Psalm 26:2-4
Revised Standard Version Catholic Edition
2 Prove me, O Lord, and try me;
test my heart and my mind.
3 For thy steadfast love is before my eyes,
and I walk in faithfulness to thee.[a]
4 I do not sit with false men,
nor do I consort with dissemblers;
Footnotes
- Psalm 26:3 Or in thy faithfulness
Masalimo 26:2-4
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
2 Patseni mayeso, Inu Yehova ndipo ndiyeseni,
santhulani mtima wanga ndi maganizo anga;
3 pakuti chikondi chanu chili pamaso panga nthawi zonse,
ndipo ndimayenda mʼchoonadi chanu nthawi zonse.
4 Ine sindikhala pansi pamodzi ndi anthu achinyengo,
kapena kufunsa nzeru kwa achiphamaso.
The Revised Standard Version of the Bible: Catholic Edition, copyright © 1965, 1966 the Division of Christian Education of the National Council of the Churches of Christ in the United States of America. Used by permission. All rights reserved.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.