Add parallel Print Page Options

10 Anthu a imvi ndi okalamba ali mbali yathu,
    anthu amvulazakale kupambana abambo ako.
11 Kodi mawu otonthoza mtima ochokera kwa Mulungu sakukukwanira,
    mawu oyankhula mofatsawa kwa iwe?
12 Chifukwa chiyani ukupsa mtima,
    ndipo chifukwa chiyani ukutuzula maso ako,

Read full chapter