Yesaya 45:5-7
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
5 Ine ndine Yehova ndipo palibenso wina;
kupatula Ine palibenso Mulungu wina.
Ndidzakupatsa mphamvu,
ngakhale sukundidziwa Ine,
6 kotero kuti kuchokera kummawa mpaka kumadzulo
anthu adzadziwa kuti palibe wina koma Ine ndekha.
Ine ndine Yehova,
ndipo palibenso wina.
7 Ndimalenga kuwala ndi mdima,
ndimabweretsa madalitso ndi tsoka;
ndine Yehova, amene ndimachita zonsezi.
Isaiah 45:5-7
New International Version
5 I am the Lord, and there is no other;(A)
apart from me there is no God.(B)
I will strengthen you,(C)
though you have not acknowledged me,
6 so that from the rising of the sun
to the place of its setting(D)
people may know(E) there is none besides me.(F)
I am the Lord, and there is no other.
7 I form the light and create darkness,(G)
I bring prosperity and create disaster;(H)
I, the Lord, do all these things.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.