Mateyu 3
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Yohane Mʼbatizi
3 Mʼmasiku amenewo, Yohane Mʼbatizi anadza nalalikira mʼchipululu cha Yudeya 2 kuti, “Tembenukani mtima chifukwa ufumu wakumwamba wayandikira.” 3 Uyu ndi amene mneneri Yesaya ananena za iye kuti,
“Mawu a wofuwula mʼchipululu,
‘Konzani njira ya Ambuye,
wongolani njira zake.’ ”
4 Zovala za Yohane zinali zopangidwa ndi ubweya wa ngamira, ndipo amamangira lamba wachikopa mʼchiwuno mwake. Chakudya chake chinali dzombe ndi uchi wa kuthengo. 5 Anthu ankapita kwa iye kuchokera ku Yerusalemu ndi ku Yudeya konse ndi ku madera onse a Yorodani. 6 Ndipo akavomereza machimo awo ankabatizidwa mu mtsinje wa Yorodani.
7 Koma iye ataona Afarisi ndi Asaduki ambiri akubwera kumene ankabatiza, anawawuza kuti, “Ana a njoka inu! Ndani anakuchenjezani kuthawa mkwiyo umene ukubwera? 8 Onetsani chipatso cha kutembenuka mtima. 9 Ndipo musaganize ndi kunena mwa inu nokha kuti, ‘Tili nawo abambo athu Abrahamu.’ Ndinena kwa inu kuti Mulungu akhoza kusandutsa miyala iyi kukhala ana a Abrahamu. 10 Tikukamba pano nkhwangwa yayikidwa kale pa mizu ya mitengo, ndipo mtengo umene subala chipatso chabwino udulidwa ndi kuponyedwa pa moto.
11 “Ine ndikubatizani ndi madzi kusonyeza kutembenuka mtima. Koma pambuyo panga akubwera wina amene ali ndi mphamvu kuposa ine, amene sindiyenera kunyamula nsapato zake. Iyeyu adzakubatizani ndi Mzimu Woyera ndi moto. 12 Mʼdzanja lake muli chopetera ndipo adzayeretsa popunthirapo pake nadzathira tirigu wake mʼnkhokwe ndi kutentha zotsalira zonse ndi moto wosazima.”
Kubatizidwa kwa Yesu
13 Pamenepo Yesu anabwera kuchokera ku Galileya kudzabatizidwa ndi Yohane mu mtsinje wa Yorodani. 14 Koma Yohane anayesetsa kumukanira nati, “Ndiyenera kubatizidwa ndi Inu, bwanji Inu mubwera kwa ine?”
15 Yesu anayankha kuti, “Zibatero tsopano, ndi koyenera kwa ife kuchita zimenezi kukwaniritsa chilungamo chonse.” Ndipo Yohane anavomera.
16 Yesu atangobatizidwa, nthawi yomweyo potuluka mʼmadzi, kumwamba kunatsekuka ndipo taonani, Mzimu wa Mulungu anatsika ngati nkhunda natera pa Iye. 17 Ndipo mawu anamveka kuchokera kumwamba kuti, “Uyu ndiye mwana wanga wokondedwa amene ndikondwera naye.”
馬 太 福 音 3
Chinese New Testament: Easy-to-Read Version
施洗者约翰为耶稣铺路
3 当时,施洗者约翰在犹太的荒原上传教。 2 他对人们说∶“悔改吧,天国很近了。 [a]” 3 约翰就是先知以赛亚所说的那个人。先知说:
“旷野里有个呼唤着的人,
‘为主准备好道路。
修直他的路。’” (A)
4 约翰身穿骆驼毛织成的衣服,腰系皮带,吃的是蝗虫和野蜜。 5 人们纷纷离开耶路撒冷、犹太各地和约旦河一带所有地区,来到约翰那里。 6 他们承认自己的罪,并在约旦河里接受了约翰的洗礼。
7 许多法利赛人和撒都该人也来接受约翰的洗礼,约翰看到他们,说道∶“你们这些毒蛇,谁警告过你们去逃避即将来临的上帝的审判呢? 8 改变你们的内心吧!通过你们的生活方式来表明你们已经改变了。 9 我知道你们在想什么,你们想说:‘但是,亚伯拉罕是我们的祖先!’这毫无意义。我告诉你们,上帝可以让这些石头都变成亚伯拉罕的子孙! 10 现在砍树的斧头已经准备好了,每棵不结好果子的树 [b]都将被砍倒,扔进火里。
11 我用水给你们施洗礼来表示你们的悔改。但是,在我之后来的那位,他比我更强大,我甚至都不配当给他脱鞋的奴仆。他将用圣灵和火给你们施洗礼。 12 他手里拿着簸谷叉,他将清理谷场,把麦粒收进粮仓,把麦麸 [c]用不灭的火烧掉。”
耶稣受洗
13 然后,耶稣从加利利来到约旦河。他走到约翰面前,请约翰为他施洗礼。 14 但是约翰说他不配为耶稣施洗礼,他说∶“我应该让您给我洗礼,您怎么反而来找我呢?” 15 耶稣回答说∶“现在就照上帝的方式来做吧,凡是对的,我们都应当做。”约翰这才同意为耶稣施洗礼。
16 这样,耶稣接受了洗礼。就在耶稣从水里站出来的时候,天为他豁然敞开,耶稣看见上帝的灵像鸽子一样降落在他身上。 17 一个来自天堂的声音说∶“这是我的爱子,他令我非常喜悦!”
Footnotes
- 馬 太 福 音 3:2 很近了: 或“即将来临” 或“已来临。”
- 馬 太 福 音 3:10 树: 即不接受耶稣的人,他们会像树一样被砍倒。不结善果的树指不信耶稣的人。
- 馬 太 福 音 3:12 麦粒指好人: 麦麸指坏人。这里的意思是耶稣把好人和坏人分开。
Matthew 3
New International Version
John the Baptist Prepares the Way(A)
3 In those days John the Baptist(B) came, preaching in the wilderness of Judea 2 and saying, “Repent, for the kingdom of heaven(C) has come near.” 3 This is he who was spoken of through the prophet Isaiah:
“A voice of one calling in the wilderness,
‘Prepare the way for the Lord,
make straight paths for him.’”[a](D)
4 John’s(E) clothes were made of camel’s hair, and he had a leather belt around his waist.(F) His food was locusts(G) and wild honey. 5 People went out to him from Jerusalem and all Judea and the whole region of the Jordan. 6 Confessing their sins, they were baptized(H) by him in the Jordan River.
7 But when he saw many of the Pharisees and Sadducees coming to where he was baptizing, he said to them: “You brood of vipers!(I) Who warned you to flee from the coming wrath?(J) 8 Produce fruit in keeping with repentance.(K) 9 And do not think you can say to yourselves, ‘We have Abraham as our father.’(L) I tell you that out of these stones God can raise up children for Abraham. 10 The ax is already at the root of the trees, and every tree that does not produce good fruit will be cut down and thrown into the fire.(M)
11 “I baptize you with[b] water for repentance.(N) But after me comes one who is more powerful than I, whose sandals I am not worthy to carry. He will baptize you with[c] the Holy Spirit(O) and fire.(P) 12 His winnowing fork is in his hand, and he will clear his threshing floor, gathering his wheat into the barn and burning up the chaff with unquenchable fire.”(Q)
The Baptism of Jesus(R)
13 Then Jesus came from Galilee to the Jordan to be baptized by John.(S) 14 But John tried to deter him, saying, “I need to be baptized by you, and do you come to me?”
15 Jesus replied, “Let it be so now; it is proper for us to do this to fulfill all righteousness.” Then John consented.
16 As soon as Jesus was baptized, he went up out of the water. At that moment heaven was opened,(T) and he saw the Spirit of God(U) descending like a dove and alighting on him. 17 And a voice from heaven(V) said, “This is my Son,(W) whom I love; with him I am well pleased.”(X)
Footnotes
- Matthew 3:3 Isaiah 40:3
- Matthew 3:11 Or in
- Matthew 3:11 Or in
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Copyright © 2004 by World Bible Translation Center
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.
