Add parallel Print Page Options

10 Anthu a imvi ndi okalamba ali mbali yathu,
    anthu amvulazakale kupambana abambo ako.
11 Kodi mawu otonthoza mtima ochokera kwa Mulungu sakukukwanira,
    mawu oyankhula mofatsawa kwa iwe?
12 Chifukwa chiyani ukupsa mtima,
    ndipo chifukwa chiyani ukutuzula maso ako,

Read full chapter

10 The gray-haired and the aged(A) are on our side,
    men even older than your father.(B)
11 Are God’s consolations(C) not enough for you,
    words(D) spoken gently to you?(E)
12 Why has your heart(F) carried you away,
    and why do your eyes flash,

Read full chapter