Add parallel Print Page Options

Kukonzanso Pangano

29 Awa ndiwo mawu a mʼpangano limene Yehova analamula Mose kuti achite ndi Aisraeli ku Mowabu, powonjezera pa pangano limene anapangana nawo ku Horebu.

Mose anayitanitsa Aisraeli onse nati kwa iwo:

Inu munaona zonse zimene Yehova anachita kwa Farao, nduna zake ndi dziko lake lonse ku Igupto. Ndi maso anu munaona mayesero onse aja, zizindikiro zozizwitsa ndi zodabwitsa zazikulu zija. Koma mpaka lero Yehova sanakupatseni mtima wozindikira kapena maso openya kapena makutu akumva. Mʼzaka makumi anayi zimene ndinakutsogolerani mʼchipululu, zovala zanu ndiponso nsapato za ku mapazi anu sizinangʼambike. Inu simunadye buledi ndi kumwa vinyo kapena chakumwa chilichonse choledzeretsa. Ndinachita izi kuti mudziwe kuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu.

Pamene munafika malo ano, Sihoni mfumu ya ku Hesiboni ndi Ogi mfumu ya ku Basani anabwera kudzamenyana nafe koma tinawagonjetsa iwo. Tinatenga dziko lawo ndi kulipereka ngati cholowa cha fuko la Rubeni, fuko la Gadi ndi theka la fuko la Manase.

Tsatirani mosamalitsa mawu a mʼpangano ili kuti zinthu zizikuyenderani bwino pa zochitika zanu zonse. 10 Lero lino nonse mukuyima pamaso pa Yehova Mulungu wanu, atsogoleri a mafuko anu, akuluakulu ndi nduna zanu, ndi amuna ena onse a mu Israeli, 11 pamodzi ndi ana ndi akazi anu, kudzanso alendo amene akukhala pakati panu omwe amakuwazirani nkhuni ndi kukutungirani madzi. 12 Mukuyimirira pano kuti mulowe mʼpangano ndi Yehova Mulungu wanu, pangano limene Yehova akuchita ndi inu lero ndi kulisindikiza ndi malumbiro, 13 kukukhazikitsani lero lino ngati anthu ake, ndi kuti Iye akhale Mulungu wanu monga anakulonjezani inu ndiponso monga analumbira kwa makolo anu Abrahamu, Isake ndi Yakobo. 14 Ndikupanga pangano ili ndi malumbiro ake osati kwa inu nokha, 15 amene muli pano pamaso pa Yehova Mulungu wathu, koma ndi iwonso amene sali pano lero.

16 Inu nomwe mukudziwa mmene tinkakhalira ku Igupto ndi mmene tinadutsira mayiko pa ulendo wobwera kuno. 17 Ife tinaona pakati pawo mafanizo ndi mafano awo onyansa, amtengo ndi amiyala, asiliva ndi agolide. 18 Onetsetsani kuti pasapezeke mwamuna kapena mkazi, banja kapena fuko pakati panu lero amene mtima wawo udzapandukira Yehova Mulungu wanu ndi kupita kukapembedza milungu ya mitundu iyo. Onetsetsani kuti pasapezeke muzu pakati panu wotulutsa mankhwala akupha otere.

19 Munthu wotere akamva mawu a lumbiro ili, asadzidalitse yekha mʼmaganizo mwake namati, “Ine ndidzapulumuka ngakhale nditapitiriza kuyenda njira yanga.” Zoterezi zidzadzetsa masautso pa nthaka ya chinyontho ndi yowuma yomwe. 20 Yehova sadzamukhululukira. Mkwiyo ndi nsanje ya Yehova zidzamuyakira munthuyo. Matemberero onse wolembedwa mʼbukuli adzamugwera iye ndipo Yehova adzafafaniza dzina lake pa dziko lapansi. 21 Yehova adzasankha pakati pa Aisraeli anthu oyenera masautso monga mwa matemberero onse a mʼpangano olembedwa Mʼbuku la Malamulo.

22 Ana anu a mibado yakutsogolo ndi alendo amene adzachokera kutali adzaona matsoka amene adzakugwerani mʼdziko muno ndiponso matenda amene Yehova adzabweretsa pa dzikoli. 23 Dziko lonse lidzasanduka nthaka ya mchere ndi ya sulufule. Simudzadzalamo kanthu, simudzakhala chomera chilichonse, ndi mbewu yomera mʼmenemo. Dziko lanu lidzakhala lowonongeka ngati Sodomu ndi Gomora, Adima ndi Zeboimu, mizinda imene Yehova anayiwononga ndi mkwiyo wake waukulu. 24 Mitundu yonse ya anthu idzafunsa kuti, “Kodi chifukwa chiyani Yehova anachita zotere mʼdziko lake? Kodi chifukwa chiyani anaonetsa mkwiyo woopsa wotere?”

25 Ndipo yankho la mafunso amenewa lidzakhala lakuti, “Chifukwa chakuti anthu awa aphwanya pangano la Yehova Mulungu wa makolo awo, pangano limene Iye anapangana nawo pamene anawatulutsa ku Igupto. 26 Iwo anachoka ndi kukatumikira milungu ina ndi kuyipembedza, milungu imene sanayidziwe, milungu imene sanawapatse. 27 Choncho Yehova anakwiyira dziko lino, kotero anabweretsa matemberero onse amene analembedwa mʼbuku lino. 28 Ndi mkwiyo komanso ukali wake woopsa Yehova anawazula mʼdziko lawo ndi kuwaponyera mʼdziko lina, monga mmene zilili lero lino.”

29 Zinsinsi ndi za Yehova Mulungu wathu koma zinthu zimene zaululidwa ndi zathu ndi ana athu kwamuyaya, kuti titsatire mawu onse a mʼmalamulowa.

Renewal of the Covenant

29 [a]These are the terms of the covenant the Lord commanded Moses to make with the Israelites in Moab,(A) in addition to the covenant he had made with them at Horeb.(B)

Moses summoned all the Israelites and said to them:

Your eyes have seen all that the Lord did in Egypt to Pharaoh, to all his officials and to all his land.(C) With your own eyes you saw those great trials, those signs and great wonders.(D) But to this day the Lord has not given you a mind that understands or eyes that see or ears that hear.(E) Yet the Lord says, “During the forty years that I led(F) you through the wilderness, your clothes did not wear out, nor did the sandals on your feet.(G) You ate no bread and drank no wine or other fermented drink.(H) I did this so that you might know that I am the Lord your God.”(I)

When you reached this place, Sihon(J) king of Heshbon(K) and Og king of Bashan came out to fight against us, but we defeated them.(L) We took their land and gave it as an inheritance(M) to the Reubenites, the Gadites and the half-tribe of Manasseh.(N)

Carefully follow(O) the terms of this covenant,(P) so that you may prosper in everything you do.(Q) 10 All of you are standing today in the presence of the Lord your God—your leaders and chief men, your elders and officials, and all the other men of Israel, 11 together with your children and your wives, and the foreigners living in your camps who chop your wood and carry your water.(R) 12 You are standing here in order to enter into a covenant with the Lord your God, a covenant the Lord is making with you this day and sealing with an oath, 13 to confirm you this day as his people,(S) that he may be your God(T) as he promised you and as he swore to your fathers, Abraham, Isaac and Jacob. 14 I am making this covenant,(U) with its oath, not only with you 15 who are standing here with us today in the presence of the Lord our God but also with those who are not here today.(V)

16 You yourselves know how we lived in Egypt and how we passed through the countries on the way here. 17 You saw among them their detestable images and idols of wood and stone, of silver and gold.(W) 18 Make sure there is no man or woman, clan or tribe among you today whose heart turns(X) away from the Lord our God to go and worship the gods of those nations; make sure there is no root among you that produces such bitter poison.(Y)

19 When such a person hears the words of this oath and they invoke a blessing(Z) on themselves, thinking, “I will be safe, even though I persist in going my own way,”(AA) they will bring disaster on the watered land as well as the dry. 20 The Lord will never be willing to forgive(AB) them; his wrath and zeal(AC) will burn(AD) against them. All the curses written in this book will fall on them, and the Lord will blot(AE) out their names from under heaven. 21 The Lord will single them out from all the tribes of Israel for disaster,(AF) according to all the curses of the covenant written in this Book of the Law.(AG)

22 Your children who follow you in later generations and foreigners who come from distant lands will see the calamities that have fallen on the land and the diseases with which the Lord has afflicted it.(AH) 23 The whole land will be a burning waste(AI) of salt(AJ) and sulfur—nothing planted, nothing sprouting, no vegetation growing on it. It will be like the destruction of Sodom and Gomorrah,(AK) Admah and Zeboyim, which the Lord overthrew in fierce anger.(AL) 24 All the nations will ask: “Why has the Lord done this to this land?(AM) Why this fierce, burning anger?”

25 And the answer will be: “It is because this people abandoned the covenant of the Lord, the God of their ancestors, the covenant he made with them when he brought them out of Egypt.(AN) 26 They went off and worshiped other gods and bowed down to them, gods they did not know, gods he had not given them. 27 Therefore the Lord’s anger burned against this land, so that he brought on it all the curses written in this book.(AO) 28 In furious anger and in great wrath(AP) the Lord uprooted(AQ) them from their land and thrust them into another land, as it is now.”

29 The secret things belong to the Lord our God,(AR) but the things revealed belong to us and to our children forever, that we may follow all the words of this law.(AS)

Footnotes

  1. Deuteronomy 29:1 In Hebrew texts 29:1 is numbered 28:69, and 29:2-29 is numbered 29:1-28.

The Covenant Renewed in Moab

29 These are the words of the covenant which the Lord commanded Moses to make with the children of Israel in the land of Moab, besides the (A)covenant which He made with them in Horeb.

Now Moses called all Israel and said to them: (B)“You have seen all that the Lord did before your eyes in the land of Egypt, to Pharaoh and to all his servants and to all his land— (C)the great trials which your eyes have seen, the signs, and those great wonders. Yet (D)the Lord has not given you a heart to [a]perceive and eyes to see and ears to hear, to this very day. (E)And I have led you forty years in the wilderness. (F)Your clothes have not worn out on you, and your sandals have not worn out on your feet. (G)You have not eaten bread, nor have you drunk wine or similar drink, that you may know that I am the Lord your God. And when you came to this place, (H)Sihon king of Heshbon and Og king of Bashan came out against us to battle, and we conquered them. We took their land and (I)gave it as an inheritance to the Reubenites, to the Gadites, and to half the tribe of Manasseh. Therefore (J)keep the words of this covenant, and do them, that you may (K)prosper in all that you do.

10 “All of you stand today before the Lord your God: your leaders and your tribes and your elders and your officers, all the men of Israel, 11 your little ones and your wives—also the stranger who is in your camp, from (L)the one who cuts your wood to the one who draws your water— 12 that you may enter into covenant with the Lord your God, and (M)into His oath, which the Lord your God makes with you today, 13 that He may (N)establish you today as a people for Himself, and that He may be God to you, (O)just as He has spoken to you, and (P)just as He has sworn to your fathers, to Abraham, Isaac, and Jacob.

14 “I make this covenant and this oath, (Q)not with you alone, 15 but with him who stands here with us today before the Lord our God, (R)as well as with him who is not here with us today 16 (for you know that we dwelt in the land of Egypt and that we came through the nations which you passed by, 17 and you saw their [b]abominations and their idols which were among them—wood and stone and silver and gold); 18 so that there may not be among you man or woman or family or tribe, (S)whose heart turns away today from the Lord our God, to go and serve the gods of these nations, (T)and that there may not be among you a root bearing (U)bitterness or wormwood; 19 and so it may not happen, when he hears the words of this curse, that he blesses himself in his heart, saying, ‘I shall have peace, even though I [c]follow the (V)dictates of my heart’—(W)as though the drunkard could be included with the sober.

20 (X)“The Lord would not spare him; for then (Y)the anger of the Lord and (Z)His jealousy would burn against that man, and every curse that is written in this book would settle on him, and the Lord (AA)would blot out his name from under heaven. 21 And the Lord (AB)would separate him from all the tribes of Israel for adversity, according to all the curses of the covenant that are written in this Book of the (AC)Law, 22 so that the coming generation of your children who rise up after you, and the foreigner who comes from a far land, would say, when they (AD)see the plagues of that land and the sicknesses which the Lord has laid on it:

23 ‘The whole land is brimstone, (AE)salt, and burning; it is not sown, nor does it bear, nor does any grass grow there, (AF)like the overthrow of Sodom and Gomorrah, Admah, and Zeboiim, which the Lord overthrew in His anger and His wrath.’ 24 All nations would say, (AG)‘Why has the Lord done so to this land? What does the heat of this great anger mean?’ 25 Then people would say: ‘Because they have forsaken the covenant of the Lord God of their fathers, which He made with them when He brought them out of the land of Egypt; 26 for they went and served other gods and worshiped them, gods that they did not know and that He had not given to them. 27 Then the anger of the Lord was aroused against this land, (AH)to bring on it every curse that is written in this book. 28 And the Lord (AI)uprooted them from their land in anger, in wrath, and in great indignation, and cast them into another land, as it is this day.’

29 “The secret things belong to the Lord our God, but those things which are revealed belong to us and to our children forever, that we may do all the words of this law.

Footnotes

  1. Deuteronomy 29:4 understand or know
  2. Deuteronomy 29:17 detestable things
  3. Deuteronomy 29:19 walk in the stubbornness or imagination