Add parallel Print Page Options

Amayi awo akhala akuchita zachiwerewere
    ndipo anawabereka anawo akuchita zinthu zochititsa manyazi.
Iwo anati, ‘Ine ndidzatsatira zibwenzi zanga,
    zimene zimandipatsa chakudya ndi madzi,
    ubweya ndi thonje, mafuta ndi chakumwa.’

Read full chapter