Hoseya 10
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
10 Israeli anali mpesa wotambalala;
anabereka zipatso zambiri.
Pamene zipatso zawo zinanka zichuluka,
anawonjezera kumanga maguwa ansembe.
Pamene dziko lake linkatukuka,
anakongoletsa miyala yake yopatulika.
2 Mtima wawo ndi wonyenga
ndipo tsopano ayenera kulangidwa chifukwa cha kulakwa kwawo.
Yehova adzagumula maguwa awo ansembe
ndi kuwononga miyala yawo yopatulika.
3 Pamenepo anthuwo adzanena kuti, “Ife tilibe mfumu
chifukwa sitinaope Yehova.
Koma ngakhale tikanakhala ndi mfumu,
kodi mfumuyo ikanatichitira chiyani?”
4 Mafumu amalonjeza zambiri,
amalumbira zabodza
pochita mapangano.
Kotero maweruzo amaphuka
ngati zitsamba zakupha mʼmunda umene walimidwa.
5 Anthu amene amakhala mu Samariya akuchita mantha
chifukwa cha fano la mwana wangʼombe ku Beti-Aveni.
Anthu ake adzalirira fanolo,
chimodzimodzinso ansembe ake adamawo,
amene anakondwera ndi kukongola kwake,
chifukwa lachotsedwa pakati pawo ndi kupita ku ukapolo.
6 Fanolo lidzatengedwa kupita ku Asiriya
ngati mphatso kwa mfumu yayikulu.
Efereimu adzachititsidwa manyazi
chifukwa cha mafano ake amitengo.
7 Samariya ndi mfumu yake adzatengedwa kupita kutali
ngati kanthambi koyenda pa madzi.
8 Malo opembedzerako mafano a ku Aveni adzawonongedwa.
Ili ndiye tchimo la Israeli.
Minga ndi mitungwi zidzamera
ndi kuphimba maguwa awo ansembe.
Kenaka anthu adzawuza mapiri kuti, “Tiphimbeni!”
ndipo adzawuza zitunda kuti, “Tigwereni!”
9 “Iwe Israeli, wachimwa kuyambira mʼmasiku a Gibeya,
ndipo wakhala uli pomwepo.
Kodi nkhondo sinagonjetse anthu
ochita zoyipa ku Gibeya?
10 Pamene ndifunire, ndidzalanga anthuwo;
mitundu ya anthu idzasonkhanitsidwa kudzalimbana nawo,
kuwayika mʼndende chifukwa cha uchimo wawo waukulu.
11 Efereimu ndi mwana wangʼombe wamkazi wophunzitsidwa
amene amakonda kupuntha tirigu,
choncho Ine ndidzayika goli
mʼkhosi lake lokongolalo.
Ndidzasenzetsa Efereimu goli,
Yuda ayenera kulima,
ndipo Yakobo ayenera kutipula.
12 Mufese nokha chilungamo
ndipo mudzakolola chipatso cha chikondi changa chosasinthika.
Ndipo tipulani munda wanu wosalimidwawo;
pakuti ino ndi nthawi yofunafuna Yehova,
mpaka Iye atabwera
kudzakugwetserani mivumbi ya chilungamo.
13 Koma inu munadzala zolakwa,
mwakolola zoyipa;
mwadya chipatso cha chinyengo.
Chifukwa mumadalira mphamvu zanu
ndiponso ankhondo anu ochulukawo,
14 phokoso lankhondo lidzamveka pakati pa anthu anga
kotero kuti malinga anu onse adzawonongeka,
monga momwe Salimani anawonongera Beti-Aribeli pa nthawi ya nkhondo;
pamene anapha amayi pamodzi ndi ana awo omwe.
15 Momwemonso zidzakuchitikira, iwe Beteli
chifukwa kuyipa kwako ndi kwakukulu.
Tsiku limeneli likadzafika,
mfumu ya Israeli idzawonongedwa kwathunthu.
Oseas 10
Nueva Biblia de las Américas
10 Israel es un viñedo frondoso(A),
Dando fruto para sí mismo.
Según la abundancia de su fruto,
Así multiplicaba los altares(B);
Cuanto más rica era su tierra,
Más hermosos hacían sus pilares sagrados(C).
2 Su corazón es infiel(D);
Ahora serán hallados culpables(E);
El Señor derribará sus altares
Y destruirá sus pilares sagrados(F).
3 ¶Ciertamente ahora dirán: «No tenemos rey,
Porque no hemos temido al Señor.
Y el rey, ¿qué haría por nosotros(G)?».
4 Hablan solo palabras,
Hacen pactos con juramentos vanos(H),
Y el juicio brotará como hierbas venenosas en los surcos del campo(I).
5 Por el becerro(J) de Bet Avén(K)
Temerán los habitantes de Samaria.
En verdad, por él hará duelo su pueblo,
Y sus sacerdotes idólatras(L) se lamentarán a causa de él,
Porque de él se ha alejado su gloria(M).
6 También el becerro será llevado a Asiria(N)
Como tributo al rey Jareb[a](O);
Efraín se cubrirá de vergüenza(P),
E Israel se avergonzará de su consejo(Q).
7 Samaria será destruida con su rey(R),
Como astilla sobre la superficie del agua.
8 También serán destruidos los lugares altos de Avén(S), el pecado de Israel(T);
Espinos y cardos(U) crecerán sobre sus altares.
Entonces dirán a los montes:
«¡Cúbrannos!», y a los collados: «¡Caigan sobre nosotros(V)!».
9 Desde los días de Guibeá has pecado, oh Israel;
¡Allí se han quedado!
¿No los alcanzará en Guibeá la batalla contra los hijos de la iniquidad?
10 Cuando Yo lo desee(W), los castigaré(X);
Y se juntarán pueblos contra ellos(Y)
Cuando sean castigados por su doble iniquidad.
11 ¶Efraín es una novilla domesticada que le gusta trillar(Z),
Pero Yo pasaré un yugo sobre su hermoso cuello(AA);
Unciré a Efraín,
Arará Judá, rastrillará Jacob por sí mismo.
12 Siembren para ustedes según la justicia(AB),
Sieguen conforme a la misericordia[b];
Rompan la tierra para sembrar(AC),
Porque es tiempo de buscar al Señor(AD)
Hasta que venga a enseñarles justicia(AE).
13 Ustedes han arado iniquidad(AF), han segado injusticia,
Han comido fruto de mentira(AG).
Porque has confiado en tu camino, en la multitud de tus guerreros(AH),
14 Se levantará un tumulto entre tu pueblo,
Y todas tus fortalezas serán destruidas(AI),
Como Salmán destruyó a Bet Arbel el día de la batalla,
Cuando las madres fueron despedazadas con sus hijos(AJ).
15 Así les será hecho en Betel[c] a causa de su gran iniquidad.
Al amanecer, el rey de Israel será totalmente destruido.
Hosea 10
King James Version
10 Israel is an empty vine, he bringeth forth fruit unto himself: according to the multitude of his fruit he hath increased the altars; according to the goodness of his land they have made goodly images.
2 Their heart is divided; now shall they be found faulty: he shall break down their altars, he shall spoil their images.
3 For now they shall say, We have no king, because we feared not the Lord; what then should a king do to us?
4 They have spoken words, swearing falsely in making a covenant: thus judgment springeth up as hemlock in the furrows of the field.
5 The inhabitants of Samaria shall fear because of the calves of Bethaven: for the people thereof shall mourn over it, and the priests thereof that rejoiced on it, for the glory thereof, because it is departed from it.
6 It shall be also carried unto Assyria for a present to king Jareb: Ephraim shall receive shame, and Israel shall be ashamed of his own counsel.
7 As for Samaria, her king is cut off as the foam upon the water.
8 The high places also of Aven, the sin of Israel, shall be destroyed: the thorn and the thistle shall come up on their altars; and they shall say to the mountains, Cover us; and to the hills, Fall on us.
9 O Israel, thou hast sinned from the days of Gibeah: there they stood: the battle in Gibeah against the children of iniquity did not overtake them.
10 It is in my desire that I should chastise them; and the people shall be gathered against them, when they shall bind themselves in their two furrows.
11 And Ephraim is as an heifer that is taught, and loveth to tread out the corn; but I passed over upon her fair neck: I will make Ephraim to ride; Judah shall plow, and Jacob shall break his clods.
12 Sow to yourselves in righteousness, reap in mercy; break up your fallow ground: for it is time to seek the Lord, till he come and rain righteousness upon you.
13 Ye have plowed wickedness, ye have reaped iniquity; ye have eaten the fruit of lies: because thou didst trust in thy way, in the multitude of thy mighty men.
14 Therefore shall a tumult arise among thy people, and all thy fortresses shall be spoiled, as Shalman spoiled Betharbel in the day of battle: the mother was dashed in pieces upon her children.
15 So shall Bethel do unto you because of your great wickedness: in a morning shall the king of Israel utterly be cut off.
Hosea 10
New International Version
10 Israel was a spreading vine;(A)
he brought forth fruit for himself.
As his fruit increased,
he built more altars;(B)
as his land prospered,(C)
he adorned his sacred stones.(D)
2 Their heart is deceitful,(E)
and now they must bear their guilt.(F)
The Lord will demolish their altars(G)
and destroy their sacred stones.(H)
3 Then they will say, “We have no king
because we did not revere the Lord.
But even if we had a king,
what could he do for us?”
4 They make many promises,
take false oaths(I)
and make agreements;(J)
therefore lawsuits spring up
like poisonous weeds(K) in a plowed field.
5 The people who live in Samaria fear
for the calf-idol(L) of Beth Aven.[a](M)
Its people will mourn over it,
and so will its idolatrous priests,(N)
those who had rejoiced over its splendor,
because it is taken from them into exile.(O)
6 It will be carried to Assyria(P)
as tribute(Q) for the great king.(R)
Ephraim will be disgraced;(S)
Israel will be ashamed(T) of its foreign alliances.
7 Samaria’s king will be destroyed,(U)
swept away like a twig on the surface of the waters.
8 The high places(V) of wickedness[b](W) will be destroyed—
it is the sin of Israel.
Thorns(X) and thistles will grow up
and cover their altars.(Y)
Then they will say to the mountains, “Cover us!”(Z)
and to the hills, “Fall on us!”(AA)
9 “Since the days of Gibeah,(AB) you have sinned,(AC) Israel,
and there you have remained.[c]
Will not war again overtake
the evildoers in Gibeah?
10 When I please, I will punish(AD) them;
nations will be gathered against them
to put them in bonds for their double sin.
11 Ephraim is a trained heifer
that loves to thresh;
so I will put a yoke(AE)
on her fair neck.
I will drive Ephraim,
Judah must plow,
and Jacob must break up the ground.
12 Sow(AF) righteousness(AG) for yourselves,
reap the fruit of unfailing love,
and break up your unplowed ground;(AH)
for it is time to seek(AI) the Lord,
until he comes
and showers his righteousness(AJ) on you.
13 But you have planted wickedness,
you have reaped evil,(AK)
you have eaten the fruit of deception.(AL)
Because you have depended on your own strength
and on your many warriors,(AM)
14 the roar of battle will rise against your people,
so that all your fortresses will be devastated(AN)—
as Shalman(AO) devastated Beth Arbel on the day of battle,
when mothers were dashed to the ground with their children.(AP)
15 So will it happen to you, Bethel,
because your wickedness is great.
When that day dawns,
the king of Israel will be completely destroyed.(AQ)
Footnotes
- Hosea 10:5 Beth Aven means house of wickedness (a derogatory name for Bethel, which means house of God).
- Hosea 10:8 Hebrew aven, a reference to Beth Aven (a derogatory name for Bethel); see verse 5.
- Hosea 10:9 Or there a stand was taken
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Nueva Biblia de las Américas™ NBLA™ Copyright © 2005 por The Lockman Foundation
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.

