Add parallel Print Page Options

Kulapa Kubweretsa Madalitso

14 Iwe Israeli bwerera kwa Yehova Mulungu wako.
    Machimo anu ndi amene akugwetsani!
Bweretsani zopempha zanu
    ndipo bwererani kwa Yehova.
Munene kwa Iye kuti,
    “Tikhululukireni machimo athu onse
ndi kutilandira mokoma mtima,
    kuti tithe kukuyamikani ndi mawu a pakamwa pathu.
Asiriya sangatipulumutse;
    ife sitidzakwera pa akavalo ankhondo,
sitidzanenanso kuti, ‘Milungu yathu’
    kwa zimene manja athu omwe anazipanga,
    pakuti ndinu amene mumachitira chifundo ana amasiye.”

Ine ndidzachiza kusakhulupirika kwawo
    ndipo ndidzawakonda mwaufulu
    pakuti ndaleka kuwakwiyira.
Ndidzakhala ngati mame kwa Israeli
    Ndipo iye adzachita maluwa ngati kakombo.
Adzazika mizu yake pansi
    ngati mkungudza wa ku Lebanoni;
    mphukira zake zidzakula.
Kukongola kwake kudzakhala ngati mtengo wa olivi,
    kununkhira kwake ngati mkungudza wa ku Lebanoni.
Anthu adzakhalanso mu mthunzi wake.
    Iye adzakula bwino ngati tirigu.
Adzachita maluwa ngati mphesa
    ndipo kutchuka kwake kudzakhala ngati vinyo wochokera ku Lebanoni.
Efereimu adzati, “Ndidzachita nawonso chiyani mafano?
    Ine ndidzamuyankha ndi kumusamalira.
Ine ndili ngati mtengo wa payini wobiriwira;
    zipatso zako zimachokera kwa Ine.”

Ndani ali ndi nzeru? Adzazindikire zinthu izi.
    Ndani amene amamvetsa zinthu? Adzamvetse izi.
Njira za Yehova ndi zolungama;
    anthu olungama amayenda mʼmenemo,
    koma anthu owukira amapunthwamo.

Repentance to Bring Blessing

14 [a]Return,(A) Israel, to the Lord your God.
    Your sins(B) have been your downfall!(C)
Take words with you
    and return to the Lord.
Say to him:
    “Forgive(D) all our sins
and receive us graciously,(E)
    that we may offer the fruit of our lips.[b](F)
Assyria cannot save us;(G)
    we will not mount warhorses.(H)
We will never again say ‘Our gods’(I)
    to what our own hands have made,(J)
    for in you the fatherless(K) find compassion.”

“I will heal(L) their waywardness(M)
    and love them freely,(N)
    for my anger has turned away(O) from them.
I will be like the dew(P) to Israel;
    he will blossom like a lily.(Q)
Like a cedar of Lebanon(R)
    he will send down his roots;(S)
    his young shoots will grow.
His splendor will be like an olive tree,(T)
    his fragrance like a cedar of Lebanon.(U)
People will dwell again in his shade;(V)
    they will flourish like the grain,
they will blossom(W) like the vine—
    Israel’s fame will be like the wine(X) of Lebanon.(Y)
Ephraim, what more have I[c] to do with idols?(Z)
    I will answer him and care for him.
I am like a flourishing juniper;(AA)
    your fruitfulness comes from me.”

Who is wise?(AB) Let them realize these things.
    Who is discerning? Let them understand.(AC)
The ways of the Lord are right;(AD)
    the righteous walk(AE) in them,
    but the rebellious stumble in them.

Footnotes

  1. Hosea 14:1 In Hebrew texts 14:1-9 is numbered 14:2-10.
  2. Hosea 14:2 Or offer our lips as sacrifices of bulls
  3. Hosea 14:8 Or Hebrew; Septuagint What more has Ephraim

14 O israel, return unto the Lord thy God; for thou hast fallen by thine iniquity.

Take with you words, and turn to the Lord: say unto him, Take away all iniquity, and receive us graciously: so will we render the calves of our lips.

Asshur shall not save us; we will not ride upon horses: neither will we say any more to the work of our hands, Ye are our gods: for in thee the fatherless findeth mercy.

I will heal their backsliding, I will love them freely: for mine anger is turned away from him.

I will be as the dew unto Israel: he shall grow as the lily, and cast forth his roots as Lebanon.

His branches shall spread, and his beauty shall be as the olive tree, and his smell as Lebanon.

They that dwell under his shadow shall return; they shall revive as the corn, and grow as the vine: the scent thereof shall be as the wine of Lebanon.

Ephraim shall say, What have I to do any more with idols? I have heard him, and observed him: I am like a green fir tree. From me is thy fruit found.

Who is wise, and he shall understand these things? prudent, and he shall know them? for the ways of the Lord are right, and the just shall walk in them: but the transgressors shall fall therein.