Add parallel Print Page Options

Salimo la Davide.

103 Tamanda Yehova, iwe moyo wanga;
    ndi zonse zamʼkati mwanga zitamande dzina lake loyera.
Tamanda Yehova, iwe moyo wanga,
    ndipo usayiwale zabwino zake zonse.
Amene amakhululuka machimo ako onse
    ndi kuchiritsa nthenda zako zonse,
amene awombola moyo wako ku dzenje
    ndi kukuveka chikondi ndi chifundo chake ngati chipewa chaufumu,
amene akwaniritsa zokhumba zako ndi zinthu zabwino,
    kotero kuti umakhala wamphamvu zatsopano ngati mphungu.

Yehova amachita chilungamo
    ndipo amaweruza molungama onse opsinjika.

Iye anadziwitsa Mose njira zake,
    ntchito zake kwa Aisraeli.
Yehova ndi wachifundo ndi wokoma mtima,
    wosakwiya msanga ndi wachikondi chochuluka.
Iye sadzatsutsa nthawi zonse,
    kapena kusunga mkwiyo wake kwamuyaya;
10 satichitira molingana ndi machimo athu,
    kapena kutibwezera molingana ndi mphulupulu zathu.
11 Pakuti monga kumwamba kuli kutali ndi dziko lapansi,
    koteronso chikondi chake nʼchachikulu kwa iwo amene amamuopa;
12 monga kummawa kutalikirana ndi kumadzulo,
    koteronso Iye watichotsera mphulupulu zathu kuti zikhale kutali nafe.
13 Monga bambo amachitira chifundo ana ake,
    choncho Yehova ali ndi chifundo ndi iwo amene amamuopa;
14 pakuti Iye amadziwa momwe tinawumbidwira,
    amakumbukira kuti ndife fumbi.
15 Kunena za munthu, masiku ake ali ngati udzu,
    amaphuka ngati duwa la mʼmunda;
16 koma mphepo imawombapo ndipo silionekanso
    ndipo malo ake sakumbukirikanso.
17 Koma kuchokera muyaya mpaka muyaya
    chikondi cha Yehova chili ndi iwo amene amamuopa,
    ndi chilungamo chake chili ndi ana a ana awo;
18 iwo amene amasunga pangano lake
    ndi kukumbukira kumvera malangizo ake.

19 Yehova wakhazikitsa mpando wake waufumu mmwamba
    ndipo ufumu wake umalamulira onse.

20 Tamandani Yehova, inu angelo ake,
    amphamvu inu amene mumachita zimene amalamula,
    amene mumamvera mawu ake.
21 Tamandani Yehova, zolengedwa zonse zakumwamba,
    inu atumiki ake amene mumachita chifuniro chake.
22 Tamandani Yehova, ntchito yake yonse
    kulikonse mu ulamuliro wake.

Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.

Psalm 103

Of David.

Praise the Lord,(A) my soul;(B)
    all my inmost being, praise his holy name.(C)
Praise the Lord,(D) my soul,
    and forget not(E) all his benefits—
who forgives all your sins(F)
    and heals(G) all your diseases,
who redeems your life(H) from the pit
    and crowns you with love and compassion,(I)
who satisfies(J) your desires with good things
    so that your youth is renewed(K) like the eagle’s.(L)

The Lord works righteousness(M)
    and justice for all the oppressed.(N)

He made known(O) his ways(P) to Moses,
    his deeds(Q) to the people of Israel:
The Lord is compassionate and gracious,(R)
    slow to anger, abounding in love.
He will not always accuse,
    nor will he harbor his anger forever;(S)
10 he does not treat us as our sins deserve(T)
    or repay us according to our iniquities.
11 For as high as the heavens are above the earth,
    so great is his love(U) for those who fear him;(V)
12 as far as the east is from the west,
    so far has he removed our transgressions(W) from us.

13 As a father has compassion(X) on his children,
    so the Lord has compassion on those who fear him;
14 for he knows how we are formed,(Y)
    he remembers that we are dust.(Z)
15 The life of mortals is like grass,(AA)
    they flourish like a flower(AB) of the field;
16 the wind blows(AC) over it and it is gone,
    and its place(AD) remembers it no more.
17 But from everlasting to everlasting
    the Lord’s love is with those who fear him,
    and his righteousness with their children’s children(AE)
18 with those who keep his covenant(AF)
    and remember(AG) to obey his precepts.(AH)

19 The Lord has established his throne(AI) in heaven,
    and his kingdom rules(AJ) over all.

20 Praise the Lord,(AK) you his angels,(AL)
    you mighty ones(AM) who do his bidding,(AN)
    who obey his word.
21 Praise the Lord, all his heavenly hosts,(AO)
    you his servants(AP) who do his will.
22 Praise the Lord, all his works(AQ)
    everywhere in his dominion.

Praise the Lord, my soul.(AR)

103 Bless the Lord, O my soul: and all that is within me, bless his holy name.

Bless the Lord, O my soul, and forget not all his benefits:

Who forgiveth all thine iniquities; who healeth all thy diseases;

Who redeemeth thy life from destruction; who crowneth thee with lovingkindness and tender mercies;

Who satisfieth thy mouth with good things; so that thy youth is renewed like the eagle's.

The Lord executeth righteousness and judgment for all that are oppressed.

He made known his ways unto Moses, his acts unto the children of Israel.

The Lord is merciful and gracious, slow to anger, and plenteous in mercy.

He will not always chide: neither will he keep his anger for ever.

10 He hath not dealt with us after our sins; nor rewarded us according to our iniquities.

11 For as the heaven is high above the earth, so great is his mercy toward them that fear him.

12 As far as the east is from the west, so far hath he removed our transgressions from us.

13 Like as a father pitieth his children, so the Lord pitieth them that fear him.

14 For he knoweth our frame; he remembereth that we are dust.

15 As for man, his days are as grass: as a flower of the field, so he flourisheth.

16 For the wind passeth over it, and it is gone; and the place thereof shall know it no more.

17 But the mercy of the Lord is from everlasting to everlasting upon them that fear him, and his righteousness unto children's children;

18 To such as keep his covenant, and to those that remember his commandments to do them.

19 The Lord hath prepared his throne in the heavens; and his kingdom ruleth over all.

20 Bless the Lord, ye his angels, that excel in strength, that do his commandments, hearkening unto the voice of his word.

21 Bless ye the Lord, all ye his hosts; ye ministers of his, that do his pleasure.

22 Bless the Lord, all his works in all places of his dominion: bless the Lord, O my soul.