詩篇 2
Chinese Union Version Modern Punctuation (Traditional)
耶和華之受膏者為王
2 外邦為什麼爭鬧,萬民為什麼謀算虛妄的事?
2 世上的君王一齊起來,臣宰一同商議,要抵擋耶和華並他的受膏者,
3 說:「我們要掙開他們的捆綁,脫去他們的繩索!」
4 那坐在天上的必發笑,主必嗤笑他們。
5 那時,他要在怒中責備他們,在烈怒中驚嚇他們,
6 說:「我已經立我的君在錫安我的聖山上了。」
7 受膏者說:「我要傳聖旨。耶和華曾對我說:『你是我的兒子,我今日生你。
8 你求我,我就將列國賜你為基業,將地極賜你為田產。
9 你必用鐵杖打破他們,你必將他們如同窯匠的瓦器摔碎。』」
10 現在你們君王應當醒悟,你們世上的審判官該受管教!
11 當存畏懼侍奉耶和華,又當存戰兢而快樂。
12 當以嘴親子,恐怕他發怒,你們便在道中滅亡,因為他的怒氣快要發作。凡投靠他的,都是有福的!
Masalimo 2
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
2 Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu?
Akonzekeranji zopanda pake anthu?
2 Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo;
ndipo olamulira asonkhana pamodzi
kulimbana ndi Ambuye
ndi wodzozedwa wakeyo.
3 Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo
ndipo titaye zingwe zawo.”
4 Wokhala mmwamba akuseka;
Ambuye akuwanyoza iwowo.
5 Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake
ndi kuwaopseza mu ukali wake, kunena kuti,
6 “Ine ndakhazikitsa mfumu yanga
pa Ziyoni, phiri langa loyera.”
7 Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula:
Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga;
lero Ine ndakhala Atate ako.
8 Tandipempha,
ndipo ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ikhale cholowa chako;
malekezero a dziko lapansi kuti akhale chuma chako.
9 Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo;
udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.”
10 Kotero, inu mafumu, chenjerani;
chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi.
11 Tumikirani Yehova mwa mantha
ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.
12 Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye;
kuti mungawonongedwe mʼnjira zanu,
pakuti ukali wake utha kuuka mʼkanthawi kochepa.
Odala ndi onse amene amathawira kwa Iye.
Psalm 2
New International Version
Psalm 2
1 Why do the nations conspire[a]
and the peoples plot(A) in vain?
2 The kings(B) of the earth rise up
and the rulers band together
against the Lord and against his anointed,(C) saying,
3 “Let us break their chains(D)
and throw off their shackles.”(E)
4 The One enthroned(F) in heaven laughs;(G)
the Lord scoffs at them.
5 He rebukes them in his anger(H)
and terrifies them in his wrath,(I) saying,
6 “I have installed my king(J)
on Zion,(K) my holy mountain.(L)”
7 I will proclaim the Lord’s decree:
He said to me, “You are my son;(M)
today I have become your father.(N)
8 Ask me,
and I will make the nations(O) your inheritance,(P)
the ends of the earth(Q) your possession.
9 You will break them with a rod of iron[b];(R)
you will dash them to pieces(S) like pottery.(T)”
10 Therefore, you kings, be wise;(U)
be warned, you rulers(V) of the earth.
11 Serve the Lord with fear(W)
and celebrate his rule(X) with trembling.(Y)
12 Kiss his son,(Z) or he will be angry
and your way will lead to your destruction,
for his wrath(AA) can flare up in a moment.
Blessed(AB) are all who take refuge(AC) in him.
Copyright © 2011 by Global Bible Initiative
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.
