Add parallel Print Page Options

Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

133 Onani, nʼkokoma ndi kokondweretsa ndithu
    pamene abale akhala pamodzi mwachiyanjano!
Zili ngati mafuta amtengowapatali othiridwa pa mutu,
    otsikira ku ndevu,
ku ndevu za Aaroni,
    oyenderera mpaka mʼkhosi mwa mkanjo wake.
Zili ngati mame a ku Heremoni
    otsikira pa Phiri la Ziyoni.
Pakuti pamenepo Yehova amaperekapo dalitso,
    ndiwo moyo wamuyaya.

Psalm 133

A song of ascents. Of David.

How good and pleasant it is
    when God’s people live together(A) in unity!(B)

It is like precious oil poured on the head,(C)
    running down on the beard,
running down on Aaron’s beard,
    down on the collar of his robe.
It is as if the dew(D) of Hermon(E)
    were falling on Mount Zion.(F)
For there the Lord bestows his blessing,(G)
    even life forevermore.(H)