Add parallel Print Page Options

111 Tamandani Yehova.

Ndidzathokoza Yehova ndi mtima wanga wonse
    mʼbwalo la anthu olungama mtima ndi pa msonkhano.

Ntchito za Yehova nʼzazikulu;
    onse amene amakondwera nazo amazilingalira.
Zochita zake ndi za ulemerero ndi zaufumu,
    ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
Iye wachititsa kuti zodabwitsa zake zikumbukirike;
    Yehova ndi wokoma mtima ndi wachifundo.
Amapereka chakudya kwa amene amamuopa Iye;
    amakumbukira pangano lake kwamuyaya.
Waonetsa anthu ake mphamvu ya ntchito zake,
    kuwapatsa mayiko a anthu a mitundu ina.
Ntchito za manja ake ndi zokhulupirika ndi zolungama;
    malangizo ake onse ndi odalirika.
Malamulo ndi okhazikika ku nthawi za nthawi,
    ochitidwa mokhulupirika ndi molungama.
Iyeyo amawombola anthu ake;
    anakhazikitsa pangano lake kwamuyaya
    dzina lake ndi loyera ndi loopsa.

10 Kuopa Yehova ndicho chiyambi cha nzeru;
    onse amene amatsatira malangizo ake amamvetsa bwino zinthu.
    Iye ndi wotamandika mpaka muyaya.

Psalm 111[a]

Praise the Lord.[b]

I will extol the Lord(A) with all my heart(B)
    in the council(C) of the upright and in the assembly.(D)

Great are the works(E) of the Lord;
    they are pondered by all(F) who delight in them.
Glorious and majestic are his deeds,
    and his righteousness endures(G) forever.
He has caused his wonders to be remembered;
    the Lord is gracious and compassionate.(H)
He provides food(I) for those who fear him;(J)
    he remembers his covenant(K) forever.

He has shown his people the power of his works,(L)
    giving them the lands of other nations.(M)
The works of his hands(N) are faithful and just;
    all his precepts are trustworthy.(O)
They are established for ever(P) and ever,
    enacted in faithfulness and uprightness.
He provided redemption(Q) for his people;
    he ordained his covenant forever—
    holy and awesome(R) is his name.

10 The fear of the Lord(S) is the beginning of wisdom;(T)
    all who follow his precepts have good understanding.(U)
    To him belongs eternal praise.(V)

Footnotes

  1. Psalm 111:1 This psalm is an acrostic poem, the lines of which begin with the successive letters of the Hebrew alphabet.
  2. Psalm 111:1 Hebrew Hallelu Yah

111 Praise ye the Lord. I will praise the Lord with my whole heart, in the assembly of the upright, and in the congregation.

The works of the Lord are great, sought out of all them that have pleasure therein.

His work is honourable and glorious: and his righteousness endureth for ever.

He hath made his wonderful works to be remembered: the Lord is gracious and full of compassion.

He hath given meat unto them that fear him: he will ever be mindful of his covenant.

He hath shewed his people the power of his works, that he may give them the heritage of the heathen.

The works of his hands are verity and judgment; all his commandments are sure.

They stand fast for ever and ever, and are done in truth and uprightness.

He sent redemption unto his people: he hath commanded his covenant for ever: holy and reverend is his name.

10 The fear of the Lord is the beginning of wisdom: a good understanding have all they that do his commandments: his praise endureth for ever.