1 Akorinto 8
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Nyama ya Nsembe za Mafano
8 Tsopano za chakudya choperekedwa nsembe kwa mafano: Ife tidziwa kuti tonse tili ndi chidziwitso. Komatu chidziwitso chokha chimadzitukumula, koma chikondi ndicho chimapindulitsa. 2 Munthu amene amaganiza kuti amadziwa kanthu, ndiye kuti sakudziwa monga mmene amayenera kudziwira. 3 Koma munthu amene amakonda Mulungu amadziwika ndi Mulunguyo.
4 Choncho kunena za chakudya choperekedwa nsembe kwa mafano; ife tikudziwa kuti mafano si kanthu nʼpangʼonongʼono pomwe pa dziko lapansi, ndiponso kuti palibe Mulungu wina koma mmodzi yekha. 5 Popeza kuti ngakhale pali yotchedwa milungu, kaya ndi kumwamba kapena pa dziko lapansi (poti ilipodi milungu yambirimbiri ndi ambuye ambirimbiri), 6 koma kwa ife pali Mulungu mmodzi yekha, Atate, zinthu zonse zinachokera mwa Iye ndipo ndife ake. Komanso pali Ambuye mmodzi Yesu Khristu kumene zinthu zonse zinachokera ndipo mwa Iye ife tili ndi moyo.
7 Koma saliyense amadziwa zimenezi. Alipo ena ozolowera mafano kwambiri mwakuti akadya chakudya chotere amaganiza kuti chakudyacho chinaperekedwa nsembe kwa mafano. Ndiye poti chikumbumtima chawo nʼchofowoka chimadetsedwadi. 8 Koma chakudya sichitisendeza kufupi ndi Mulungu. Tikapanda kudya si vuto, tikadya sitisinthikanso.
9 Komabe samalani kuti ufulu wanu ochita zinthu usafike pokhumudwitsa ofowoka. 10 Pakuti ngati aliyense wachikumbumtima chofowoka akakuonani achidziwitsonu mukudya mʼnyumba yopembedzera mafano, kodi iyeyo sichidzamulimbitsa mtima kuti azidya chakudya choperekedwa nsembe kwa mafano? 11 Kotero kuti chifukwa cha chidziwitso chanu mʼbale wofowokayu amene chifukwa cha iye, Khristu anafa, wawonongeka chifukwa cha chidziwitso chanu. 12 Mukamachimwira abale anu motere ndikuwawonongera chikumbumtima chawo chofowokacho, mukuchimwira Khristu. 13 Nʼchifukwa chake ngati zimene ine ndimadya zichititsa mʼbale wanga kugwa mu tchimo, sindidzadyanso chakudyacho kuti mʼbaleyo ndisamuchimwitse.
1 Corinthiens 8
La Bible du Semeur
Sur les viandes sacrifiées aux idoles
8 Passons au problème[a] des viandes provenant d’animaux sacrifiés aux idoles[b]. Nous possédons tous la connaissance voulue, nous le savons. Mais la connaissance rend orgueilleux. L’amour, lui, fait grandir dans la foi. 2 Celui qui s’imagine avoir de la connaissance ne connaît pas encore comme on doit connaître. 3 Mais celui qui aime Dieu, celui-là est connu de Dieu. 4 Qu’en est-il donc de la question de la consommation des viandes sacrifiées aux idoles ? Nous savons qu’il n’existe pas d’idoles dans le monde et qu’il n’y a qu’un seul Dieu. 5 Certes, bien des êtres célestes ou terrestres sont considérés comme des divinités, de sorte qu’il y a de nombreux dieux ou seigneurs. 6 Mais pour ce qui nous concerne, il n’y a qu’un seul Dieu : le Père, de qui toute chose vient, et pour qui nous vivons, et il n’y a qu’un seul Seigneur : Jésus-Christ, par qui tout existe et par qui nous sommes.
7 Mais tous les chrétiens n’ont pas encore bien assimilé ces vérités. Quelques-uns, encore marqués par leur habitude de rendre un culte aux idoles, continuent à manger ces viandes avec la pensée qu’elles ont été offertes à des idoles. Alors leur conscience, qui est faible, se charge de culpabilité. 8 Mais ce n’est pas un aliment qui peut nous rapprocher de Dieu ; en manger ou pas ne nous rendra ni meilleurs, ni pires. 9 Toutefois, faites bien attention à ce que votre liberté ne cause pas la chute de ceux qui sont mal affermis dans la foi. 10 Supposons, en effet, que l’un d’eux te voie, toi, qui as la connaissance, assis à table dans un temple d’idoles[c]. Sa conscience ne va-t-elle pas l’encourager, lui qui est mal affermi, à manger des viandes sacrifiées aux idoles ? 11 Ainsi, à cause de ta connaissance, ce chrétien mal affermi va courir à sa perte. Et pourtant, c’est un frère ou une sœur pour qui Christ a donné sa vie ! 12 Si vous péchez de la sorte envers des frères ou des sœurs, en blessant leur conscience qui est faible, vous péchez contre Christ lui-même. 13 C’est pourquoi, si ce que je mange devait causer la chute de mon frère ou de ma sœur, j’y renoncerais à tout jamais, afin de ne pas être pour lui une occasion de chute.
Footnotes
- 8.1 Voir note 7.1.
- 8.1 Ces viandes provenaient des animaux offerts en sacrifice dans les temples païens. Une partie de la viande était consommée sur place, une autre était donnée aux prêtres, ce qui restait était rendu aux offrants ou vendu au marché (10.25). Certains chrétiens se demandaient si ce n’était pas participer à l’idolâtrie que de consommer des viandes (achetées au marché) qui avaient été offertes aux idoles (voir Ac 15.29).
- 8.10 Les païens invitaient leurs amis aux repas de sacrifice dans les temples d’idoles.
1 Corinthians 8
New King James Version
Be Sensitive to Conscience
8 Now (A)concerning things offered to idols: We know that we all have (B)knowledge. (C)Knowledge [a]puffs up, but love [b]edifies. 2 And (D)if anyone thinks that he knows anything, he knows nothing yet as he ought to know. 3 But if anyone loves God, this one is known by Him.
4 Therefore concerning the eating of things offered to idols, we know that (E)an idol is nothing in the world, (F)and that there is no other God but one. 5 For even if there are (G)so-called gods, whether in heaven or on earth (as there are many gods and many lords), 6 yet (H)for us there is one God, the Father, (I)of whom are all things, and we for Him; and (J)one Lord Jesus Christ, (K)through whom are all things, and (L)through whom we live.
7 However, there is not in everyone that knowledge; for some, (M)with consciousness of the idol, until now eat it as a thing offered to an idol; and their conscience, being weak, is (N)defiled. 8 But (O)food does not commend us to God; for neither if we eat are we the better, nor if we do not eat are we the worse.
9 But (P)beware lest somehow this liberty of yours become (Q)a [c]stumbling block to those who are weak. 10 For if anyone sees you who have knowledge eating in an idol’s temple, will not (R)the conscience of him who is weak be emboldened to eat those things offered to idols? 11 And (S)because of your knowledge shall the weak brother perish, for whom Christ died? 12 But (T)when you thus sin against the brethren, and wound their weak conscience, you sin against Christ. 13 Therefore, (U)if food makes my brother stumble, I will never again eat meat, lest I make my brother stumble.
Footnotes
- 1 Corinthians 8:1 makes arrogant
- 1 Corinthians 8:1 builds up
- 1 Corinthians 8:9 cause of offense
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
La Bible Du Semeur (The Bible of the Sower) Copyright © 1992, 1999 by Biblica, Inc.®
Used by permission. All rights reserved worldwide.
Scripture taken from the New King James Version®. Copyright © 1982 by Thomas Nelson. Used by permission. All rights reserved.
