Add parallel Print Page Options

Yehova Agonjetsa Anthu a Mitundu Ina

63 Kodi ndani uyo akubwera kuchokera ku Edomu,
    atavala zovala za ku Bozira za madontho ofiira?
Kodi uyu ndani, amene wavala zovala zokongola,
    akuyenda mwa mphamvu zake?

“Ndi Ineyo, woyankhula zachilungamo
    ndiponso wamphamvu zopulumutsa.”

Nanga bwanji zovala zanu zili psuu,
    ngati za munthu wofinya mphesa?

“Ndapondereza ndekha anthu a mitundu ina ngati mphesa,
    palibe ndi mmodzi yemwe anali nane.
Ndinawapondereza ndili wokwiya
    ndipo ndinawapondereza ndili ndi ukali;
magazi awo anadothera pa zovala zanga,
    ndipo zovala zanga zonse zinathimbirira.
Pakuti ndinatsimikiza mu mtima mwanga kuti lafika tsiku lolipsira anthu anga;
    ndipo chaka cha kuwomboledwa kwanga chafika.
Ndinayangʼana ndipo panalibe munthu wondithandiza.
    Ndinadabwa kwambiri kuti panalibe wondichirikiza;
choncho ndinapambana ndi mphamvu zanga,
    ndipo mkwiyo wanga unandilimbitsa.
Ndinapondereza mitundu ya anthu ndili wokwiya;
    ndipo ndinawasakaza
    ndipo ndinathira magazi awo pansi.”

Matamando ndi Pemphero

Ndidzafotokoza za kukoma mtima kwa Yehova,
    ntchito zimene Iye ayenera kutamandidwa.
    Ndidzatamanda Yehova chifukwa cha zonse zimene watichitira.
Inde, mwa chifundo ndi kukoma mtima kwake
    Yehova wachitira nyumba ya Israeli
    zinthu zabwino zambiri.
Yehova anati, “Ndithu awa ndi anthu anga,
    ana anga amene sadzandinyenga Ine.”
    Choncho anawapulumutsa.
Iyenso anasautsidwa mʼmasautso awo onse,
    ndipo mngelo wochokera kwa Iye anawapulumutsa.
Mwa chikondi ndi chifundo chake iye anawapulumutsa,
    anawanyamula ndikuwatenga
    kuyambira kale lomwe.
10 Komabe iwo anawukira
    ndi kumvetsa chisoni Mzimu Woyera.
Motero Yehova anatembenuka nakhala mdani wawo
    ndipo Iye mwini anamenyana nawo.

11 Pamenepo anthu ake anakumbukira masiku amakedzana,
    masiku a Mose mtumiki wake;
ndipo anafunsa kuti, “Ali kuti Yehova amene anawawolotsa pa nyanja,
    pamodzi ndi Mose mʼbusa wawo?
Ali kuti Iye amene anayika
    Mzimu Woyera pakati pawo?
12 Ali kuti amene anachita zinthu zodabwitsa
    ndi mphamvu zake zazikulu kudzera mwa Mose?
Ali kuti amene anagawa madzi pa nyanja anthu ake akuona,
    kuti dzina lake limveke mpaka muyaya,
13 amene anawayendetsa pa nyanja yozama?
Monga kavalo woyendayenda mʼchipululu,
    iwo sanapunthwe;
14 Mzimu Woyera unawapumulitsa
    ngati mmene ngʼombe zimapumulira.
Umu ndi mmene Inu munatsogolera anthu anu
    kuti dzina lanu lilemekezeke.”

15 Inu Yehova amene muli kumwambako, pa mpando wanu wolemekezeka,
    wopatulika ndi waulemerero, tiyangʼaneni ife.
Kodi changu chanu ndi mphamvu zanu zili kuti?
    Simukutionetsanso kukoma mtima kwanu ndi chifundo chanu.
16 Koma Inu ndinu Atate athu,
    ngakhale Abrahamu satidziwa
    kapena Israeli kutivomereza ife;
Inu Yehova, ndinu Atate athu,
    kuyambira kale dzina lanu ndinu Mpulumutsi wathu.
17 Chifukwa chiyani, Inu Yehova, mukutisocheretsa pa njira zanu?
    Bwanji mukutilola kuti tikhale owuma mitima kotero kuti sitikukuopaninso?
Bwererani chifukwa cha atumiki anu;
    mafuko a anthu amene ali cholowa chanu.
18 Anthu anu atangokhala pa malo anu opatulika pa kanthawi kochepa,
    adani athu anasakaza malo anu opatulika.
19 Ife tili ngati anthu amene
    simunawalamulirepo
    ngati iwo amene sanakhalepo anthu anu.

The Lord's Day of Vengeance

63 Who is this who comes from (A)Edom,
    in crimsoned garments from (B)Bozrah,
he who is splendid in his apparel,
    (C)marching in the greatness of his strength?
“It is I, speaking in righteousness,
    mighty to save.”

Why is your (D)apparel red,
    and your garments like his (E)who treads in the winepress?

(F)“I have trodden the winepress alone,
    (G)and from the peoples no one was with me;
I trod them in my anger
    and trampled them in my wrath;
their lifeblood[a] spattered on my garments,
    and stained all my apparel.
(H)For the day of vengeance was in my heart,
    and my year of redemption[b] had come.
I looked, but (I)there was no one to help;
    I was appalled, but there was no one to uphold;
so my own arm brought me salvation,
    and my wrath upheld me.
I trampled down the peoples in my anger;
    (J)I made them drunk in my wrath,
    and I poured out their lifeblood on the earth.”

The Lord's Mercy Remembered

I will recount the steadfast love of the Lord,
    the praises of the Lord,
according to all that the Lord has granted us,
    (K)and the great goodness to the house of Israel
that he has granted them according to his compassion,
    according to the abundance of his steadfast love.
For he said, “Surely they are my people,
    children who will not deal falsely.”
    And he became their Savior.
(L)In all their affliction he was afflicted,[c]
    and the angel of his presence saved them;
(M)in his love and in his pity he redeemed them;
    (N)he lifted them up and carried them all the days of old.

10 (O)But they rebelled
    (P)and grieved his Holy Spirit;
therefore he turned to be their enemy,
    and himself fought against them.
11 Then he remembered (Q)the days of old,
    of Moses and his people.[d]
(R)Where is he who brought them up out of the sea
    with the shepherds of his flock?
Where is he who put in the midst of them
    his Holy Spirit,
12 who caused his glorious arm
    to go at the right hand of Moses,
(S)who divided the waters before them
    (T)to make for himself an everlasting name,
13     who led them through the depths?
Like a horse in the desert,
    they did not stumble.
14 Like livestock that go down into the valley,
    (U)the Spirit of the Lord gave them rest.
So you led your people,
    (V)to make for yourself a glorious name.

Prayer for Mercy

15 (W)Look down from heaven and see,
    (X)from your holy and beautiful[e] habitation.
Where are (Y)your zeal and your might?
    The stirring of your inner parts and your compassion
    are held back from me.
16 For (Z)you are our Father,
    though Abraham does not know us,
    and Israel does not acknowledge us;
you, O Lord, are our Father,
    (AA)our Redeemer from of old is your name.
17 O Lord, why do you make us wander from your ways
    and (AB)harden our heart, so that we fear you not?
(AC)Return for the sake of your servants,
    the tribes of your heritage.
18 (AD)Your holy people held possession for a little while;[f]
    (AE)our adversaries have trampled down your sanctuary.
19 (AF)We have become like those over whom you have never ruled,
    like those who are not called by your name.

Footnotes

  1. Isaiah 63:3 Or their juice; also verse 6
  2. Isaiah 63:4 Or the year of my redeemed
  3. Isaiah 63:9 Or he did not afflict
  4. Isaiah 63:11 Or Then his people remembered the days of old, of Moses
  5. Isaiah 63:15 Or holy and glorious
  6. Isaiah 63:18 Or They have dispossessed your holy people for a little while

The Lord in Judgment and Salvation

63 Who is this who comes from Edom,
With dyed garments from Bozrah,
This One who is [a]glorious in His apparel,
Traveling in the greatness of His strength?—

“I who speak in righteousness, mighty to save.”

Why (A)is Your apparel red,
And Your garments like one who treads in the winepress?

“I have (B)trodden the winepress alone,
And from the peoples no one was with Me.
For I have trodden them in My anger,
And trampled them in My fury;
Their blood is sprinkled upon My garments,
And I have stained all My robes.
For the (C)day of vengeance is in My heart,
And the year of My redeemed has come.
(D)I looked, but (E)there was no one to help,
And I wondered
That there was no one to uphold;
Therefore My own (F)arm brought salvation for Me;
And My own fury, it sustained Me.
I have trodden down the peoples in My anger,
Made them drunk in My fury,
And brought down their strength to the earth.”

God’s Mercy Remembered

I will mention the lovingkindnesses of the Lord
And the praises of the Lord,
According to all that the Lord has bestowed on us,
And the great goodness toward the house of Israel,
Which He has bestowed on them according to His mercies,
According to the multitude of His lovingkindnesses.
For He said, “Surely they are My people,
Children who will not lie.”
So He became their Savior.
(G)In all their affliction He was [b]afflicted,
(H)And the Angel of His Presence saved them;
(I)In His love and in His pity He redeemed them;
And (J)He bore them and carried them
All the days of old.
10 But they (K)rebelled and (L)grieved His Holy Spirit;
(M)So He turned Himself against them as an enemy,
And He fought against them.

11 Then he (N)remembered the days of old,
Moses and his people, saying:
“Where is He who (O)brought them up out of the sea
With the [c]shepherd of His flock?
(P)Where is He who put His Holy Spirit within them,
12 Who led them by the right hand of Moses,
(Q)With His glorious arm,
(R)Dividing the water before them
To make for Himself an everlasting name,
13 (S)Who led them through the deep,
As a horse in the wilderness,
That they might not stumble?”

14 As a beast goes down into the valley,
And the Spirit of the Lord causes him to rest,
So You lead Your people,
(T)To make Yourself a glorious name.

A Prayer of Penitence

15 (U)Look down from heaven,
And see (V)from Your habitation, holy and glorious.
Where are Your zeal and Your strength,
The yearning (W)of Your heart and Your mercies toward me?
Are they restrained?
16 (X)Doubtless You are our Father,
Though Abraham (Y)was ignorant of us,
And Israel does not acknowledge us.
You, O Lord, are our Father;
Our Redeemer from Everlasting is Your name.
17 O Lord, why have You (Z)made us stray from Your ways,
And hardened our heart from Your fear?
Return for Your servants’ sake,
The tribes of Your inheritance.
18 (AA)Your holy people have possessed it but a little while;
(AB)Our adversaries have trodden down Your sanctuary.
19 We have become like those of old, over whom You never ruled,
Those who were never called by Your name.

Footnotes

  1. Isaiah 63:1 Or adorned
  2. Isaiah 63:9 Kt., LXX, Syr. not afflicted
  3. Isaiah 63:11 MT, Vg. shepherds