Add parallel Print Page Options

亚伯拉罕与亚比米勒

20 亚伯拉罕从那里迁到南地,就住在加低斯和书珥中间。亚伯拉罕寄居在基拉耳的时候, 曾经提到他的妻子撒拉说:“她是我的妹妹。”于是基拉耳王亚比米勒派人来把撒拉取了去。 当夜, 神在梦中来到亚比米勒那里,对他说:“你该死,因为你接来的那女人,是个有夫之妇。” 亚比米勒还没有亲近撒拉,所以他说:“我主啊,连正义的人你也要杀害吗? 那人岂不是自己对我说:‘她是我的妹妹’吗?就是那女人自己也说:‘他是我的哥哥’。我作这事,是手洁心清的。”  神在梦中对他说:“我也知道你作这事,是问心无愧的,所以我也阻止你,免得你得罪我。因此我不容许你接触她。 现在你要把那人的妻子还给他,因为他是先知,他要为你祷告,你才可以存活。你若不还给他,你当知道,你和所有属你的,都死定了。”

亚比米勒清早起来,召了他的众臣仆来,把这一切都说给他们听,以致他们都很惧怕。 亚比米勒把亚伯拉罕召了来,对他说:“你为甚么向我们这样行呢?我在甚么事上得罪了你,以致你给我和我的国带来这个大罪呢?你对我作了不应该作的事。” 10 亚比米勒又对亚伯拉罕说:“你为了甚么缘故要这样作呢?” 11 亚伯拉罕回答:“因为我以为这地方必定没有敬畏 神的人,他们会因我妻子的缘故杀我。 12 何况她也实在是我的妹妹;她原是我同父异母的妹妹,后来作了我的妻子。 13  神叫我离开我父家,在外飘流的时候,我对她说:‘我们无论到甚么地方去,你都要对人说:“他是我的哥哥。”这就是你待我的恩情了。’” 14 亚比米勒取了些牛羊、仆婢,送给亚伯拉罕,又把亚伯拉罕的妻子撒拉还给他。 15 亚比米勒说:“看哪,我的国土都在你面前,你喜欢哪里,就住在哪里吧。”

16 他又对撒拉说:“看哪,我给了你哥哥一千银子,作你在全家人面前的遮羞钱(“遮羞钱”直译是“眼睛的遮盖”;原文意思不确定;或译:“清白的证明”)。这样,你在众人面前就算清白了。” 17 亚伯拉罕祷告 神, 神就医好了亚比米勒和他的妻子,以及他的众婢女,使她们能生育。 18 因为耶和华为了亚伯拉罕妻子撒拉的缘故,曾经使亚比米勒家中所有的妇女,都不能生育。

Abrahamu ndi Mfumu Abimeleki

20 Abrahamu anachokako kumeneko napita ku Negevi ndipo anakakhala ku dziko la Gerari, limene lili pakati pa mzinda wa Kadesi ndi mzinda wa Suri. Anakhala ku Gerari kwa kanthawi, ndipo Abrahamu ankawawuza za Sara kuti, “Iyeyu ndi mlongo wanga.” Choncho Abimeleki, mfumu wa ku Gerari anamutenga Sara uja.

Koma usiku, Mulungu anafika kwa Abimeleki kutulo nati, “Ufatu iwe chifukwa cha mkazi amene watengayu popeza ndi wokwatiwa.”

Nthawi imeneyi nʼkuti Abimeleki asanamukhudze mkaziyo, kotero kuti anati, “Ambuye, kodi mudzawonongadi mtundu wolungama? Kodi Abrahamu sanandiwuze kuti iyeyu ndi mlongo wake? Ndiponso mkaziyu ankanena kuti Abrahamu ndi mlongo wake. Choncho ine pochita izi, ndinkachita moona mtima ndiponso mopanda chinyengo.”

Tsono kumaloto komweko Mulungu anati kwa iye, “Inde ndikudziwa kuti wachita izi moona mtima, ndipo Ine sindinafune kuti undichimwire. Nʼchifukwa chake sindinakulole kuti umukhudze. Tsopano kabwezere mkaziyo kwa mwamuna wake. Iyeyu ndi mneneri, ndipo adzakupempherera kuti ukhale ndi moyo. Koma ukapanda kukamupereka, udziwiretu kuti udzafa pamodzi ndi onse a pa banja pako.”

Mmamawa mwake Abimeleki anayitanitsa akuluakulu ake onse, ndipo atawafotokozera zimene zinachitika, iwo aja anachita mantha kwambiri. Kenaka Abimeleki anayitana Abrahamu ndipo anati, “Kodi wachita chiyani? Ndakulakwira chiyani kuti undibweretsere ine pamodzi ndi anthu anga chilango chachikulu chotere? Wandichitira zinthu zimene sizinayenera kuchitika.” 10 Ndipo Abrahamu anafunsa Abimeleki kuti, “Chifukwa chiyani wachita zimenezi?”

11 Abrahamu anayankha nati, “Ndinkaganiza kuti kuno kulibiretu munthu woopa Mulungu. Ndiye ndimati mwina adzandipha chifukwa cha mkazi wanga. 12 Komabe kunena zoona, iyeyu ndi mlongo wangadi, mwana wamkazi wa abambo anga ngakhale kuti si ife a mayi mmodzi. Tsono akhoza kukhala mkazi wanga. 13 Ndiye pamene Mulungu anati ndichoke ku nyumba ya abambo anga, ndinawuza mkazi wangayu kuti, ‘Kuti uwonetse kuti ndiwe mkazi wokoma mtima, uziwuza anthu kulikonse kumene tingapite kuti ndine mlongo wako.’ ”

14 Tsono Abimeleki anapereka nkhosa, ngʼombe ndi antchito aamuna ndi aakazi kwa Abrahamu. Ndipo anamubwezeranso Abrahamu Sara, mkazi wake. 15 Tsono Abimeleki anati kwa Abrahamu, “Dziko langa ndi limene ukulionali; ukhale paliponse pamene ufuna.”

16 Ndipo kwa Sara, iye anati, “Ndikumupatsa mlongo wakoyu makilogalamu khumi ndi awiri a siliva kutsimikiza kuti iwe ndi wosalakwa pamaso pa onse amene ali ndi iwe; ulibedi mlandu.”

17 Tsono Abrahamu anapemphera kwa Mulungu ndipo Mulunguyo anachiritsa Abimeleki, mkazi wake pamodzi ndi adzakazi ake kuti athenso kubereka ana. 18 Paja Yehova nʼkuti atatseka akazi onse a mʼbanja la Abimeleki kuti asabereke ana chifukwa cha Sara, mkazi wa Abrahamu.

20 And Abraham journeyed from thence toward the south country, and dwelled between Kadesh and Shur, and sojourned in Gerar.

And Abraham said of Sarah his wife, She is my sister: and Abimelech king of Gerar sent, and took Sarah.

But God came to Abimelech in a dream by night, and said to him, Behold, thou art but a dead man, for the woman which thou hast taken; for she is a man's wife.

But Abimelech had not come near her: and he said, Lord, wilt thou slay also a righteous nation?

Said he not unto me, She is my sister? and she, even she herself said, He is my brother: in the integrity of my heart and innocency of my hands have I done this.

And God said unto him in a dream, Yea, I know that thou didst this in the integrity of thy heart; for I also withheld thee from sinning against me: therefore suffered I thee not to touch her.

Now therefore restore the man his wife; for he is a prophet, and he shall pray for thee, and thou shalt live: and if thou restore her not, know thou that thou shalt surely die, thou, and all that are thine.

Therefore Abimelech rose early in the morning, and called all his servants, and told all these things in their ears: and the men were sore afraid.

Then Abimelech called Abraham, and said unto him, What hast thou done unto us? and what have I offended thee, that thou hast brought on me and on my kingdom a great sin? thou hast done deeds unto me that ought not to be done.

10 And Abimelech said unto Abraham, What sawest thou, that thou hast done this thing?

11 And Abraham said, Because I thought, Surely the fear of God is not in this place; and they will slay me for my wife's sake.

12 And yet indeed she is my sister; she is the daughter of my father, but not the daughter of my mother; and she became my wife.

13 And it came to pass, when God caused me to wander from my father's house, that I said unto her, This is thy kindness which thou shalt shew unto me; at every place whither we shall come, say of me, He is my brother.

14 And Abimelech took sheep, and oxen, and menservants, and womenservants, and gave them unto Abraham, and restored him Sarah his wife.

15 And Abimelech said, Behold, my land is before thee: dwell where it pleaseth thee.

16 And unto Sarah he said, Behold, I have given thy brother a thousand pieces of silver: behold, he is to thee a covering of the eyes, unto all that are with thee, and with all other: thus she was reproved.

17 So Abraham prayed unto God: and God healed Abimelech, and his wife, and his maidservants; and they bare children.

18 For the Lord had fast closed up all the wombs of the house of Abimelech, because of Sarah Abraham's wife.

Abraham and Abimelech

20 And Abraham journeyed from (A)there to the South, and dwelt between (B)Kadesh and Shur, and (C)stayed in Gerar. Now Abraham said of Sarah his wife, (D)“She is my sister.” And Abimelech king of Gerar sent and (E)took Sarah.

But (F)God came to Abimelech (G)in a dream by night, and said to him, (H)“Indeed you are a dead man because of the woman whom you have taken, for she is [a]a man’s wife.”

But Abimelech had not come near her; and he said, “Lord, (I)will You slay a righteous nation also? Did he not say to me, ‘She is my sister’? And she, even she herself said, ‘He is my brother.’ (J)In the [b]integrity of my heart and innocence of my hands I have done this.”

And God said to him in a dream, “Yes, I know that you did this in the integrity of your heart. For (K)I also withheld you from sinning (L)against Me; therefore I did not let you touch her. Now therefore, restore the man’s wife; (M)for he is a prophet, and he will pray for you and you shall live. But if you do not restore her, (N)know that you shall surely die, you (O)and all who are yours.”

So Abimelech rose early in the morning, called all his servants, and told all these things in their hearing; and the men were very much afraid. And Abimelech called Abraham and said to him, “What have you done to us? How have I [c]offended you, (P)that you have brought on me and on my kingdom a great sin? You have done deeds to me (Q)that ought not to be done.” 10 Then Abimelech said to Abraham, “What did you have in view, that you have done this thing?”

11 And Abraham said, “Because I thought, surely (R)the fear of God is not in this place; and (S)they will kill me on account of my wife. 12 But indeed (T)she is truly my sister. She is the daughter of my father, but not the daughter of my mother; and she became my wife. 13 And it came to pass, when (U)God caused me to wander from my father’s house, that I said to her, ‘This is your kindness that you should do for me: in every place, wherever we go, (V)say of me, “He is my brother.” ’ ”

14 Then Abimelech (W)took sheep, oxen, and male and female servants, and gave them to Abraham; and he restored Sarah his wife to him. 15 And Abimelech said, “See, (X)my land is before you; dwell where it pleases you.” 16 Then to Sarah he said, “Behold, I have given your brother a thousand pieces of silver; (Y)indeed this [d]vindicates you (Z)before all who are with you and before everybody.” Thus she was [e]rebuked.

17 So Abraham (AA)prayed to God; and God (AB)healed Abimelech, his wife, and his female servants. Then they bore children; 18 for the Lord (AC)had closed up all the wombs of the house of Abimelech because of Sarah, Abraham’s wife.

Footnotes

  1. Genesis 20:3 Lit. married to a husband
  2. Genesis 20:5 innocence
  3. Genesis 20:9 sinned against
  4. Genesis 20:16 Lit. is a covering of the eyes for you to all
  5. Genesis 20:16 Or justified