Add parallel Print Page Options

Ine ndine Yehova ndipo palibenso wina;
    kupatula Ine palibenso Mulungu wina.
Ndidzakupatsa mphamvu,
    ngakhale sukundidziwa Ine,
kotero kuti kuchokera kummawa mpaka kumadzulo
    anthu adzadziwa kuti palibe wina koma Ine ndekha.
Ine ndine Yehova,
    ndipo palibenso wina.
Ndimalenga kuwala ndi mdima,
    ndimabweretsa madalitso ndi tsoka;
    ndine Yehova, amene ndimachita zonsezi.

Read full chapter

I am the Lord, and there is no other;(A)
    apart from me there is no God.(B)
I will strengthen you,(C)
    though you have not acknowledged me,
so that from the rising of the sun
    to the place of its setting(D)
people may know(E) there is none besides me.(F)
    I am the Lord, and there is no other.
I form the light and create darkness,(G)
    I bring prosperity and create disaster;(H)
    I, the Lord, do all these things.

Read full chapter