詩篇 2
Chinese Union Version Modern Punctuation (Traditional)
耶和華之受膏者為王
2 外邦為什麼爭鬧,萬民為什麼謀算虛妄的事?
2 世上的君王一齊起來,臣宰一同商議,要抵擋耶和華並他的受膏者,
3 說:「我們要掙開他們的捆綁,脫去他們的繩索!」
4 那坐在天上的必發笑,主必嗤笑他們。
5 那時,他要在怒中責備他們,在烈怒中驚嚇他們,
6 說:「我已經立我的君在錫安我的聖山上了。」
7 受膏者說:「我要傳聖旨。耶和華曾對我說:『你是我的兒子,我今日生你。
8 你求我,我就將列國賜你為基業,將地極賜你為田產。
9 你必用鐵杖打破他們,你必將他們如同窯匠的瓦器摔碎。』」
10 現在你們君王應當醒悟,你們世上的審判官該受管教!
11 當存畏懼侍奉耶和華,又當存戰兢而快樂。
12 當以嘴親子,恐怕他發怒,你們便在道中滅亡,因為他的怒氣快要發作。凡投靠他的,都是有福的!
Masalimo 2
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
2 Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu?
Akonzekeranji zopanda pake anthu?
2 Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo;
ndipo olamulira asonkhana pamodzi
kulimbana ndi Ambuye
ndi wodzozedwa wakeyo.
3 Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo
ndipo titaye zingwe zawo.”
4 Wokhala mmwamba akuseka;
Ambuye akuwanyoza iwowo.
5 Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake
ndi kuwaopseza mu ukali wake, kunena kuti,
6 “Ine ndakhazikitsa mfumu yanga
pa Ziyoni, phiri langa loyera.”
7 Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula:
Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga;
lero Ine ndakhala Atate ako.
8 Tandipempha,
ndipo ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ikhale cholowa chako;
malekezero a dziko lapansi kuti akhale chuma chako.
9 Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo;
udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.”
10 Kotero, inu mafumu, chenjerani;
chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi.
11 Tumikirani Yehova mwa mantha
ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.
12 Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye;
kuti mungawonongedwe mʼnjira zanu,
pakuti ukali wake utha kuuka mʼkanthawi kochepa.
Odala ndi onse amene amathawira kwa Iye.
Copyright © 2011 by Global Bible Initiative
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.