Font Size
Machitidwe a Atumwi 2:3
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Machitidwe a Atumwi 2:3
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
3 Iwo anaona zinthu zokhala ngati malilime amoto ogawikana ndipo anakhala pa aliyense wa iwo.
Read full chapter
Machitidwe a Atumwi 2:4
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Machitidwe a Atumwi 2:4
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
4 Ndipo onse anadzazidwa ndi Mzimu Woyera, nayamba kuyankhula mu ziyankhulo zina, monga Mzimu Woyerayo anawayankhulitsa.
Read full chapter
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero (CCL)
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.