Add parallel Print Page Options

Za Kuweruza Ena

“Musaweruze ena, kuti inunso mungadzaweruzidwe. Pakuti momwe inu muweruzira ena, inunso mudzaweruzidwa chimodzimodzi, muyeso umene muyesera ena inunso mudzayesedwa ndi womwewo.

“Chifukwa chiyani iwe uyangʼana kachitsotso ka mʼdiso la mʼbale wako koma susamalira chimtengo chili mʼdiso mwako? Kodi unganene bwanji kwa mʼbale wako kuti, ‘Ndikuchotse kachitsotso mʼdiso mwako,’ pamene nthawi zonse chimtengo uli nacho mʼdiso mwako? Wachiphamaso iwe! Yamba wachotsa chimtengo chili mʼdiso mwako ndipo pamenepo udzatha kuona bwino ndi kuchotsa kachitsotso kali mʼdiso mwa mʼbale wako.

“Musapatse agalu zinthu zopatulika; kapena musaponyere nkhumba ngale zanu. Pakuti ngati mutero, zidzaziponda ndipo pomwepo zidzakutembenukirani ndi kukudulani nthulinthuli.

Pemphani, Funafunani, Gogodani

“Pemphani ndipo mudzapatsidwa; funafunani ndipo mudzapeza; gogodani ndipo adzakutsekulirani. Pakuti wopempha aliyense amalandira; ndi wofuna amapeza; ndipo iye amene agogoda, adzamutsekulira.

“Ndani mwa inu, mwana wake akamupempha buledi amamupatsa mwala? 10 Kapena ngati mwana apempha nsomba, kodi amamupatsa njoka? 11 Tsono ngati inu woyipitsitsa mumadziwa kupatsa ana anu mphatso zabwino, nanga Atate anu akumwamba sadzapereka mphatso zabwino kwa iwo amene amupempha? 12 Nʼchifukwa chake zinthu zilizonse mukafuna kuti anthu akuchitireni, yambani ndinu kuwachitira, pakuti izi ndi zimene malamulo ndi aneneri amaphunzitsa.

Zipata Ziwiri ndi Njira Ziwiri

13 “Lowani pa chipata chopapatiza. Pakuti chipata cholowera kuchiwonongeko nʼchachikulu ndipo msewu wake ndi waukulunso. Ndipo anthu ambiri amalowera pamenepo. 14 Koma chipata ndi chopapatiza ndi msewu ndi waungʼono umene utsogolera anthu ku moyo wosatha ndipo ndi owerengeka okha amene ayipeza njirayo.

Aneneri Owona ndi Onyenga

15 “Chenjerani nawo aneneri onyenga. Amabwera kwa inu atavala zikopa zankhosa, koma mʼkati mwawo ali mimbulu yolusa. 16 Mudzawazindikira iwo ndi zipatso zawo. Kodi anthu amathyola mpesa pa mtengo wa minga, kapena nkhuyu pa nthula? 17 Chimodzimodzinso mtengo wabwino umabala chipatso chabwino, koma mtengo woyipa umabala chipatso choyipa. 18 Mtengo wabwino sungabale chipatso choyipa, ndi mtengo woyipa sungabale chipatso chabwino. 19 Mtengo uliwonse umene subala chipatso chabwino umadulidwa ndi kuponyedwa pa moto. 20 Momwemonso, ndi zipatso zawo iwo mudzawazindikira.

Ophunzira Owona ndi Onyenga

21 “Si munthu aliyense amene amanena kwa Ine, ‘Ambuye, Ambuye,’ adzalowe mu ufumu wakumwamba, koma ndi yekhayo amene amachita chifuniro cha Atate anga amene ali kumwamba. 22 Ambiri adzati kwa Ine pa tsikulo, ‘Ambuye, Ambuye, kodi sitinkanenera mʼdzina lanu ndi mʼdzina lanunso tinkatulutsa ziwanda ndi kuchita zodabwitsa zambiri?’ 23 Pamenepo ndidzawawuza momveka bwino kuti, ‘Sindinakudziweni inu. Chokani kwa Ine, inu ochita zoyipa!’

Womanga Nyumba Wanzeru ndi Wopusa

24 “Nʼchifukwa chake aliyense amene amva mawu anga ndi kuwachita akufanana ndi munthu wanzeru amene anamanga nyumba yake pa thanthwe. 25 Mvula inagwa, mitsinje inadzaza, ndi mphepo zinawomba pa nyumbayo; koma sinagwe, chifukwa maziko ake anali pa thanthwe. 26 Koma aliyense amene amva mawu angawa ndi kusawachita ali ngati munthu wopusa amene anamanga nyumba yake pa mchenga. 27 Mvula inagwa, mitsinje inadzaza, ndi mphepo zinawomba pa nyumbayo, ndipo inagwa ndipo kugwa kwake kunali kwakukulu.”

28 Yesu atamaliza kunena zonsezi, magulu a anthu anadabwa ndi chiphunzitso chake, 29 chifukwa anaphunzitsa ngati amene anali ndi ulamuliro osati ngati aphunzitsi amalamulo.

Do Not Judge(A)

“Judge[a] (B)not, that you be not judged. For with what [b]judgment you judge, you will be judged; (C)and with the measure you use, it will be measured back to you. (D)And why do you look at the speck in your brother’s eye, but do not consider the plank in your own eye? Or how can you say to your brother, ‘Let me remove the speck from your eye’; and look, a plank is in your own eye? Hypocrite! First remove the plank from your own eye, and then you will see clearly to remove the speck from your brother’s eye.

(E)“Do not give what is holy to the dogs; nor cast your pearls before swine, lest they trample them under their feet, and turn and tear you in pieces.

Keep Asking, Seeking, Knocking(F)

(G)“Ask, and it will be given to you; seek, and you will find; knock, and it will be opened to you. For (H)everyone who asks receives, and he who seeks finds, and to him who knocks it will be opened. (I)Or what man is there among you who, if his son asks for bread, will give him a stone? 10 Or if he asks for a fish, will he give him a serpent? 11 If you then, (J)being evil, know how to give good gifts to your children, how much more will your Father who is in heaven give good things to those who ask Him! 12 Therefore, (K)whatever you want men to do to you, do also to them, for (L)this is the Law and the Prophets.

The Narrow Way(M)

13 (N)“Enter by the narrow gate; for wide is the gate and broad is the way that leads to destruction, and there are many who go in by it. 14 [c]Because narrow is the gate and [d]difficult is the way which leads to life, and there are few who find it.

You Will Know Them by Their Fruits(O)

15 (P)“Beware of false prophets, (Q)who come to you in sheep’s clothing, but inwardly they are ravenous wolves. 16 (R)You will know them by their fruits. (S)Do men gather grapes from thornbushes or figs from thistles? 17 Even so, (T)every good tree bears good fruit, but a bad tree bears bad fruit. 18 A good tree cannot bear bad fruit, nor can a bad tree bear good fruit. 19 (U)Every tree that does not bear good fruit is cut down and thrown into the fire. 20 Therefore by their fruits you will know them.

I Never Knew You(V)

21 “Not everyone who says to Me, (W)‘Lord, Lord,’ shall enter the kingdom of heaven, but he who (X)does the will of My Father in heaven. 22 Many will say to Me in that day, ‘Lord, Lord, have we (Y)not prophesied in Your name, cast out demons in Your name, and done many wonders in Your name?’ 23 And (Z)then I will declare to them, ‘I never knew you; (AA)depart from Me, you who practice lawlessness!’

Build on the Rock(AB)

24 “Therefore (AC)whoever hears these sayings of Mine, and does them, I will liken him to a wise man who built his house on the rock: 25 and the rain descended, the floods came, and the winds blew and beat on that house; and it did not fall, for it was founded on the rock.

26 “But everyone who hears these sayings of Mine, and does not do them, will be like a foolish man who built his house on the sand: 27 and the rain descended, the floods came, and the winds blew and beat on that house; and it fell. And great was its fall.”

28 And so it was, when Jesus had ended these sayings, that (AD)the people were astonished at His teaching, 29 (AE)for He taught them as one having authority, and not as the scribes.

Footnotes

  1. Matthew 7:1 Condemn
  2. Matthew 7:2 Condemnation
  3. Matthew 7:14 NU, M How narrow . . . !
  4. Matthew 7:14 confined

Не съдете другите

(Лк. 6:37-38,41-42)

Не съдете и няма да бъдете съдени. Защото както съдите вие, така ще съдят и вас. Каквато мярка използвате за другите, такава ще бъде използвана и за вас.

Защо забелязваш тресчицата в окото на брат си, а не обръщаш внимание на гредата в своето око? Как можеш да кажеш на брат си: „Нека да извадя тресчицата от окото ти“, когато в собственото ти око има греда? Лицемерецо, първо изкарай гредата от своето око. Тогава ще виждаш ясно, за да извадиш тресчицата от окото на брат си.

Не давайте на кучетата това, което е свято. Те само ще се обърнат и ще ви разкъсат. Не хвърляйте перлите си пред свинете. Те само ще ги стъпчат с краката си.

Молете Бога за всичко, от което имате нужда

(Лк. 11:9-13)

Искайте и ще ви се даде. Търсете и ще намерите. Хлопайте и ще ви бъде отворено. Понеже всеки, който иска, получава; който търси, намира; на който хлопа, му отварят.

Кой от вас би дал на детето си камък, ако то поиска хляб? 10 И ако поиска риба, няма да му дадете змия, нали? 11 Щом вие, въпреки че сте зли, знаете как да давате добри дарове на децата си, то колко повече вашият Баща в небесата ще даде добри неща на онези, които поискат от него!

Важно правило

12 Затова, постъпвайте с другите така, както искате те да постъпват с вас. Това е същността на Моисеевия закон и писанията на пророците.

Пътят към небето и пътят към ада

(Лк. 13:24)

13 Влезте през тясната порта, защото широка е портата и просторен — пътят, който води към гибел, и много са хората, които вървят по него. 14 Но колко тясна е портата и стеснен — пътят, който води към живот, и малко са хората, които го намират.

Дървото се познава по плода

(Лк. 6:43-44)

15 Пазете се от лъжепророците! Те идват при вас преоблечени като овчици, но отвътре са свирепи вълци. 16 По плодовете им ще ги разпознаете. Човек не бере грозде от тръни или смокини от репеи, нали? 17 По същия начин, всяко добро дърво ражда добри плодове, а лошото дърво ражда лоши плодове. 18 Едно добро дърво не може да даде лоши плодове, нито едно лошо дърво може да даде добри плодове. 19 Всяко дърво, което не ражда добри плодове, се отсича и се хвърля в огъня. 20 Така че, ще разпознаете лъжепророците по плодовете им.

Никога не съм ви познавал

(Лк. 13:25-27)

21 Не всеки, който ми казва „Господи, Господи“, ще влезе в небесното царство. Там ще влезе само този, който върши волята на моя Баща в небесата. 22 Много хора ще ми кажат в онзи Ден: „Господи, Господи, нима не в твоето име пророкувахме? Нима не в твоето име прогонвахме демони? Нима не в твоето име направихме много чудеса?“ 23 Тогава открито ще им заявя: „Никога не съм ви познавал. Махнете се от мен вие, които не зачитате Божия закон!“

Два вида хора

(Лк. 6:47-49)

24 Всеки, който чува тези мои думи и им се подчинява, е като благоразумния човек, който построил къщата си върху скала. 25 Дъждът завалял и реките придошли; ветровете задухали и заблъскали по тази къща. Но тя не се срутила, защото основата й била върху скала. 26 Обаче всеки, който чува тези мои думи и не им се подчинява, е като глупавия човек, който построил къщата си върху пясък. 27 Дъждът завалял и реките придошли; ветровете задухали и заблъскали по тази къща и тя се срутила с голям грохот.“

28 Когато Исус престана да говори, хората бяха удивени от учението му, 29 защото той ги поучаваше не като техните законоучители, а като някой, който има власт.