Add parallel Print Page Options

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

128 Odala ndi onse amene amaopa Yehova,
    amene amayenda mʼnjira zake.
Udzadya chipatso cha ntchito yako;
    madalitso ndi chuma zidzakhala zako.
Mkazi wako adzakhala ngati mpesa wobereka
    mʼkati mwa nyumba yako;
ana ako adzakhala ngati mphukira za mitengo ya olivi
    kuzungulira tebulo lako.
Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa
    amene amaopa Yehova.

Yehova akudalitse kuchokera mʼZiyoni
    masiku onse a moyo wako;
uwone zokoma za Yerusalemu,
    ndipo ukhale ndi moyo kuti udzaone zidzukulu zako.

Mtendere ukhale ndi Israeli.

Psalm 128

A song of ascents.

Blessed are all who fear the Lord,(A)
    who walk in obedience to him.(B)
You will eat the fruit of your labor;(C)
    blessings and prosperity(D) will be yours.
Your wife will be like a fruitful vine(E)
    within your house;
your children(F) will be like olive shoots(G)
    around your table.
Yes, this will be the blessing(H)
    for the man who fears the Lord.(I)

May the Lord bless you from Zion;(J)
    may you see the prosperity of Jerusalem(K)
    all the days of your life.
May you live to see your children’s children—(L)
    peace be on Israel.(M)

128 Blessed is every one that feareth the Lord; that walketh in his ways.

For thou shalt eat the labour of thine hands: happy shalt thou be, and it shall be well with thee.

Thy wife shall be as a fruitful vine by the sides of thine house: thy children like olive plants round about thy table.

Behold, that thus shall the man be blessed that feareth the Lord.

The Lord shall bless thee out of Zion: and thou shalt see the good of Jerusalem all the days of thy life.

Yea, thou shalt see thy children's children, and peace upon Israel.