玛拉基书 4
Chinese Contemporary Bible (Simplified)
耶和华的日子
4 “万军之耶和华说,‘那日要来临了,就像烧红的火炉,所有狂妄自大、作恶多端的人都要像碎秸一样被火烧尽,连根带枝,荡然无存。 2 但必有公义的太阳为你们这些敬畏我名的人升起,它的光芒有医治的能力。你们必像栏中出来的牛犊一样欢欣跳跃。 3 到我所定的日子,你们必践踏恶人,他们必成为你们脚下的尘土。’这是万军之耶和华说的。
4 “你们要记住我仆人摩西的律法,就是我在何烈山借着他传给以色列人的律例和典章。
5 “看啊,在耶和华那伟大而可畏的日子来临以前,我必差遣以利亚先知到你们那里。 6 他必使父亲的心转向儿女,儿女的心转向父亲,免得我来用咒诅毁灭这地方。”
瑪拉基書 4
Chinese Contemporary Bible (Traditional)
耶和華的日子
4 「萬軍之耶和華說,『那日要來臨了,就像燒紅的火爐,所有狂妄自大、作惡多端的人都要像碎稭一樣被火燒盡,連根帶枝,蕩然無存。 2 但必有公義的太陽為你們這些敬畏我名的人升起,它的光芒有醫治的能力。你們必像欄中出來的牛犢一樣歡欣跳躍。 3 到我所定的日子,你們必踐踏惡人,他們必成為你們腳下的塵土。』這是萬軍之耶和華說的。
4 「你們要記住我僕人摩西的律法,就是我在何烈山藉著他傳給以色列人的律例和典章。
5 「看啊,在耶和華那偉大而可畏的日子來臨以前,我必差遣以利亞先知到你們那裡。 6 他必使父親的心轉向兒女,兒女的心轉向父親,免得我來用咒詛毀滅這地方。」
Malaki 4
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Tsiku la Yehova
4 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ndithu tsiku likubwera; lidzayaka ngati ngʼanjo. Anthu onse odzikuza, ndi aliyense ochita zoyipa adzapsa ngati chiputu, ndipo pa tsiku limene likubweralo adzapserera ndi moto. Sipadzatsalira muzu kapena nthambi. 2 Koma inu amene mumaopa dzina langa, dzuwa lachilungamo lidzakutulukirani lili ndi kuwala kokuchiritsani. Ndipo inu mudzatuluka ndi kulumphalumpha ngati ana angʼombe amene atulutsidwa mʼkhola. 3 Tsiku limenelo inu mudzapondereza anthu oyipa; adzakhala phulusa ku mapazi anu pa tsiku limene Ine ndidzachite zinthu zimenezi,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
4 Kumbukirani zophunzitsa za mtumiki wanga Mose, malamulo ndi malangizo amene ndinamupatsa pa Horebu kuti awuze Aisraeli onse.
5 “Taonani, ndidzakutumizirani mneneri Eliya lisanafike tsiku lalikulu ndi loopsa la Yehova. 6 Iye adzabweza mitima ya makolo kwa ana awo, ndi mitima ya ana kwa makolo awo. Kupanda kutero ndidzabwera kudzakantha dziko lanu ndi temberero.”
Chinese Contemporary Bible Copyright © 1979, 2005, 2007, 2011 by Biblica® Used by permission. All rights reserved worldwide.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Copyright © 2004 by World Bible Translation Center