Add parallel Print Page Options

Mpingo ndi Atsogoleri Ake

Ndipo abale sindikanakuyankhulani ngati auzimu koma adziko lapansi, makanda chabe mwa Khristu. Ndinakupatsani mkaka osati chakudya cholimba pakuti munali musanakonzeke kuchilandira. Zoonadi, simunakonzekebe. Mukanali adziko lapansi. Pakuti pakati panu pali kaduka ndi kukangana, kodi si inu a dziko lapansi? Kodi simukuchita ngati anthu wamba? Pamene wina anena kuti, “Ine ndimatsatira Paulo,” ndipo wina akuti, “Ine ndimatsatira Apolo,” Kodi si inu akunja?

Ndiponso kodi Apolo ndi ndani? Nanga Paulo ndi ndani? Otumikira chabe, omwe kudzera mwa iwo inu munakhulupirira monga Ambuye anawagawira aliyense ntchito yake. Ine ndinadzala mbewu, Apolo anayithirira, koma Mulungu ndiye anayikulitsa. Choncho kuphatikiza iye wodzala ndi iye wothirira, onse sali kanthu, koma Mulungu yekha amene amakulitsa zinthu. Munthu wodzala ndi munthu wothirira ali ndi cholinga chimodzi, ndipo aliyense adzapatsidwa mphotho molingana ndi ntchito yake. Pakuti ife ndife antchito anzake a Mulungu; inu ndinu munda wa Mulungu, Nyumba ya Mulungu.

10 Mwachisomo chimene Mulungu wandipatsa, ine ndinayika maziko monga mmisiri waluntha, ndipo ena akumangapo. Koma aliyense ayenera kuchenjera mmene akumangira. 11 Pakuti wina sangayikenso maziko ena oposera amene anakhazikitsidwa kale, amene ndi Yesu Khristu. 12 Ngati munthu aliyense amanga pa maziko awa pogwiritsa ntchito golide, siliva, miyala yamtengowapatali, milimo yamitengo, tsekera kapena udzu, 13 ntchito yake idzaonekera pamene Tsiku la chiweruzo lidzazionetsa poyera. Tsikulo lidzafika ndi moto, ndipo motowo ndi umene udzayesa ntchito ya munthu aliyense. 14 Ngati zimene zamangidwazo sizidzagwa, adzalandira mphotho yake. 15 Ndipo ngati zidzanyeke ndi moto, sadzalandira mphotho koma iye mwini adzapulumukabe, koma monga ngati munthu amene wapulumuka mʼmoto.

16 Kodi inu simukudziwa kuti ndinu Nyumba ya Mulungu ndipo kuti Mzimu wa Mulungu amakhala mwa inu? 17 Ngati wina aliyense awononga Nyumba ya Mulunguyo, Mulungu nayenso adzamuwononga ameneyo; popeza Nyumba ya Mulungu ndi yopatulika ndipo Nyumbayo ndi inu amene.

18 Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. 19 Pakuti nzeru ya dziko lapansi ndi yopusa pamaso pa Mulungu. Monga kwalembedwera kuti, “Iye amakola anthu ochenjera mu msampha wa kuchenjera kwawo,” 20 ndiponso, “Ambuye amadziwa kuti maganizo a wanzeru ndi opandapake.” 21 Choncho, wina asanyadire anthu chabe! Zonse ndi zanu, 22 kaya Paulo kapena Apolo kapena Kefa kapena dziko lapansi, kapena moyo, kapena imfa, kapena tsopano, kapena mʼtsogolo, zonse ndi zanu, 23 ndipo inu ndinu a Khristu, ndipo Khristu ndi wa Mulungu.

Sectarianism Is Carnal

And I, brethren, could not speak to you as to spiritual people but as to carnal, as to (A)babes in Christ. I fed you with (B)milk and not with solid food; (C)for until now you were not able to receive it, and even now you are still not able; for you are still carnal. For where there are envy, strife, and divisions among you, are you not carnal and [a]behaving like mere men? For when one says, “I am of Paul,” and another, “I am of Apollos,” are you not carnal?

Watering, Working, Warning

Who then is Paul, and who is Apollos, but (D)ministers through whom you believed, as the Lord gave to each one? (E)I planted, (F)Apollos watered, (G)but God gave the increase. So then (H)neither he who plants is anything, nor he who waters, but God who gives the increase. Now he who plants and he who waters are one, (I)and each one will receive his own reward according to his own labor.

For (J)we are God’s fellow workers; you are God’s field, you are (K)God’s building. 10 (L)According to the grace of God which was given to me, as a wise master builder I have laid (M)the foundation, and another builds on it. But let each one take heed how he builds on it. 11 For no other foundation can anyone lay than (N)that which is laid, (O)which is Jesus Christ. 12 Now if anyone builds on this foundation with gold, silver, precious stones, wood, hay, straw, 13 each one’s work will become clear; for the Day (P)will declare it, because (Q)it will be revealed by fire; and the fire will test each one’s work, of what sort it is. 14 If anyone’s work which he has built on it endures, he will receive a reward. 15 If anyone’s work is burned, he will suffer loss; but he himself will be saved, yet so as through fire.

16 (R)Do you not know that you are the temple of God and that the Spirit of God dwells in you? 17 If anyone [b]defiles the temple of God, God will destroy him. For the temple of God is holy, which temple you are.

Avoid Worldly Wisdom

18 (S)Let no one deceive himself. If anyone among you seems to be wise in this age, let him become a fool that he may become wise. 19 For the wisdom of this world is foolishness with God. For it is written, (T)“He catches the wise in their own craftiness”; 20 and again, (U)“The Lord knows the thoughts of the wise, that they are futile.” 21 Therefore let no one boast in men. For (V)all things are yours: 22 whether Paul or Apollos or Cephas, or the world or life or death, or things present or things to come—all are yours. 23 And (W)you are Christ’s, and Christ is God’s.

Footnotes

  1. 1 Corinthians 3:3 Lit. walking according to man
  2. 1 Corinthians 3:17 destroys

Divisions in the Church

But I, brothers,[a] could not address you as (A)spiritual people, but as (B)people of the flesh, as (C)infants in Christ. (D)I fed you with milk, not solid food, for (E)you were not ready for it. And even now you are not yet ready, for you are still of the flesh. For while there is (F)jealousy and strife among you, are you not of the flesh and behaving only in a human way? For (G)when one says, “I follow Paul,” and another, “I follow Apollos,” (H)are you not being merely human?

What then is Apollos? What is Paul? (I)Servants through whom you believed, (J)as the Lord assigned to each. (K)I planted, (L)Apollos watered, (M)but God gave the growth. So (N)neither he who plants nor he who waters is anything, but only God who gives the growth. He who plants and he who waters are one, and each (O)will receive his wages according to his labor. For we are (P)God's fellow workers. You are God's field, (Q)God's building.

10 (R)According to the grace of God given to me, like a skilled[b] master builder I laid a (S)foundation, and (T)someone else is building upon it. Let each one take care how he builds upon it. 11 For no one can lay a (U)foundation other (V)than that which is laid, (W)which is Jesus Christ. 12 Now if anyone builds on the foundation with gold, silver, precious stones, wood, hay, straw— 13 (X)each one's work will become manifest, for the Day will disclose it, because it will be revealed (Y)by fire, and (Z)the fire will test what sort of work each one has done. 14 If the work that anyone has built on the foundation survives, (AA)he will receive a reward. 15 If anyone's work is burned up, he will suffer loss, though he himself will be saved, (AB)but only as through fire.

16 (AC)Do you not know that you[c] are God's temple and that God's Spirit dwells in you? 17 If anyone destroys God's temple, God will destroy him. For (AD)God's temple is holy, and you are that temple.

18 (AE)Let no one deceive himself. (AF)If anyone among you thinks that he is wise in this age, let him become a fool that he may become wise. 19 For (AG)the wisdom of this world is folly with God. For it is written, (AH)“He catches the wise in their craftiness,” 20 and again, (AI)“The Lord knows the thoughts of the wise, that they are futile.” 21 So (AJ)let no one boast in men. For (AK)all things are yours, 22 whether Paul or Apollos or Cephas or the world or life or death or the present or the future—all are yours, 23 and (AL)you are Christ's, and (AM)Christ is God's.

Footnotes

  1. 1 Corinthians 3:1 Or brothers and sisters
  2. 1 Corinthians 3:10 Or wise
  3. 1 Corinthians 3:16 The Greek for you is plural in verses 16 and 17