Masalimo 111
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
111 Tamandani Yehova.
Ndidzathokoza Yehova ndi mtima wanga wonse
mʼbwalo la anthu olungama mtima ndi pa msonkhano.
2 Ntchito za Yehova nʼzazikulu;
onse amene amakondwera nazo amazilingalira.
3 Zochita zake ndi za ulemerero ndi zaufumu,
ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
4 Iye wachititsa kuti zodabwitsa zake zikumbukirike;
Yehova ndi wokoma mtima ndi wachifundo.
5 Amapereka chakudya kwa amene amamuopa Iye;
amakumbukira pangano lake kwamuyaya.
6 Waonetsa anthu ake mphamvu ya ntchito zake,
kuwapatsa mayiko a anthu a mitundu ina.
7 Ntchito za manja ake ndi zokhulupirika ndi zolungama;
malangizo ake onse ndi odalirika.
8 Malamulo ndi okhazikika ku nthawi za nthawi,
ochitidwa mokhulupirika ndi molungama.
9 Iyeyo amawombola anthu ake;
anakhazikitsa pangano lake kwamuyaya
dzina lake ndi loyera ndi loopsa.
10 Kuopa Yehova ndicho chiyambi cha nzeru;
onse amene amatsatira malangizo ake amamvetsa bwino zinthu.
Iye ndi wotamandika mpaka muyaya.
Psalm 111
New International Version
Psalm 111[a]
1 Praise the Lord.[b]
I will extol the Lord(A) with all my heart(B)
in the council(C) of the upright and in the assembly.(D)
2 Great are the works(E) of the Lord;
they are pondered by all(F) who delight in them.
3 Glorious and majestic are his deeds,
and his righteousness endures(G) forever.
4 He has caused his wonders to be remembered;
the Lord is gracious and compassionate.(H)
5 He provides food(I) for those who fear him;(J)
he remembers his covenant(K) forever.
6 He has shown his people the power of his works,(L)
giving them the lands of other nations.(M)
7 The works of his hands(N) are faithful and just;
all his precepts are trustworthy.(O)
8 They are established for ever(P) and ever,
enacted in faithfulness and uprightness.
9 He provided redemption(Q) for his people;
he ordained his covenant forever—
holy and awesome(R) is his name.
Footnotes
- Psalm 111:1 This psalm is an acrostic poem, the lines of which begin with the successive letters of the Hebrew alphabet.
- Psalm 111:1 Hebrew Hallelu Yah
Psalm 111
King James Version
111 Praise ye the Lord. I will praise the Lord with my whole heart, in the assembly of the upright, and in the congregation.
2 The works of the Lord are great, sought out of all them that have pleasure therein.
3 His work is honourable and glorious: and his righteousness endureth for ever.
4 He hath made his wonderful works to be remembered: the Lord is gracious and full of compassion.
5 He hath given meat unto them that fear him: he will ever be mindful of his covenant.
6 He hath shewed his people the power of his works, that he may give them the heritage of the heathen.
7 The works of his hands are verity and judgment; all his commandments are sure.
8 They stand fast for ever and ever, and are done in truth and uprightness.
9 He sent redemption unto his people: he hath commanded his covenant for ever: holy and reverend is his name.
10 The fear of the Lord is the beginning of wisdom: a good understanding have all they that do his commandments: his praise endureth for ever.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.