Add parallel Print Page Options

112 Tamandani Yehova.

Wodala munthu amene amaopa Yehova,
    amene amakondwera kwambiri ndi malamulo ake.

Ana ake adzakhala amphamvu mʼdziko;
    mʼbado wa olungama mtima udzadalitsidwa.
Kulemera ndi chuma zili mʼnyumba yake,
    ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
Ngakhale mu mdima kuwala kumatulukira olungama mtima;
    wokoma mtima, wachifundo ndi wowongoka mtima.
Zinthu zabwino zidzabwera kwa iye amene amapereka mowolowamanja ndi wokongoletsa mwaufulu,
    amene amachita ntchito yake mwachilungamo.

Ndithu sadzagwedezeka;
    munthu wolungama sadzayiwalika mpaka muyaya.
Saopa akamva zoyipa zimene zachitika;
    mtima wake ndi wokhazikika ndipo amadalira Yehova.
Mtima wake ndi wotetezedwa, sadzakhala ndi mantha;
    potsiriza pake adzayangʼana adani ake mwachipambano.
Wopereka mphatso zake mowolowamanja kwa osauka,
    chilungamo chake chimanka mpaka muyaya;
    nyanga yake idzakwezedwa mwaulemu.

10 Munthu woyipa adzaona zimenezi ndipo adzapsa mtima;
    adzakukuta mano ake ndipo adzasungunuka.
    Zolakalaka za anthu oyipa sizidzachitika konse.

Psalm 112[a]

Praise the Lord.[b](A)

Blessed are those(B) who fear the Lord,(C)
    who find great delight(D) in his commands.

Their children(E) will be mighty in the land;
    the generation of the upright will be blessed.
Wealth and riches(F) are in their houses,
    and their righteousness endures(G) forever.
Even in darkness light dawns(H) for the upright,
    for those who are gracious and compassionate and righteous.(I)
Good will come to those who are generous and lend freely,(J)
    who conduct their affairs with justice.

Surely the righteous will never be shaken;(K)
    they will be remembered(L) forever.
They will have no fear of bad news;
    their hearts are steadfast,(M) trusting in the Lord.(N)
Their hearts are secure, they will have no fear;(O)
    in the end they will look in triumph on their foes.(P)
They have freely scattered their gifts to the poor,(Q)
    their righteousness endures(R) forever;
    their horn[c] will be lifted(S) high in honor.

10 The wicked will see(T) and be vexed,
    they will gnash their teeth(U) and waste away;(V)
    the longings of the wicked will come to nothing.(W)

Footnotes

  1. Psalm 112:1 This psalm is an acrostic poem, the lines of which begin with the successive letters of the Hebrew alphabet.
  2. Psalm 112:1 Hebrew Hallelu Yah
  3. Psalm 112:9 Horn here symbolizes dignity.