Add parallel Print Page Options

Yohane Mʼbatizi

Mʼmasiku amenewo, Yohane Mʼbatizi anadza nalalikira mʼchipululu cha Yudeya kuti, “Tembenukani mtima chifukwa ufumu wakumwamba wayandikira.” Uyu ndi amene mneneri Yesaya ananena za iye kuti,

“Mawu a wofuwula mʼchipululu,
‘Konzani njira ya Ambuye,
    wongolani njira zake.’ ”

Zovala za Yohane zinali zopangidwa ndi ubweya wa ngamira, ndipo amamangira lamba wachikopa mʼchiwuno mwake. Chakudya chake chinali dzombe ndi uchi wa kuthengo. Anthu ankapita kwa iye kuchokera ku Yerusalemu ndi ku Yudeya konse ndi ku madera onse a Yorodani. Ndipo akavomereza machimo awo ankabatizidwa mu mtsinje wa Yorodani.

Koma iye ataona Afarisi ndi Asaduki ambiri akubwera kumene ankabatiza, anawawuza kuti, “Ana a njoka inu! Ndani anakuchenjezani kuthawa mkwiyo umene ukubwera? Onetsani chipatso cha kutembenuka mtima. Ndipo musaganize ndi kunena mwa inu nokha kuti, ‘Tili nawo abambo athu Abrahamu.’ Ndinena kwa inu kuti Mulungu akhoza kusandutsa miyala iyi kukhala ana a Abrahamu. 10 Tikukamba pano nkhwangwa yayikidwa kale pa mizu ya mitengo, ndipo mtengo umene subala chipatso chabwino udulidwa ndi kuponyedwa pa moto.

11 “Ine ndikubatizani ndi madzi kusonyeza kutembenuka mtima. Koma pambuyo panga akubwera wina amene ali ndi mphamvu kuposa ine, amene sindiyenera kunyamula nsapato zake. Iyeyu adzakubatizani ndi Mzimu Woyera ndi moto. 12 Mʼdzanja lake muli chopetera ndipo adzayeretsa popunthirapo pake nadzathira tirigu wake mʼnkhokwe ndi kutentha zotsalira zonse ndi moto wosazima.”

Kubatizidwa kwa Yesu

13 Pamenepo Yesu anabwera kuchokera ku Galileya kudzabatizidwa ndi Yohane mu mtsinje wa Yorodani. 14 Koma Yohane anayesetsa kumukanira nati, “Ndiyenera kubatizidwa ndi Inu, bwanji Inu mubwera kwa ine?”

15 Yesu anayankha kuti, “Zibatero tsopano, ndi koyenera kwa ife kuchita zimenezi kukwaniritsa chilungamo chonse.” Ndipo Yohane anavomera.

16 Yesu atangobatizidwa, nthawi yomweyo potuluka mʼmadzi, kumwamba kunatsekuka ndipo taonani, Mzimu wa Mulungu anatsika ngati nkhunda natera pa Iye. 17 Ndipo mawu anamveka kuchokera kumwamba kuti, “Uyu ndiye mwana wanga wokondedwa amene ndikondwera naye.”

施洗者约翰为耶稣铺路

当时,施洗者约翰在犹太的荒原上传教。 他对人们说∶“悔改吧,天国很近了。 [a] 约翰就是先知以赛亚所说的那个人。先知说:

“旷野里有个呼唤着的人,
‘为主准备好道路。
修直他的路。’” (A)

约翰身穿骆驼毛织成的衣服,腰系皮带,吃的是蝗虫和野蜜。 人们纷纷离开耶路撒冷、犹太各地和约旦河一带所有地区,来到约翰那里。 他们承认自己的罪,并在约旦河里接受了约翰的洗礼。

许多法利赛人和撒都该人也来接受约翰的洗礼,约翰看到他们,说道∶“你们这些毒蛇,谁警告过你们去逃避即将来临的上帝的审判呢? 改变你们的内心吧!通过你们的生活方式来表明你们已经改变了。 我知道你们在想什么,你们想说:‘但是,亚伯拉罕是我们的祖先!’这毫无意义。我告诉你们,上帝可以让这些石头都变成亚伯拉罕的子孙! 10 现在砍树的斧头已经准备好了,每棵不结好果子的树 [b]都将被砍倒,扔进火里。

11 我用水给你们施洗礼来表示你们的悔改。但是,在我之后来的那位,他比我更强大,我甚至都不配当给他脱鞋的奴仆。他将用圣灵和火给你们施洗礼。 12 他手里拿着簸谷叉,他将清理谷场,把麦粒收进粮仓,把麦麸 [c]用不灭的火烧掉。”

耶稣受洗

13 然后,耶稣从加利利来到约旦河。他走到约翰面前,请约翰为他施洗礼。 14 但是约翰说他不配为耶稣施洗礼,他说∶“我应该让您给我洗礼,您怎么反而来找我呢?” 15 耶稣回答说∶“现在就照上帝的方式来做吧,凡是对的,我们都应当做。”约翰这才同意为耶稣施洗礼。

16 这样,耶稣接受了洗礼。就在耶稣从水里站出来的时候,天为他豁然敞开,耶稣看见上帝的灵像鸽子一样降落在他身上。 17 一个来自天堂的声音说∶“这是我的爱子,他令我非常喜悦!”

Footnotes

  1. 馬 太 福 音 3:2 很近了: 或“即将来临” 或“已来临。”
  2. 馬 太 福 音 3:10 树: 即不接受耶稣的人,他们会像树一样被砍倒。不结善果的树指不信耶稣的人。
  3. 馬 太 福 音 3:12 麦粒指好人: 麦麸指坏人。这里的意思是耶稣把好人和坏人分开。

In those days came John the Baptist, preaching in the wilderness of Judaea,

And saying, Repent ye: for the kingdom of heaven is at hand.

For this is he that was spoken of by the prophet Esaias, saying, The voice of one crying in the wilderness, Prepare ye the way of the Lord, make his paths straight.

And the same John had his raiment of camel's hair, and a leathern girdle about his loins; and his meat was locusts and wild honey.

Then went out to him Jerusalem, and all Judaea, and all the region round about Jordan,

And were baptized of him in Jordan, confessing their sins.

But when he saw many of the Pharisees and Sadducees come to his baptism, he said unto them, O generation of vipers, who hath warned you to flee from the wrath to come?

Bring forth therefore fruits meet for repentance:

And think not to say within yourselves, We have Abraham to our father: for I say unto you, that God is able of these stones to raise up children unto Abraham.

10 And now also the axe is laid unto the root of the trees: therefore every tree which bringeth not forth good fruit is hewn down, and cast into the fire.

11 I indeed baptize you with water unto repentance. but he that cometh after me is mightier than I, whose shoes I am not worthy to bear: he shall baptize you with the Holy Ghost, and with fire:

12 Whose fan is in his hand, and he will throughly purge his floor, and gather his wheat into the garner; but he will burn up the chaff with unquenchable fire.

13 Then cometh Jesus from Galilee to Jordan unto John, to be baptized of him.

14 But John forbad him, saying, I have need to be baptized of thee, and comest thou to me?

15 And Jesus answering said unto him, Suffer it to be so now: for thus it becometh us to fulfil all righteousness. Then he suffered him.

16 And Jesus, when he was baptized, went up straightway out of the water: and, lo, the heavens were opened unto him, and he saw the Spirit of God descending like a dove, and lighting upon him:

17 And lo a voice from heaven, saying, This is my beloved Son, in whom I am well pleased.