Add parallel Print Page Options

Nsembe Zopsereza

26 Yehova anayitana Mose mu tenti ya msonkhano. Iye anati, “Aliyense wa inu ngati abwera ndi nsembe kwa Yehova kuchokera pa ziweto zake, choperekacho chikhale ngʼombe, nkhosa kapena mbuzi.

“ ‘Ngati munthu apereka nsembe yopsereza ya ngʼombe, ikhale yayimuna yopanda chilema. Aziyipereka pa khomo la tenti ya msonkhano, kuti Yehova alandire. Munthuyo asanjike dzanja lake pa mutu pa nsembe yopserezayo, ndipo idzalandiridwa kuti ikhale yopepesera machimo ake. Pambuyo pake aphe ngʼombeyo pamaso pa Yehova, ndipo ansembe, ana a Aaroni, atenge magazi ake ndi kuwawaza mbali zonse za guwa lansembe limene lili pa khomo la tenti ya msonkhano. Munthuyo asende nsembe yopserezayo ndi kuyidula nthulinthuli. Ndipo ana a Aaroni, wansembe uja asonkhe moto pa guwa ndi kuyalapo nkhuni pa motopo. Kenaka ana a Aaroni, wansembe uja, ayike nthuli za nyamayo, mutu wake pamodzi ndi mafuta omwe pa nkhuni zimene zili paguwapo. Munthuyo atsuke zamʼkati mwa nyamayo pamodzi ndi miyendo yake yomwe, ndipo wansembe awotche nyama yonse paguwapo. Iyi ndi nsembe yopsereza, chopereka chowotcha pa moto, cha fungo lokomera Yehova.

10 “ ‘Koma ngati chopereka cha nsembe yopserezayo ndi nkhosa kapena mbuzi kuchokera pa ziweto zake, munthuyo apereke yayimuna yopanda chilema. 11 Ayiphere kumpoto kwa guwa, pamaso pa Yehova, ndipo ana a Aaroni amene ndi ansembe, awaze magazi ake mbali zonse za guwalo. 12 Kenaka ayidule nyamayo nthulinthuli, ndipo wansembe ayike nthulizo pa guwa, atengenso mutu ndi mafuta omwe, ndipo ayike zonsezi pa nkhuni zimene zikuyaka pa guwa. 13 Munthuyo atsuke zamʼkati mwa nyamayo pamodzi ndi miyendo yake yomwe, ndipo wansembe abwere nazo zonse ndi kuzitentha pa guwa. Iyi ndi nsembe yopsereza, chopereka chotentha pa moto, fungo lokomera Yehova.

14 “ ‘Koma ngati chopereka kwa Yehova ndi nsembe yopsereza ya mbalame, ndiye ikhale njiwa kapena mawunda. 15 Wansembe abwere nayo ku guwa, ayidule mutu moyipotola ndi kutentha mutuwo pa guwa. Magazi ake awathire pansi kuti ayenderere pambali pa guwa. 16 Iye achotse chithokomiro pamodzi ndi nthenga zake zomwe ndi kuzitaya ku malo wotayirako phulusa, kummawa kwa guwalo. 17 Kenaka ayingʼambe pakati, koma asachotse mapiko. Ndipo wansembe ayiwotche pa nkhuni zimene zikuyaka pa guwa. Imeneyi ndi nsembe yopsereza, yowotcha pa moto ndiponso ya fungo lokomera Yehova.

The Burnt Offering

The Lord called to Moses(A) and spoke to him from the tent of meeting.(B) He said, “Speak to the Israelites and say to them: ‘When anyone among you brings an offering to the Lord,(C) bring as your offering an animal from either the herd or the flock.(D)

“‘If the offering is a burnt offering(E) from the herd,(F) you are to offer a male without defect.(G) You must present it at the entrance to the tent(H) of meeting so that it will be acceptable(I) to the Lord. You are to lay your hand on the head(J) of the burnt offering,(K) and it will be accepted(L) on your behalf to make atonement(M) for you. You are to slaughter(N) the young bull(O) before the Lord, and then Aaron’s sons(P) the priests shall bring the blood and splash it against the sides of the altar(Q) at the entrance to the tent of meeting. You are to skin(R) the burnt offering and cut it into pieces.(S) The sons of Aaron the priest are to put fire on the altar and arrange wood(T) on the fire. Then Aaron’s sons the priests shall arrange the pieces, including the head and the fat,(U) on the wood(V) that is burning on the altar. You are to wash the internal organs and the legs with water,(W) and the priest is to burn all of it(X) on the altar.(Y) It is a burnt offering,(Z) a food offering,(AA) an aroma pleasing to the Lord.(AB)

10 “‘If the offering is a burnt offering from the flock, from either the sheep(AC) or the goats,(AD) you are to offer a male without defect. 11 You are to slaughter it at the north side of the altar(AE) before the Lord, and Aaron’s sons the priests shall splash its blood against the sides of the altar.(AF) 12 You are to cut it into pieces, and the priest shall arrange them, including the head and the fat,(AG) on the wood that is burning on the altar. 13 You are to wash the internal organs and the legs with water,(AH) and the priest is to bring all of them and burn them(AI) on the altar.(AJ) It is a burnt offering,(AK) a food offering, an aroma pleasing to the Lord.

14 “‘If the offering to the Lord is a burnt offering of birds, you are to offer a dove or a young pigeon.(AL) 15 The priest shall bring it to the altar, wring off the head(AM) and burn it on the altar; its blood shall be drained out on the side of the altar.(AN) 16 He is to remove the crop and the feathers[a] and throw them down east of the altar where the ashes(AO) are. 17 He shall tear it open by the wings, not dividing it completely,(AP) and then the priest shall burn it on the wood(AQ) that is burning on the altar. It is a burnt offering, a food offering, an aroma pleasing to the Lord.

Footnotes

  1. Leviticus 1:16 Or crop with its contents; the meaning of the Hebrew for this word is uncertain.