Masalimo 13
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.
13 Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale?
Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?
2 Ndidzalimbana ndi maganizo anga
ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti?
Mpaka liti adani anga adzandipambana?
3 Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga.
Walitsani maso anga kuti ndingafe;
4 mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,”
ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.
5 Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika;
mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.
6 Ine ndidzayimbira Yehova
pakuti wandichitira zokoma.
Psalm 13
New King James Version
Trust in the Salvation of the Lord
To the Chief Musician. A Psalm of David.
13 How long, O Lord? Will You forget me forever?
(A)How long will You hide Your face from me?
2 How long shall I take counsel in my soul,
Having sorrow in my heart daily?
How long will my enemy be exalted over me?
3 Consider and hear me, O Lord my God;
(B)Enlighten my eyes,
(C)Lest I sleep the sleep of death;
4 Lest my enemy say,
“I have prevailed against him”;
Lest those who trouble me rejoice when I am moved.
5 But I have trusted in Your mercy;
My heart shall rejoice in Your salvation.
6 I will sing to the Lord,
Because He has dealt bountifully with me.
Psalm 13
King James Version
13 How long wilt thou forget me, O Lord? for ever? how long wilt thou hide thy face from me?
2 How long shall I take counsel in my soul, having sorrow in my heart daily? how long shall mine enemy be exalted over me?
3 Consider and hear me, O Lord my God: lighten mine eyes, lest I sleep the sleep of death;
4 Lest mine enemy say, I have prevailed against him; and those that trouble me rejoice when I am moved.
5 But I have trusted in thy mercy; my heart shall rejoice in thy salvation.
6 I will sing unto the Lord, because he hath dealt bountifully with me.
Psalm 13
English Standard Version
How Long, O Lord?
To the choirmaster. A Psalm of David.
13 (A)How long, O Lord? Will you (B)forget me forever?
How long will you (C)hide your face from me?
2 How long must I take (D)counsel in my soul
and have sorrow in my heart all the day?
How long shall my enemy be exalted over me?
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Scripture taken from the New King James Version®. Copyright © 1982 by Thomas Nelson. Used by permission. All rights reserved.
The ESV® Bible (The Holy Bible, English Standard Version®), © 2001 by Crossway, a publishing ministry of Good News Publishers. ESV Text Edition: 2025.

