Chivumbulutso 20
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Zaka 1,000
20 Ndipo ndinaona mngelo akutsika kuchokera kumwamba ali ndi kiyi ya ku chidzenje chakuya chija atanyamula mʼdzanja lake unyolo waukulu. 2 Iye anachigwira chinjokacho, chinjoka chakalekale chija, amene ndi Mdierekezi kapena kuti Satana, ndipo anamumanga zaka 1,000. 3 Anamuponya ku chidzenje chakuya chija namutsekera ndi kiyi ndi kumatirira pa khomopo kuti asatulukenso kukanyenga mitundu ya anthu mpaka patapita zaka 1,000. Zikadzatha zakazo, adzamumasula kwa kanthawi pangʼono chabe.
4 Ndinaona mipando yaufumu pamene anakhalapo anthu amene anapatsidwa mphamvu zoweruza. Ndipo ndinaona mizimu ya amene anadulidwa makosi chifukwa cha umboni wa Yesu ndi chifukwa cha Mawu a Mulungu. Iwo sanapembedze nawo chirombo kapena fano lake ndipo sanalembedwe chizindikiro chake pa mphumi zawo kapena pa manja awo. Iwo anakhalanso ndi moyo nalamulira pamodzi ndi Khristu zaka 1,000. 5 (Akufa ena onse sanaukenso mpaka zitatha zaka 1,000). Uku ndiko kuuka kwa akufa koyamba. 6 Odala ndi oyera mtima amene adzaukitsidwa nawo pa kuukitsidwa koyamba. Imfa yachiwiri ilibe mphamvu pa iwo koma adzakhala ansembe a Mulungu ndi a Khristu ndipo adzalamulira naye pamodzi zaka 1,000.
Kugonjetsedwa kwa Satana
7 Zaka 1,000 zikadzatha, Satana adzamasulidwa ku ndende yake 8 ndipo adzapita kukanyenga mitundu ya anthu kumbali zonse zinayi za dziko lapansi, Gogi ndi Magogi, kuwasonkhanitsa kuti akachite nkhondo. Kuchuluka kwawo kudzakhala ngati mchenga wa mʼmbali mwa nyanja. 9 Iwo anayenda ponseponse pa dziko lapansi nazinga msasa wa anthu a Mulungu, mzinda umene Iye amawukonda. Koma moto unatsika kuchokera kumwamba ndi kuwanyeketsa. 10 Ndipo Mdierekezi amene anawanyenga, anaponyedwa mʼnyanja ya sulufule wotentha, kumene kunaponyedwa chirombo chija ndi mneneri wonama uja. Iwo adzazunzika usiku ndi usana kwamuyaya.
Chiweruzo Chotsiriza
11 Kenaka ndinaona Mpando Waufumu waukulu woyera ndi Iye amene anakhalapo. Dziko lapansi ndi kumwamba zinathawa pamaso pake ndipo panalibenso malo awo. 12 Ndipo ndinaona akufa, aakulu ndi aangʼono omwe atayimirira patsogolo pa Mpando Waufumu ndipo mabuku anatsekulidwa. Buku lina linatsekulidwa limene linali Buku Lamoyo. Akufa anaweruzidwa monga mwa zimene anachita monga mmene zinalembedwera mʼmabuku. 13 Nyanja inapereka amene anaferamo ndipo imfa ndi Hade zinapereka akufa ake ndipo munthu aliyense anaweruzidwa monga mwa ntchito zake. 14 Kenaka imfa ndi Hade zinaponyedwa mʼnyanja ya moto. Nyanja yamoto ndiyo imfa yachiwiri. 15 Ngati dzina la wina aliyense silinapezeke mʼBuku Lamoyo, anaponyedwa mʼnyanja yamoto.
Revelation 20
New King James Version
Satan Bound 1,000 Years
20 Then I saw an angel coming down from heaven, (A)having the key to the bottomless pit and a great chain in his hand. 2 He laid hold of (B)the dragon, that serpent of old, who is the Devil and Satan, and bound him for a thousand years; 3 and he cast him into the bottomless pit, and shut him up, and (C)set a seal on him, (D)so that he should deceive the nations no more till the thousand years were finished. But after these things he must be released for a little while.
The Saints Reign with Christ 1,000 Years
4 And I saw (E)thrones, and they sat on them, and (F)judgment was committed to them. Then I saw (G)the souls of those who had been beheaded for their witness to Jesus and for the word of God, (H)who had not worshiped the beast (I)or his image, and had not received his mark on their foreheads or on their hands. And they (J)lived and (K)reigned with Christ for [a]a thousand years. 5 But the rest of the dead did not live again until the thousand years were finished. This is the first resurrection. 6 Blessed and holy is he who has part in the first resurrection. Over such (L)the second death has no power, but they shall be (M)priests of God and of Christ, (N)and shall reign with Him a thousand years.
Satanic Rebellion Crushed(O)
7 Now when the thousand years have expired, Satan will be released from his prison 8 and will go out (P)to deceive the nations which are in the four corners of the earth, (Q)Gog and Magog, (R)to gather them together to battle, whose number is as the sand of the sea. 9 (S)They went up on the breadth of the earth and surrounded the camp of the saints and the beloved city. And fire came down from God out of heaven and devoured them. 10 The devil, who deceived them, was cast into the lake of fire and brimstone (T)where[b] the beast and the false prophet are. And they (U)will be tormented day and night forever and ever.
The Great White Throne Judgment
11 Then I saw a great white throne and Him who sat on it, from whose face (V)the earth and the heaven fled away. (W)And there was found no place for them. 12 And I saw the dead, (X)small and great, standing before [c]God, (Y)and books were opened. And another (Z)book was opened, which is the Book of Life. And the dead were judged (AA)according to their works, by the things which were written in the books. 13 The sea gave up the dead who were in it, (AB)and Death and Hades delivered up the dead who were in them. (AC)And they were judged, each one according to his works. 14 Then (AD)Death and Hades were cast into the lake of fire. (AE)This is the second [d]death. 15 And anyone not found written in the Book of Life (AF)was cast into the lake of fire.
Footnotes
- Revelation 20:4 M the
- Revelation 20:10 NU, M where also
- Revelation 20:12 NU, M the throne
- Revelation 20:14 NU, M death, the lake of fire.
Revelation 20
King James Version
20 And I saw an angel come down from heaven, having the key of the bottomless pit and a great chain in his hand.
2 And he laid hold on the dragon, that old serpent, which is the Devil, and Satan, and bound him a thousand years,
3 And cast him into the bottomless pit, and shut him up, and set a seal upon him, that he should deceive the nations no more, till the thousand years should be fulfilled: and after that he must be loosed a little season.
4 And I saw thrones, and they sat upon them, and judgment was given unto them: and I saw the souls of them that were beheaded for the witness of Jesus, and for the word of God, and which had not worshipped the beast, neither his image, neither had received his mark upon their foreheads, or in their hands; and they lived and reigned with Christ a thousand years.
5 But the rest of the dead lived not again until the thousand years were finished. This is the first resurrection.
6 Blessed and holy is he that hath part in the first resurrection: on such the second death hath no power, but they shall be priests of God and of Christ, and shall reign with him a thousand years.
7 And when the thousand years are expired, Satan shall be loosed out of his prison,
8 And shall go out to deceive the nations which are in the four quarters of the earth, Gog, and Magog, to gather them together to battle: the number of whom is as the sand of the sea.
9 And they went up on the breadth of the earth, and compassed the camp of the saints about, and the beloved city: and fire came down from God out of heaven, and devoured them.
10 And the devil that deceived them was cast into the lake of fire and brimstone, where the beast and the false prophet are, and shall be tormented day and night for ever and ever.
11 And I saw a great white throne, and him that sat on it, from whose face the earth and the heaven fled away; and there was found no place for them.
12 And I saw the dead, small and great, stand before God; and the books were opened: and another book was opened, which is the book of life: and the dead were judged out of those things which were written in the books, according to their works.
13 And the sea gave up the dead which were in it; and death and hell delivered up the dead which were in them: and they were judged every man according to their works.
14 And death and hell were cast into the lake of fire. This is the second death.
15 And whosoever was not found written in the book of life was cast into the lake of fire.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Scripture taken from the New King James Version®. Copyright © 1982 by Thomas Nelson. Used by permission. All rights reserved.
