Add parallel Print Page Options

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.

14 Chitsiru chimati mu mtima mwake,
    “Kulibe Mulungu.”
Oterewa ndi oyipa ndipo ntchito zawo ndi zonyansa;
    palibe amene amachita zabwino.

Yehova kumwamba wayangʼana pansi,
    kuyangʼana anthu onse
kuti aone ngati alipo wina wanzeru,
    amene amafunafuna Mulungu.
Onse atembenukira kumbali,
    onse pamodzi asanduka oyipa;
palibe amene amachita zabwino,
    palibiretu ndi mmodzi yemwe.

Kodi anthu ochita zoyipawa sadziwa chilichonse?
    Akudya anthu anga ngati chakudya chawo
    ndipo satamanda Yehova?
Awo ali apowo, agwidwa ndi mantha aakulu,
    pakuti Mulungu ali mʼgulu la olungama.
Inu ochita zoyipa mumalepheretsa chikonzero cha anthu osauka,
    koma Yehova ndiye pothawirapo pawo.

Ndithu, chipulumutso cha Israeli chidzachokera ku Ziyoni!
    Pamene Yehova abwezeretsa ufulu wa anthu ake,
    Yakobo akondwere ndipo Israeli asangalale!

人之愚頑及罪惡

14 大衛的詩,交於伶長。

愚頑人心裡說:「沒有神!」他們都是邪惡,行了可憎惡的事,沒有一個人行善。
耶和華從天上垂看世人,要看有明白的沒有,有尋求神的沒有。
他們都偏離正路,一同變為汙穢;並沒有行善的,連一個也沒有。
作孽的都沒有知識嗎?他們吞吃我的百姓,如同吃飯一樣,並不求告耶和華。
他們在那裡大大地害怕,因為神在義人的族類中。
你們叫困苦人的謀算變為羞辱,然而耶和華是他的避難所。
但願以色列的救恩從錫安而出!耶和華救回他被擄的子民,那時雅各要快樂,以色列要歡喜。

世人的邪恶

大卫的诗,交给乐长。

14 愚昧人心里想:“没有上帝。”
他们全然败坏,行为邪恶,
无人行善。
耶和华从天上俯视人间,
看有没有明智者,
有没有寻求上帝的人。
人们都偏离正路,
一同堕落;
没有人行善,
一个也没有!
恶人吞吃我的百姓如同吃饭,
他们不求告耶和华。
难道他们无知吗?
但他们终必充满恐惧,
因为上帝站在义人当中。
你们恶人使困苦人的计划落空,
但耶和华是他们的避难所。
愿以色列的拯救来自锡安!
耶和华救回祂被掳的子民时,
雅各要欢欣,以色列要快乐。

世人的邪惡

大衛的詩,交給樂長。

14 愚昧人心裡想:「沒有上帝。」
他們全然敗壞,行為邪惡,
無人行善。
耶和華從天上俯視人間,
看有沒有明智者,
有沒有尋求上帝的人。
人們都偏離正路,
一同墮落;
沒有人行善,
一個也沒有!
惡人吞吃我的百姓如同吃飯,
他們不求告耶和華。
難道他們無知嗎?
但他們終必充滿恐懼,
因為上帝站在義人當中。
你們惡人使困苦人的計劃落空,
但耶和華是他們的避難所。
願以色列的拯救來自錫安!
耶和華救回祂被擄的子民時,
雅各要歡欣,以色列要快樂。