1 Akorinto 3
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Mpingo ndi Atsogoleri Ake
3 Ndipo abale sindikanakuyankhulani ngati auzimu koma adziko lapansi, makanda chabe mwa Khristu. 2 Ndinakupatsani mkaka osati chakudya cholimba pakuti munali musanakonzeke kuchilandira. Zoonadi, simunakonzekebe. 3 Mukanali adziko lapansi. Pakuti pakati panu pali kaduka ndi kukangana, kodi si inu a dziko lapansi? Kodi simukuchita ngati anthu wamba? 4 Pamene wina anena kuti, “Ine ndimatsatira Paulo,” ndipo wina akuti, “Ine ndimatsatira Apolo,” Kodi si inu akunja?
5 Ndiponso kodi Apolo ndi ndani? Nanga Paulo ndi ndani? Otumikira chabe, omwe kudzera mwa iwo inu munakhulupirira monga Ambuye anawagawira aliyense ntchito yake. 6 Ine ndinadzala mbewu, Apolo anayithirira, koma Mulungu ndiye anayikulitsa. 7 Choncho kuphatikiza iye wodzala ndi iye wothirira, onse sali kanthu, koma Mulungu yekha amene amakulitsa zinthu. 8 Munthu wodzala ndi munthu wothirira ali ndi cholinga chimodzi, ndipo aliyense adzapatsidwa mphotho molingana ndi ntchito yake. 9 Pakuti ife ndife antchito anzake a Mulungu; inu ndinu munda wa Mulungu, Nyumba ya Mulungu.
10 Mwachisomo chimene Mulungu wandipatsa, ine ndinayika maziko monga mmisiri waluntha, ndipo ena akumangapo. Koma aliyense ayenera kuchenjera mmene akumangira. 11 Pakuti wina sangayikenso maziko ena oposera amene anakhazikitsidwa kale, amene ndi Yesu Khristu. 12 Ngati munthu aliyense amanga pa maziko awa pogwiritsa ntchito golide, siliva, miyala yamtengowapatali, milimo yamitengo, tsekera kapena udzu, 13 ntchito yake idzaonekera pamene Tsiku la chiweruzo lidzazionetsa poyera. Tsikulo lidzafika ndi moto, ndipo motowo ndi umene udzayesa ntchito ya munthu aliyense. 14 Ngati zimene zamangidwazo sizidzagwa, adzalandira mphotho yake. 15 Ndipo ngati zidzanyeke ndi moto, sadzalandira mphotho koma iye mwini adzapulumukabe, koma monga ngati munthu amene wapulumuka mʼmoto.
16 Kodi inu simukudziwa kuti ndinu Nyumba ya Mulungu ndipo kuti Mzimu wa Mulungu amakhala mwa inu? 17 Ngati wina aliyense awononga Nyumba ya Mulunguyo, Mulungu nayenso adzamuwononga ameneyo; popeza Nyumba ya Mulungu ndi yopatulika ndipo Nyumbayo ndi inu amene.
18 Choncho musadzinyenge. Ngati wina wa inu akuganiza kuti ndi wanzeru pa mulingo wa mʼbado uno, ayenera kukhala “wopusa” kuti athe kukhala wanzeru. 19 Pakuti nzeru ya dziko lapansi ndi yopusa pamaso pa Mulungu. Monga kwalembedwera kuti, “Iye amakola anthu ochenjera mu msampha wa kuchenjera kwawo,” 20 ndiponso, “Ambuye amadziwa kuti maganizo a wanzeru ndi opandapake.” 21 Choncho, wina asanyadire anthu chabe! Zonse ndi zanu, 22 kaya Paulo kapena Apolo kapena Kefa kapena dziko lapansi, kapena moyo, kapena imfa, kapena tsopano, kapena mʼtsogolo, zonse ndi zanu, 23 ndipo inu ndinu a Khristu, ndipo Khristu ndi wa Mulungu.
1 Corinthians 3
EasyEnglish Bible
God wants his people to grow as believers
3 My Christian friends, I could not teach you as I would teach people who have God's Spirit. I had to teach you as people who belong only to this world. You were like little children who could not understand the message about Christ very well. 2 I had to teach you things that were easy to understand, like a mother gives milk to a baby. You were not yet ready to receive proper food. And you are still not ready to receive God's complete message! 3 You still do what your human nature wants to do. You are jealous of each other, and you quarrel with each other. Yes! This shows that you do what your human nature wants to do. You live like people who do not know God. 4 Some of you say, ‘Paul is my leader.’ And other people say, ‘Apollos is my leader.’ When you speak like that, you are talking like people who belong to this world.
5 Is Apollos important? Is Paul important? No! We are God's servants. We told you God's good news and you believed it. Each of us is doing the job which the Lord has given to us. 6 When I told you God's good news, I was like someone who planted seeds. Then Apollos was like someone who gave water to the young plants. But it was God who caused everything to grow. 7 The person who plants the seeds is not important. The person who gives water to the plants is not important. The important person is God, because he causes everything to grow. 8 The person who plants and the person who gives water both have the same purpose. God will pay each person what is right for their work. 9 Apollos and I work together as God's servants. You are like God's field that we work in.
You are also like a building that belongs to God. 10 I am like a good builder. God has given that job to me and he has helped me to do it well. I was the person who built the foundation. Now other people are building on that foundation.[a] But each person must be careful how he builds. 11 God has already put Jesus Christ as the only foundation of this building. So nobody can put any other foundation there.
12 People may build on this foundation with gold, silver or valuable stones. Or they may build on it with wood, dry grass or leaves. 13 One day, God will show clearly how good each builder's work is. God will put each person's work into a fire on that great day.[b] The fire will show whether their work is good or bad. 14 If the fire does not destroy the work, then that builder will receive good things from God. 15 But if the fire destroys a builder's work, that person will lose everything. The person himself will be safe. But he will be like someone who has run through the fire to a safe place.
16 You surely know that you are like God's special house. As God's people, God's Spirit lives in you. 17 If anyone destroys God's special house, then God will destroy that person. And you are like that house. You belong to God in a special way.
18 Be careful! Do not think that you are better than you really are. Maybe you think that you are wise, like people today want to be wise. But if you want to become truly wise, be ready for other people to think that you are a fool. 19 People in this world think that some people are wise. But God thinks that those wise people are fools. It says in the Bible:
‘God causes the clever thoughts of wise people to confuse them.’[c]
20 In another place, the Bible says:
‘The Lord knows that the thoughts of wise people have no value.’[d]
21 Because of that, you should not be proud of any human leader. All leaders are there to serve you, as God's people. 22 Do not be proud of Paul, Apollos or Peter. We belong to you. All of this world, and life and death belong to you. The things of today and tomorrow belong to you. Everything belongs to you, 23 you belong to Christ, and Christ belongs to God.
1 Corinthians 3
King James Version
3 And I, brethren, could not speak unto you as unto spiritual, but as unto carnal, even as unto babes in Christ.
2 I have fed you with milk, and not with meat: for hitherto ye were not able to bear it, neither yet now are ye able.
3 For ye are yet carnal: for whereas there is among you envying, and strife, and divisions, are ye not carnal, and walk as men?
4 For while one saith, I am of Paul; and another, I am of Apollos; are ye not carnal?
5 Who then is Paul, and who is Apollos, but ministers by whom ye believed, even as the Lord gave to every man?
6 I have planted, Apollos watered; but God gave the increase.
7 So then neither is he that planteth any thing, neither he that watereth; but God that giveth the increase.
8 Now he that planteth and he that watereth are one: and every man shall receive his own reward according to his own labour.
9 For we are labourers together with God: ye are God's husbandry, ye are God's building.
10 According to the grace of God which is given unto me, as a wise masterbuilder, I have laid the foundation, and another buildeth thereon. But let every man take heed how he buildeth thereupon.
11 For other foundation can no man lay than that is laid, which is Jesus Christ.
12 Now if any man build upon this foundation gold, silver, precious stones, wood, hay, stubble;
13 Every man's work shall be made manifest: for the day shall declare it, because it shall be revealed by fire; and the fire shall try every man's work of what sort it is.
14 If any man's work abide which he hath built thereupon, he shall receive a reward.
15 If any man's work shall be burned, he shall suffer loss: but he himself shall be saved; yet so as by fire.
16 Know ye not that ye are the temple of God, and that the Spirit of God dwelleth in you?
17 If any man defile the temple of God, him shall God destroy; for the temple of God is holy, which temple ye are.
18 Let no man deceive himself. If any man among you seemeth to be wise in this world, let him become a fool, that he may be wise.
19 For the wisdom of this world is foolishness with God. For it is written, He taketh the wise in their own craftiness.
20 And again, The Lord knoweth the thoughts of the wise, that they are vain.
21 Therefore let no man glory in men. For all things are your's;
22 Whether Paul, or Apollos, or Cephas, or the world, or life, or death, or things present, or things to come; all are your's;
23 And ye are Christ's; and Christ is God's.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
EasyEnglish Bible Copyright © MissionAssist 2019 - Charitable Incorporated Organisation 1162807. Used by permission. All rights reserved.