Font Size
Yobu 4:8
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Yobu 4:8
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
8 Monga ndaonera ine, anthu amene amatipula zoyipa,
ndi iwo amene amadzala mavuto, amakolola zomwezo.
Yobu 20:11
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Yobu 20:11
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
11 Mphamvu zaunyamata zimene zili mʼthupi mwake
zidzagona naye limodzi mʼfumbi.
Miyambo 1:31
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Miyambo 1:31
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
31 Tsono adzadya zipatso zoyenera mayendedwe awo
ndi kukhuta ndi ntchito zimene anachita kwa ena.
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (CCL)
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.