“My troubled thoughts prompt me to answer
    because I am greatly disturbed.(A)
I hear a rebuke(B) that dishonors me,
    and my understanding inspires me to reply.

“Surely you know how it has been from of old,(C)
    ever since mankind[a] was placed on the earth,

Read full chapter

Footnotes

  1. Job 20:4 Or Adam

“Therefore my anxious thoughts make me answer,
Because of the turmoil within me.
I have heard the rebuke [a]that reproaches me,
And the spirit of my understanding causes me to answer.

“Do you not know this of (A)old,
Since man was placed on earth,

Read full chapter

Footnotes

  1. Job 20:3 Lit. of my insulting correction

“Kuvutika kwa mʼmaganizo kwanga kwandifulumiza kuti ndiyankhe
    chifukwa ndasautsidwa kwambiri.
Ndikumva kudzudzula kondinyoza,
    ndipo kumvetsetsa kwanga kwa zinthu kwandifulumiza kuti ndiyankhe.

“Ndithudi iwe ukudziwa momwe zinthu zakhala zikuchitikira kuyambira kale,
    kuchoka nthawi imene munthu analengedwa pa dziko lapansi,

Read full chapter