Add parallel Print Page Options

Akulu Ampingo ndi Anyamata mu Mpingo

Ine ndikupempha akulu a mpingo amene ali pakati panu, monga inenso mkulu mnzawo, mboni ya zowawa za Khristu ndiponso amene ndidzalandira nawo ulemerero umene uti udzaonetsedwe. Wetani gulu la Mulungu limene lili mʼmanja mwanu, muziliyangʼanira. Muzichita osati mowumirizidwa, koma mwakufuna kwanu, monga momwe Mulungu akufunira kuti mutero. Musachite chifukwa chadyera la ndalama, koma ndi mtima ofuna kutumikira. Musakhale ngati mafumu pa amene mukuwayangʼanira, koma mukhale chitsanzo kwa gululo. Ndipo Mʼbusa wamkulu akadzaonekera, mudzalandira chipewa cha ulemerero chosafota.

Momwemonso, inu anyamata gonjerani amene ndi akulu. Inu nonse mukhale odzichepetsa kuti mutumikirane, chifukwa,

“Mulungu amatsutsana nawo odzikuza,
    koma amapereka chisomo kwa odzichepetsa.”

Choncho, mudzichepetse pamaso pa Mulungu wamphamvu, kuti pa nthawi yake adzakukwezeni. Tayani pa Iye nkhawa zanu zonse chifukwa ndiye amakusamalani.

Khalani odziretsa ndi atcheru. Mdani wanu mdierekezi amayendayenda monga mkango wobangula kufunafuna wina kuti amumeze. Mukaneni iye, ndipo mukhazikike mʼchikhulupiriro, chifukwa mukudziwa kuti abale anzanu pa dziko lonse lapansi nawonso akumva zowawa zomwezi.

10 Ndipo Mulungu wachisomo chonse, amene anakuyitanani ku ulemerero wake wamuyaya mwa Khristu, mutamva zowawa pa kanthawi, adzakukonzaninso ndi kukulimbitsani pa maziko olimba. 11 Kwa Iye kukhale mphamvu mpaka muyaya, Ameni.

Mawu Otsiriza

12 Mothandizidwa ndi Sila, amene ndi mʼbale wokhulupirika, ndakulemberani mwachidule kukulimbikitsani ndi kuchita umboni kuti ichi ndi chisomo choona cha Mulungu. 13 Imani mwamphamvu mʼchisomochi. Mlongo wanu amene ali ku Babuloni, wosankhidwa pamodzi nanu akupereka moni, nayenso Marko, mwana wanga, akupereka moni. 14 Mupatsane moni ndi mpsopsono wachikondi. Mtendere ukhale ndi inu nonse amene muli mwa Khristu.

The elders which are among you I exhort, who am also an elder, and a witness of the sufferings of Christ, and also a partaker of the glory that shall be revealed:

Feed the flock of God which is among you, taking the oversight thereof, not by constraint, but willingly; not for filthy lucre, but of a ready mind;

Neither as being lords over God's heritage, but being examples to the flock.

And when the chief Shepherd shall appear, ye shall receive a crown of glory that fadeth not away.

Likewise, ye younger, submit yourselves unto the elder. Yea, all of you be subject one to another, and be clothed with humility: for God resisteth the proud, and giveth grace to the humble.

Humble yourselves therefore under the mighty hand of God, that he may exalt you in due time:

Casting all your care upon him; for he careth for you.

Be sober, be vigilant; because your adversary the devil, as a roaring lion, walketh about, seeking whom he may devour:

Whom resist stedfast in the faith, knowing that the same afflictions are accomplished in your brethren that are in the world.

10 But the God of all grace, who hath called us unto his eternal glory by Christ Jesus, after that ye have suffered a while, make you perfect, stablish, strengthen, settle you.

11 To him be glory and dominion for ever and ever. Amen.

12 By Silvanus, a faithful brother unto you, as I suppose, I have written briefly, exhorting, and testifying that this is the true grace of God wherein ye stand.

13 The church that is at Babylon, elected together with you, saluteth you; and so doth Marcus my son.

14 Greet ye one another with a kiss of charity. Peace be with you all that are in Christ Jesus. Amen.

Shepherd the Flock of God

So I exhort the elders among you, (A)as a fellow elder and (B)a witness of the sufferings of Christ, as well as a partaker in the glory that is going to be revealed: (C)shepherd the flock of God that is among you, exercising oversight,[a] (D)not under compulsion, but willingly, as God would have you;[b] (E)not for shameful gain, but eagerly; not (F)domineering over those in your charge, but (G)being examples to the flock. And when (H)the chief Shepherd appears, you will receive the (I)unfading (J)crown of glory. Likewise, you who are younger, be subject to the elders. (K)Clothe yourselves, all of you, with humility toward one another, for (L)“God opposes the proud but gives grace to the humble.”

(M)Humble yourselves, therefore, under the mighty hand of God so that at the proper time he may exalt you, (N)casting all your anxieties on him, because (O)he cares for you. (P)Be sober-minded; (Q)be watchful. Your (R)adversary the devil (S)prowls around (T)like a roaring lion, seeking someone to devour. (U)Resist him, (V)firm in your faith, knowing that (W)the same kinds of suffering are being experienced by your brotherhood throughout the world. 10 And (X)after you have suffered a little while, the God of all grace, (Y)who has called you to his (Z)eternal glory in Christ, will himself (AA)restore, (AB)confirm, strengthen, and establish you. 11 (AC)To him be the dominion forever and ever. Amen.

Final Greetings

12 By (AD)Silvanus, a faithful brother as I regard him, (AE)I have written briefly to you, exhorting and declaring that this is (AF)the true grace of God. (AG)Stand firm in it. 13 She who is at Babylon, who is likewise chosen, sends you greetings, and so does (AH)Mark, my son. 14 (AI)Greet one another with the kiss of love.

(AJ)Peace to all of you who are in Christ.

Footnotes

  1. 1 Peter 5:2 Some manuscripts omit exercising oversight
  2. 1 Peter 5:2 Some manuscripts omit as God would have you