Add parallel Print Page Options

13 Mwana wanzeru amamvera malangizo a abambo ake,
    koma mwana wonyoza samamvetsera chidzudzulo.

Munthu amapeza zinthu zabwino chifukwa cha mawu ake,
    koma anthu osakhulupirika amalakalaka zachiwawa basi.

Iye amene amagwira pakamwa pake amateteza moyo wake,
    koma amene amayankhula zopanda pake adzawonongeka.

Munthu waulesi amakhumbira zinthu koma sapeza kanthu,
    koma munthu wakhama adzalemera.

Munthu wolungama amadana ndi zabodza,
    koma zochita za munthu woyipa zimanyansa ndiponso zimachititsa manyazi.

Chilungamo chimateteza munthu wangwiro,
    koma tchimo limagwetsa munthu wochimwa.

Wina amadziyesa kuti ndi wolemera chonsecho alibe kanthu kalikonse;
    munthu wina amaoneka ngati wosauka chonsecho ali ndi chuma chambiri.

Chuma cha munthu wolemera chitha kuwombola moyo wake,
    koma munthu wosauka amamva chidzudzulo.

Nyale ya munthu wolungama ndi yokondweretsa,
    koma nyale ya munthu woyipa imazimitsidwa.

10 Chipongwe chosamalabadirako za anthu ena chimadzetsa mikangano,
    koma womva malangizo a anzawo ndiwo ali ndi nzeru.

11 Chuma chochipeza mofulumira chidzatha pangʼonopangʼono
    koma chuma chosonkhanitsidwa pangʼonopangʼono chidzachulukirachulukira.

12 Chinthu chochiyembekezera chikalephereka chimalefula mtima,
    koma chinthu chochilakalaka chikachitikadi chimakhala ngati mtengo wamoyo.

13 Amene amanyoza malangizo adzawonongeka,
    koma amene amasamala lamulo amalandira mphotho.

14 Malangizo a munthu wanzeru ali ngati kasupe wamoyo;
    amathandiza munthu kuti asakondwe mu msampha wa imfa.

15 Munthu wa nzeru zabwino amapeza kuyanja pakati pa anthu,
    koma munthu wosakhulupirika adzawonongeka.

16 Munthu wochenjera amachita zinthu mwanzeru,
    koma chitsiru chimaonetsa poyera uchitsiru wake.

17 Wamthenga woyipa amagwetsa anthu mʼmavuto,
    koma nthumwi yodalirika imabweretsa mtendere.

18 Wokana mwambo adzasauka ndi kunyozedwa,
    koma wosamala chidzudzulo adzalemekezedwa.

19 Chinthu chochilakalaka chikachitika chimasangalatsa mtima,
    koma zitsiru zimadana ndi kuleka zoyipa.

20 Woyenda ndi anthu anzeru nayenso adzakhala wanzeru;
    koma woyenda ndi zitsiru adzapwetekeka.

21 Choyipa chitsata mwini,
    koma wochita zolungama adzalandira mphotho yabwino.

22 Munthu wabwino amasiyira zidzukulu zake cholowa,
    koma chuma cha munthu wochimwa amachilandira ndi olungama.

23 Tsala la munthu wosauka limalola chakudya chambiri,
    koma anthu opanda chilungamo amachilanda.

24 Amene sakwapula mwana wake, ndiye kuti amamuda,
    koma wokonda mwana wake sazengereza kumulanga.

25 Munthu wolungama amakhala ndi zakudya zoti adye nʼkukhuta,
    koma mʼmimba mwa munthu woyipa mumakhala pululu ndi njala.

13 A wise son responds to his father’s discipline,
but a mocker doesn’t listen to rebuke.

From the words of his mouth,
a man will enjoy good things,(A)
but treacherous people have an appetite for violence.(B)

The one who guards his mouth protects his life;(C)
the one who opens his lips invites his own ruin.(D)

The slacker craves, yet has nothing,
but the diligent is fully satisfied.(E)

The righteous hate lying,
but the wicked act disgustingly and disgracefully.

Righteousness guards people of integrity,[a]
but wickedness undermines the sinner.(F)

One man pretends to be rich but has nothing;(G)
another pretends to be poor but has great wealth.(H)

Riches are a ransom for a man’s life,(I)
but a poor man hears no threat.

The light of the righteous shines brightly,(J)
but the lamp of the wicked is put out.(K)

10 Arrogance leads to nothing but strife,(L)
but wisdom is gained by those who take advice.

11 Wealth obtained by fraud will dwindle,(M)
but whoever earns it through labor[b] will multiply it.(N)

12 Delayed hope makes the heart sick,
but fulfilled desire is a tree of life.(O)

13 The one who has contempt for instruction will pay the penalty,(P)
but the one who respects a command will be rewarded.(Q)

14 A wise man’s instruction is a fountain of life,(R)
turning people away from the snares of death.(S)

15 Good sense wins favor,(T)
but the way of the treacherous never changes.[c]

16 Every sensible person acts knowledgeably,
but a fool displays his stupidity.(U)

17 A wicked messenger falls into trouble,
but a trustworthy courier brings healing.(V)

18 Poverty and disgrace come to those
who ignore discipline,
but the one who accepts correction will be honored.(W)

19 Desire fulfilled is sweet to the taste,
but to turn from evil(X)
is an abomination to fools.

20 The one who walks with the wise will become wise,
but a companion of fools will suffer harm.

21 Disaster pursues sinners,
but good rewards the righteous.(Y)

22 A good man leaves an inheritance to his[d] grandchildren,
but the sinner’s wealth is stored up for the righteous.(Z)

23 The uncultivated field of the poor yields abundant food,
but without justice, it is swept away.

24 The one who will not use the rod hates his son,(AA)
but the one who loves him disciplines him diligently.(AB)

25 A righteous man eats until he is satisfied,
but the stomach of the wicked is empty.(AC)

Footnotes

  1. Proverbs 13:6 Lit guards integrity of way
  2. Proverbs 13:11 Lit whoever gathers upon [his] hand
  3. Proverbs 13:15 LXX, Syr, Tg read treacherous will perish
  4. Proverbs 13:22 Or inheritance: his

13 El hijo sabio acepta la corrección del padre;
el insolente no hace caso de reprensiones.

Cada uno recoge el fruto de lo que dice,
pero los traidores tienen hambre de violencia.

Cuidar las palabras es cuidarse uno mismo;
el que habla mucho se arruina solo.

El perezoso desea y no consigue;
el que trabaja, prospera.

El hombre justo odia la mentira;
el malvado es motivo de vergüenza y deshonra.

La rectitud protege al hombre intachable;
la maldad destruye al pecador.

Hay quienes no tienen nada y presumen de ricos,
y hay quienes todo lo tienen y aparentan ser pobres.

La riqueza del rico le salva la vida;
el pobre jamás escucha amenazas.

Los justos son como una luz brillante;
los malvados, como lámpara que se apaga.

10 El orgullo sólo provoca peleas;
la sabiduría está con los humildes.

11 La riqueza ilusoria, disminuye;
el que la junta poco a poco, la aumenta.

12 Esperanza frustrada, corazón afligido,
pero el deseo cumplido es como un árbol de vida.

13 El que desatiende una orden, lo lamentará;
el que respeta el mandato será recompensado.

14 La enseñanza del sabio es fuente de vida
y libra de los lazos de la muerte.

15 El buen juicio se gana el aprecio,
pero los traidores marchan a su ruina.

16 El que es prudente actúa con inteligencia,
pero el necio hace gala de su necedad.

17 El mensajero malvado acarrea problemas,
pero el mensajero fiel los alivia.

18 Pobreza y deshonra tendrá quien desprecia el consejo;
grandes honores, quien atiende la corrección.

19 El deseo cumplido es causa de alegría.
Los necios no soportan alejarse del mal.

20 Júntate con sabios y obtendrás sabiduría;
júntate con necios y te echarás a perder.

21 Los pecadores son perseguidos por el mal;
los justos, recompensados con el bien.

22 El hombre bueno deja herencia a sus nietos;
el pecador amasa fortunas que serán del justo.

23 En el campo del pobre hay comida abundante,
pero mucho se pierde donde no hay justicia.

24 Quien no corrige a su hijo, no lo quiere;
el que lo ama, lo corrige.

25 El justo come hasta estar satisfecho,
pero el malvado se queda con hambre.

13 A wise son heeds his father’s instruction,
    but a mocker does not respond to rebukes.(A)

From the fruit of their lips people enjoy good things,(B)
    but the unfaithful have an appetite for violence.

Those who guard their lips(C) preserve their lives,(D)
    but those who speak rashly will come to ruin.(E)

A sluggard’s appetite is never filled,(F)
    but the desires of the diligent are fully satisfied.

The righteous hate what is false,(G)
    but the wicked make themselves a stench
    and bring shame on themselves.

Righteousness guards the person of integrity,
    but wickedness overthrows the sinner.(H)

One person pretends to be rich, yet has nothing;(I)
    another pretends to be poor, yet has great wealth.(J)

A person’s riches may ransom their life,
    but the poor cannot respond to threatening rebukes.(K)

The light of the righteous shines brightly,
    but the lamp of the wicked is snuffed out.(L)

10 Where there is strife, there is pride,
    but wisdom is found in those who take advice.(M)

11 Dishonest money dwindles away,(N)
    but whoever gathers money little by little makes it grow.

12 Hope deferred makes the heart sick,
    but a longing fulfilled is a tree of life.(O)

13 Whoever scorns instruction will pay for it,(P)
    but whoever respects(Q) a command is rewarded.(R)

14 The teaching of the wise is a fountain of life,(S)
    turning a person from the snares of death.(T)

15 Good judgment wins favor,
    but the way of the unfaithful leads to their destruction.[a]

16 All who are prudent act with[b] knowledge,
    but fools expose(U) their folly.(V)

17 A wicked messenger falls into trouble,(W)
    but a trustworthy envoy brings healing.(X)

18 Whoever disregards discipline comes to poverty and shame,(Y)
    but whoever heeds correction is honored.(Z)

19 A longing fulfilled is sweet to the soul,(AA)
    but fools detest turning from evil.

20 Walk with the wise and become wise,
    for a companion of fools suffers harm.(AB)

21 Trouble pursues the sinner,(AC)
    but the righteous(AD) are rewarded with good things.(AE)

22 A good person leaves an inheritance for their children’s children,
    but a sinner’s wealth is stored up for the righteous.(AF)

23 An unplowed field produces food for the poor,
    but injustice sweeps it away.

24 Whoever spares the rod(AG) hates their children,
    but the one who loves their children is careful to discipline(AH) them.(AI)

25 The righteous eat to their hearts’ content,
    but the stomach of the wicked goes hungry.(AJ)

Footnotes

  1. Proverbs 13:15 Septuagint and Syriac; the meaning of the Hebrew for this phrase is uncertain.
  2. Proverbs 13:16 Or prudent protect themselves through