造新天新地,
過去的一切都要被遺忘,
從記憶中消失。
18 你們要因我創造的一切而永遠歡喜快樂。
看啊,我要創造一個充滿喜樂的耶路撒冷,
其中的居民個個歡欣。
19 我必因耶路撒冷而歡喜,
因我的子民而快樂。
城裡再聽不見哭泣和哀號聲。
20 再沒有只活幾天便夭折的嬰兒,
也沒有壽數未盡便死的老人,
因為滿了百歲便死的人不過算是青年,
不足百歲便死的人被視為受了咒詛。
21 他們要建造房屋,安然居住,
栽種葡萄園,吃園中的果子。
22 他們建的房屋再不會被別人居住,
他們種的果實再不會被別人享用。
我的子民必像樹木一樣長壽,
我揀選的人必長享自己親手勞碌的成果。
23 他們不會徒勞,
他們的孩子也不會遇到災禍,
因為他們及其子孫是蒙上帝賜福的人。
24 他們還沒有求告,
我就已經應允;
他們正要禱告,
我就已經垂聽。
25 豺狼和綿羊必一起吃草,
獅子必像牛一樣吃草,
蛇必以塵土為食。
在我的整個聖山上,
牠們都不傷人,不害物。
這是耶和華說的。」

65 I am sought of them that asked not for me; I am found of them that sought me not: I said, Behold me, behold me, unto a nation that was not called by my name.

I have spread out my hands all the day unto a rebellious people, which walketh in a way that was not good, after their own thoughts;

A people that provoketh me to anger continually to my face; that sacrificeth in gardens, and burneth incense upon altars of brick;

Which remain among the graves, and lodge in the monuments, which eat swine's flesh, and broth of abominable things is in their vessels;

Which say, Stand by thyself, come not near to me; for I am holier than thou. These are a smoke in my nose, a fire that burneth all the day.

Behold, it is written before me: I will not keep silence, but will recompense, even recompense into their bosom,

Your iniquities, and the iniquities of your fathers together, saith the Lord, which have burned incense upon the mountains, and blasphemed me upon the hills: therefore will I measure their former work into their bosom.

Thus saith the Lord, As the new wine is found in the cluster, and one saith, Destroy it not; for a blessing is in it: so will I do for my servants' sakes, that I may not destroy them all.

And I will bring forth a seed out of Jacob, and out of Judah an inheritor of my mountains: and mine elect shall inherit it, and my servants shall dwell there.

10 And Sharon shall be a fold of flocks, and the valley of Achor a place for the herds to lie down in, for my people that have sought me.

11 But ye are they that forsake the Lord, that forget my holy mountain, that prepare a table for that troop, and that furnish the drink offering unto that number.

12 Therefore will I number you to the sword, and ye shall all bow down to the slaughter: because when I called, ye did not answer; when I spake, ye did not hear; but did evil before mine eyes, and did choose that wherein I delighted not.

13 Therefore thus saith the Lord God, Behold, my servants shall eat, but ye shall be hungry: behold, my servants shall drink, but ye shall be thirsty: behold, my servants shall rejoice, but ye shall be ashamed:

14 Behold, my servants shall sing for joy of heart, but ye shall cry for sorrow of heart, and shall howl for vexation of spirit.

15 And ye shall leave your name for a curse unto my chosen: for the Lord God shall slay thee, and call his servants by another name:

16 That he who blesseth himself in the earth shall bless himself in the God of truth; and he that sweareth in the earth shall swear by the God of truth; because the former troubles are forgotten, and because they are hid from mine eyes.

17 For, behold, I create new heavens and a new earth: and the former shall not be remembered, nor come into mind.

18 But be ye glad and rejoice for ever in that which I create: for, behold, I create Jerusalem a rejoicing, and her people a joy.

19 And I will rejoice in Jerusalem, and joy in my people: and the voice of weeping shall be no more heard in her, nor the voice of crying.

20 There shall be no more thence an infant of days, nor an old man that hath not filled his days: for the child shall die an hundred years old; but the sinner being an hundred years old shall be accursed.

21 And they shall build houses, and inhabit them; and they shall plant vineyards, and eat the fruit of them.

22 They shall not build, and another inhabit; they shall not plant, and another eat: for as the days of a tree are the days of my people, and mine elect shall long enjoy the work of their hands.

23 They shall not labour in vain, nor bring forth for trouble; for they are the seed of the blessed of the Lord, and their offspring with them.

24 And it shall come to pass, that before they call, I will answer; and while they are yet speaking, I will hear.

25 The wolf and the lamb shall feed together, and the lion shall eat straw like the bullock: and dust shall be the serpent's meat. They shall not hurt nor destroy in all my holy mountain, saith the Lord.

The Lord’s Response

65 “I was sought by those who did not ask;[a]
I was found by those who did not seek Me.
I said: Here I am, here I am,
to a nation that was not called by[b] My name.(A)
I spread out My hands all day long
to a rebellious people(B)
who walk in the wrong path,
following their own thoughts.
These people continually provoke Me
to My face,
sacrificing in gardens,(C)
burning incense on bricks,
sitting among the graves,
spending nights in secret places,
eating the meat of pigs,(D)
and putting polluted broth in their bowls.[c]
They say, ‘Keep to yourself,
don’t come near me, for I am too holy for you!’
These practices are smoke in My nostrils,
a fire that burns all day long.
It is written before Me:
I will not keep silent,(E) but I will repay;(F)
I will repay them fully[d]
for your iniquities and the iniquities(G)
of your[e] fathers together,”
says the Lord.
“Because they burned incense on the mountains
and reproached Me on the hills,(H)
I will reward them fully[f]
for their former deeds.”

The Lord says this:

As the new wine is found in a bunch of grapes,
and one says, ‘Don’t destroy it,
for there’s some good[g] in it,’
so I will act because of My servants
and not destroy them all.
I will produce descendants from Jacob,(I)
and heirs to My mountains from Judah;
My chosen(J) ones will possess it,
and My servants will dwell there.(K)
10 Sharon will be a pasture for flocks,(L)
and the Valley of Achor a place for cattle to lie down,(M)
for My people who have sought Me.(N)
11 But you who abandon the Lord,
who forget My holy mountain,
who prepare a table for Fortune
and fill bowls of mixed wine for Destiny,[h]
12 I will destine you for the sword,
and all of you will kneel down to be slaughtered,
because I called and you did not answer,
I spoke and you did not hear;
you did what was evil in My sight
and chose what I did not delight in.(O)

13 Therefore, this is what the Lord God says:

My servants will eat,
but you will be hungry;
My servants will drink,
but you will be thirsty;
My servants will rejoice,
but you will be put to shame.
14 My servants will shout for joy from a glad heart,
but you will cry out from an anguished heart,
and you will lament out of a broken spirit.
15 You will leave your name behind
as a curse for My chosen ones,(P)
and the Lord God will kill you;
but He will give His servants another name.(Q)
16 Whoever is blessed in the land
will be blessed by the God of truth,(R)
and whoever swears in the land
will swear by the God of truth.
For the former troubles will be forgotten
and hidden from My sight.

A New Creation

17 “For I will create a new heaven and a new earth;(S)
the past events will not be remembered or come to mind.
18 Then be glad and rejoice forever
in what I am creating;
for I will create Jerusalem to be a joy
and its people to be a delight.
19 I will rejoice in Jerusalem
and be glad in My people.
The sound of weeping and crying
will no longer be heard in her.(T)
20 In her, a nursing infant will no longer live
only a few days,[i]
or an old man not live out his days.
Indeed, the youth will die at a hundred years,
and the one who misses a hundred years will be cursed.(U)
21 People will build houses and live in them;
they will plant vineyards and eat their fruit.(V)
22 They will not build and others live in them;
they will not plant and others eat.
For My people’s lives will be
like the lifetime of a tree.(W)
My chosen ones will fully enjoy
the work of their hands.
23 They will not labor without success(X)
or bear children destined for disaster,
for they will be a people blessed by the Lord
along with their descendants.(Y)
24 Even before they call, I will answer;(Z)
while they are still speaking, I will hear.
25 The wolf and the lamb will feed together,[j]
and the lion will eat straw like the ox,(AA)
but the serpent’s food will be dust!(AB)
They will not do what is evil or destroy
on My entire holy mountain,”(AC)
says the Lord.

Footnotes

  1. Isaiah 65:1 LXX, Syr, DSS, Tg read ask for Me
  2. Isaiah 65:1 LXX, Syr, DSS, Tg, Vg read that did not call on
  3. Isaiah 65:4 These vv. describe pagan worship.
  4. Isaiah 65:6 Lit repay into their lap
  5. Isaiah 65:7 LXX, Syr read [for] their iniquities and the iniquities of their
  6. Isaiah 65:7 Lit reward into their lap
  7. Isaiah 65:8 Or there’s a blessing
  8. Isaiah 65:11 Pagan gods
  9. Isaiah 65:20 Lit her, no longer infant of days
  10. Isaiah 65:25 Lit as one