1 Samueli 3
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Yehova Ayitana Samueli
3 Samueli ankatumikira Yehova moyangʼaniridwa ndi Eli. Masiku amenewo mawu a Yehova sankamveka pafupipafupi. Kuona zinthu mʼmasomphenya sikunkachitikanso kawirikawiri.
2 Tsiku lina Eli, amene maso anali ofowoka ndi kuti sankatha kuona bwino, anagona pa malo ake. 3 Nthawiyi nʼkuti nyale ya Mulungu isanazimitsidwe. Samueli anali gone mu Nyumba ya Yehova, kumene kunali Bokosi la Chipangano cha Mulungu. 4 Yehova anayitana Samueli.
Iye anayankha kuti, “Wawa.” 5 Ndipo iyeyo anathamangira kwa Eli ndipo anati, “Ndabwera ndamva kuyitana.”
Koma Eli anati, “Ine sindinakuyitane, bwerera kagone.” Ndipo iye anapita kukagona.
6 Yehova anayitananso, “Samueli!” Ndipo Samueli anadzuka ndi kupita kwa Eli nati, “Ndabwera popeza ndamva mukundiyitana.”
Eli nati, “Mwana wanga, ine sindinakuyitane, bwerera kagone.”
7 Nthawiyi nʼkuti Samueli asanadziwe Yehova ndipo Mawu a Yehova nʼkuti asanawululidwe kwa iye.
8 Yehova anayitananso Samueli kachitatu ndipo Samueli anadzuka ndikupita kwa Eli ndipo anati, “Ndabwera popeza mwandiyitana ndithu.”
Apo Eli anazindikira kuti Yehova ndiye ankayitana mnyamatayo. 9 Tsono Eli anamuwuza Samueli kuti, “Pita ukagone ndipo akakuyitananso ukanene kuti, ‘Yankhulani Yehova, pakuti mtumiki wanu ndikumvetsera.’ ” Choncho Samueli anapita ndi kukagona pamalo pake.
10 Yehova anabwera ndi kuyima pomwepo, ndi kuyitana monga nthawi zina zija, “Samueli! Samueli!”
Ndipo Samueli anayankha, “Yankhulani, pakuti mtumiki wanu akumvetsera.”
11 Ndipo Yehova anati kwa Samueli, “Taona, patsala pangʼono kuti ndichite chinthu china mu Israeli chimene chidzadabwitsa aliyense amene adzamve. 12 Tsiku limenelo ndidzachitadi zonse zimene ndinayankhula zokhudza banja la Eli kuyambira poyamba mpaka pomaliza. 13 Pakuti ndinamudziwitsa kuti Ine ndikhoza kulanga banja lake kwamuyaya chifukwa cha zoyipa zimene ana ake ankadziyipitsa nazo. Iye ankadziwa zimenezi koma osawaletsa. 14 Nʼchifukwa chake ndinalumbira kuti, ‘Zoyipa zimene banja la Eli linandichita sizidzafafanizidwa mpaka muyaya ngakhale adzapereke nsembe kapena zopereka zina.’ ”
15 Samueli anagona mpaka mmawa. Atadzuka anatsekula zitseko za Nyumba ya Yehova. Iye anachita mantha kumuwuza Eli za masomphenya ake. 16 Koma Eli anamuyitana nati, “Samueli mwana wanga.”
Samueli anayankha kuti, “Wawa.”
17 Tsono Eli anafunsa kuti, “Yehova wakuwuza chiyani? Usandibisire. Mulungu akulange ndithu ngati undibisira chilichonse cha zimene wakuwuza.” 18 Choncho Samueli anamuwuza zonse, sanamubisire kalikonse. Ndipo Eli anati, “Iye ndi Yehova, mulekeni achite chimene chamukomera.”
19 Yehova anali ndi Samueli pamene amakula, ndipo zonse zimene ankayankhula zinkachitikadi. 20 Ndipo Aisraeli onse kuyambira ku dera la Dani mpaka ku Beeriseba anazindikira kuti Yehova analozadi chala pa Samueli kuti akhale mneneri wake. 21 Yehova anapitiriza kuoneka ku Silo, ndipo kumeneko anadziwulula yekha kwa Samueli mwa mawu ake.
1 Samuel 3
English Standard Version
The Lord Calls Samuel
3 (A)Now the boy Samuel was ministering to the Lord in the presence of Eli. (B)And the word of the Lord was rare in those days; there was no frequent vision.
2 At that time Eli, (C)whose eyesight had begun to grow dim so that he could not see, was lying down in his own place. 3 (D)The lamp of God had not yet gone out, and Samuel was lying down (E)in the temple of the Lord, where the ark of God was.
4 Then the Lord called Samuel, and he said, “Here I am!” 5 and ran to Eli and said, “Here I am, for you called me.” But he said, “I did not call; lie down again.” So he went and lay down.
6 And the Lord called again, “Samuel!” and Samuel arose and went to Eli and said, “Here I am, for you called me.” But he said, “I did not call, my son; lie down again.” 7 Now Samuel did not yet know the Lord, and the word of the Lord had not yet been revealed to him.
8 And the Lord called Samuel again the third time. And he arose and went to Eli and said, “Here I am, for you called me.” Then Eli perceived that the Lord was calling the boy. 9 Therefore Eli said to Samuel, “Go, lie down, and if he calls you, you shall say, ‘Speak, Lord, for your servant hears.’” So Samuel went and lay down in his place.
10 And the Lord came and stood, calling as at other times, “Samuel! Samuel!” And Samuel said, “Speak, for your servant hears.” 11 Then the Lord said to Samuel, “Behold, I am about to do a thing in Israel (F)at which the two ears of everyone who hears it will tingle. 12 On that day I will fulfill against Eli (G)all that I have spoken concerning his house, from beginning to end. 13 (H)And I declare to him that I am about to punish his house forever, for the iniquity that he knew, (I)because his sons were blaspheming God,[a] (J)and he did not restrain them. 14 Therefore I swear to the house of Eli (K)that the iniquity of Eli's house shall not be atoned for by sacrifice or offering forever.”
15 Samuel lay until morning; then he opened the doors of the house of the Lord. And Samuel was afraid to tell the vision to Eli. 16 But Eli called Samuel and said, “Samuel, my son.” And he said, “Here I am.” 17 And Eli said, “What was it that he told you? Do not hide it from me. (L)May God do so to you and more also if you hide anything from me of all that he told you.” 18 So Samuel told him everything and hid nothing from him. And he said, (M)“It is the Lord. Let him do what seems good to him.”
19 (N)And Samuel grew, and the Lord was with him (O)and let none of his words fall to the ground. 20 And all Israel (P)from Dan to Beersheba knew that Samuel was established as a prophet of the Lord. 21 And the Lord appeared again at Shiloh, for the Lord revealed himself to Samuel (Q)at Shiloh (R)by the word of the Lord.
Footnotes
- 1 Samuel 3:13 Or blaspheming for themselves
1 Samuel 3
New International Version
The Lord Calls Samuel
3 The boy Samuel ministered(A) before the Lord under Eli. In those days the word of the Lord was rare;(B) there were not many visions.(C)
2 One night Eli, whose eyes(D) were becoming so weak that he could barely see,(E) was lying down in his usual place. 3 The lamp(F) of God had not yet gone out, and Samuel was lying down in the house(G) of the Lord, where the ark(H) of God was. 4 Then the Lord called Samuel.
Samuel answered, “Here I am.(I)” 5 And he ran to Eli and said, “Here I am; you called me.”
But Eli said, “I did not call; go back and lie down.” So he went and lay down.
6 Again the Lord called, “Samuel!” And Samuel got up and went to Eli and said, “Here I am; you called me.”
“My son,” Eli said, “I did not call; go back and lie down.”
7 Now Samuel did not yet know(J) the Lord: The word(K) of the Lord had not yet been revealed(L) to him.
8 A third time the Lord called, “Samuel!” And Samuel got up and went to Eli and said, “Here I am; you called me.”
Then Eli realized that the Lord was calling the boy. 9 So Eli told Samuel, “Go and lie down, and if he calls you, say, ‘Speak, Lord, for your servant is listening.’” So Samuel went and lay down in his place.
10 The Lord came and stood there, calling as at the other times, “Samuel! Samuel!(M)”
Then Samuel said, “Speak, for your servant is listening.”
11 And the Lord said to Samuel: “See, I am about to do something in Israel that will make the ears of everyone who hears about it tingle.(N) 12 At that time I will carry out against Eli everything(O) I spoke against his family—from beginning to end. 13 For I told him that I would judge his family forever because of the sin he knew about; his sons blasphemed God,[a] and he failed to restrain(P) them. 14 Therefore I swore to the house of Eli, ‘The guilt of Eli’s house will never be atoned(Q) for by sacrifice or offering.’”
15 Samuel lay down until morning and then opened the doors of the house of the Lord. He was afraid to tell Eli the vision, 16 but Eli called him and said, “Samuel, my son.”
Samuel answered, “Here I am.”
17 “What was it he said to you?” Eli asked. “Do not hide(R) it from me. May God deal with you, be it ever so severely,(S) if you hide from me anything he told you.” 18 So Samuel told him everything, hiding nothing from him. Then Eli said, “He is the Lord; let him do what is good in his eyes.”(T)
19 The Lord was with(U) Samuel as he grew(V) up, and he let none(W) of Samuel’s words fall to the ground. 20 And all Israel from Dan to Beersheba(X) recognized that Samuel was attested as a prophet of the Lord.(Y) 21 The Lord continued to appear at Shiloh, and there he revealed(Z) himself to Samuel through his word.
Footnotes
- 1 Samuel 3:13 An ancient Hebrew scribal tradition (see also Septuagint); Masoretic Text sons made themselves contemptible
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
The ESV® Bible (The Holy Bible, English Standard Version®), © 2001 by Crossway, a publishing ministry of Good News Publishers. ESV Text Edition: 2025.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.

