创世记 20
Chinese Contemporary Bible (Simplified)
亚伯拉罕与亚比米勒
20 亚伯拉罕从幔利迁往南地,住在加低斯和书珥之间。在基拉耳寄居期间, 2 他称妻子撒拉是自己的妹妹。基拉耳王亚比米勒派人带走了撒拉。
3 晚上,上帝在梦中对亚比米勒说:“你的死期到了,因为你带来的那个女人是别人的妻子。” 4 亚比米勒还没有亲近撒拉,因此他说:“主啊,难道你要毁灭一个无辜的国家吗? 5 那人亲口对我说这女人是他妹妹,她也说那人是她哥哥。我问心无愧,没有做错。” 6 上帝在梦中对他说:“我知道你问心无愧,所以我才阻止你,不让你亲近她,免得你得罪我。 7 现在你要把那人的妻子还给他,他是个先知,他会为你祷告,使你活命。要知道,如果你不这样做,你和你的人民都必死。”
8 亚比米勒清早起来召来他的臣仆,把这件事情告诉他们,他们听了都十分害怕。 9 亚比米勒召见亚伯拉罕,对他说:“你为什么要害我们?我什么地方得罪了你?你竟使我和我的人民陷入大罪!你不该这样做。” 10 又说:“你为什么这样做?” 11 亚伯拉罕回答说:“因为我想这里的人不敬畏上帝,他们必为了夺我妻子而杀我。 12 况且,她真是我的妹妹,与我同父异母,后来做了我的妻子。 13 上帝吩咐我离开家乡到外面漂泊的时候,我对她说,‘无论我们到哪里,你都要说我是你哥哥,这就是你对我的恩情。’”
14 于是,亚比米勒带来牛、羊和男女仆婢送给亚伯拉罕,并把他妻子撒拉还给他, 15 又对他说:“我的国土就在你面前,你想住在哪里都可以。” 16 亚比米勒对撒拉说:“我给你哥哥十一公斤银子,在你家人面前证明你是清白的,你没有做错什么。”
17 亚伯拉罕祈求上帝,上帝就治好了亚比米勒,也使他妻子和众婢女恢复了生育能力。 18 原来耶和华因为亚伯拉罕的妻子撒拉这件事,使亚比米勒宫中所有的妇女都不能生育。
Genesis 20
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Abrahamu ndi Mfumu Abimeleki
20 Abrahamu anachokako kumeneko napita ku Negevi ndipo anakakhala ku dziko la Gerari, limene lili pakati pa mzinda wa Kadesi ndi mzinda wa Suri. Anakhala ku Gerari kwa kanthawi, 2 ndipo Abrahamu ankawawuza za Sara kuti, “Iyeyu ndi mlongo wanga.” Choncho Abimeleki, mfumu wa ku Gerari anamutenga Sara uja.
3 Koma usiku, Mulungu anafika kwa Abimeleki kutulo nati, “Ufatu iwe chifukwa cha mkazi amene watengayu popeza ndi wokwatiwa.”
4 Nthawi imeneyi nʼkuti Abimeleki asanamukhudze mkaziyo, kotero kuti anati, “Ambuye, kodi mudzawonongadi mtundu wolungama? 5 Kodi Abrahamu sanandiwuze kuti iyeyu ndi mlongo wake? Ndiponso mkaziyu ankanena kuti Abrahamu ndi mlongo wake. Choncho ine pochita izi, ndinkachita moona mtima ndiponso mopanda chinyengo.”
6 Tsono kumaloto komweko Mulungu anati kwa iye, “Inde ndikudziwa kuti wachita izi moona mtima, ndipo Ine sindinafune kuti undichimwire. Nʼchifukwa chake sindinakulole kuti umukhudze. 7 Tsopano kabwezere mkaziyo kwa mwamuna wake. Iyeyu ndi mneneri, ndipo adzakupempherera kuti ukhale ndi moyo. Koma ukapanda kukamupereka, udziwiretu kuti udzafa pamodzi ndi onse a pa banja pako.”
8 Mmamawa mwake Abimeleki anayitanitsa akuluakulu ake onse, ndipo atawafotokozera zimene zinachitika, iwo aja anachita mantha kwambiri. 9 Kenaka Abimeleki anayitana Abrahamu ndipo anati, “Kodi wachita chiyani? Ndakulakwira chiyani kuti undibweretsere ine pamodzi ndi anthu anga chilango chachikulu chotere? Wandichitira zinthu zimene sizinayenera kuchitika.” 10 Ndipo Abrahamu anafunsa Abimeleki kuti, “Chifukwa chiyani wachita zimenezi?”
11 Abrahamu anayankha nati, “Ndinkaganiza kuti kuno kulibiretu munthu woopa Mulungu. Ndiye ndimati mwina adzandipha chifukwa cha mkazi wanga. 12 Komabe kunena zoona, iyeyu ndi mlongo wangadi, mwana wamkazi wa abambo anga ngakhale kuti si ife a mayi mmodzi. Tsono akhoza kukhala mkazi wanga. 13 Ndiye pamene Mulungu anati ndichoke ku nyumba ya abambo anga, ndinawuza mkazi wangayu kuti, ‘Kuti uwonetse kuti ndiwe mkazi wokoma mtima, uziwuza anthu kulikonse kumene tingapite kuti ndine mlongo wako.’ ”
14 Tsono Abimeleki anapereka nkhosa, ngʼombe ndi antchito aamuna ndi aakazi kwa Abrahamu. Ndipo anamubwezeranso Abrahamu Sara, mkazi wake. 15 Tsono Abimeleki anati kwa Abrahamu, “Dziko langa ndi limene ukulionali; ukhale paliponse pamene ufuna.”
16 Ndipo kwa Sara, iye anati, “Ndikumupatsa mlongo wakoyu makilogalamu khumi ndi awiri a siliva kutsimikiza kuti iwe ndi wosalakwa pamaso pa onse amene ali ndi iwe; ulibedi mlandu.”
17 Tsono Abrahamu anapemphera kwa Mulungu ndipo Mulunguyo anachiritsa Abimeleki, mkazi wake pamodzi ndi adzakazi ake kuti athenso kubereka ana. 18 Paja Yehova nʼkuti atatseka akazi onse a mʼbanja la Abimeleki kuti asabereke ana chifukwa cha Sara, mkazi wa Abrahamu.
创世记 20
Chinese Union Version Modern Punctuation (Simplified)
20 亚伯拉罕从那里向南地迁去,寄居在加低斯和书珥中间的基拉耳。 2 亚伯拉罕称他的妻撒拉为妹子,基拉耳王亚比米勒差人把撒拉取了去。 3 但夜间神来在梦中对亚比米勒说:“你是个死人哪!因为你取了那女人来,她原是别人的妻子。” 4 亚比米勒却还没有亲近撒拉,他说:“主啊,连有义的国,你也要毁灭吗? 5 那人岂不是自己对我说‘她是我的妹子’吗?就是女人也自己说‘他是我的哥哥’。我做这事是心正手洁的。” 6 神在梦中对他说:“我知道你做这事是心中正直,我也拦阻了你,免得你得罪我。所以我不容你沾着她。 7 现在你把这人的妻子归还他,因为他是先知,他要为你祷告,使你存活。你若不归还他,你当知道,你和你所有的人都必要死。”
亚比米勒责亚伯拉罕
8 亚比米勒清早起来,召了众臣仆来,将这些事都说给他们听,他们都甚惧怕。 9 亚比米勒召了亚伯拉罕来,对他说:“你怎么向我这样行呢?我在什么事上得罪了你,你竟使我和我国里的人陷在大罪里?你向我行不当行的事了。” 10 亚比米勒又对亚伯拉罕说:“你见了什么才做这事呢?” 11 亚伯拉罕说:“我以为这地方的人总不惧怕神,必为我妻子的缘故杀我。 12 况且她也实在是我的妹子,她与我是同父异母,后来做了我的妻子。 13 当神叫我离开父家,漂流在外的时候,我对她说:‘我们无论走到什么地方,你可以对人说“他是我的哥哥”,这就是你待我的恩典了。’” 14 亚比米勒把牛、羊、仆婢赐给亚伯拉罕,又把他的妻子撒拉归还他。 15 亚比米勒又说:“看哪,我的地都在你面前,你可以随意居住。” 16 又对撒拉说:“我给你哥哥一千银子,作为你在合家人面前遮羞[a]的,你就在众人面前没有不是了。” 17 亚伯拉罕祷告神,神就医好了亚比米勒和他的妻子,并他的众女仆,她们便能生育。 18 因耶和华为亚伯拉罕的妻子撒拉的缘故,已经使亚比米勒家中的妇人不能生育。
Footnotes
- 创世记 20:16 “羞”原文作“眼”。
Genesis 20
New International Version
Abraham and Abimelek(A)
20 Now Abraham moved on from there(B) into the region of the Negev(C) and lived between Kadesh(D) and Shur.(E) For a while(F) he stayed in Gerar,(G) 2 and there Abraham said of his wife Sarah, “She is my sister.(H)” Then Abimelek(I) king of Gerar sent for Sarah and took her.(J)
3 But God came to Abimelek(K) in a dream(L) one night and said to him, “You are as good as dead(M) because of the woman you have taken; she is a married woman.”(N)
4 Now Abimelek had not gone near her, so he said, “Lord, will you destroy an innocent nation?(O) 5 Did he not say to me, ‘She is my sister,(P)’ and didn’t she also say, ‘He is my brother’? I have done this with a clear conscience(Q) and clean hands.(R)”
6 Then God said to him in the dream, “Yes, I know you did this with a clear conscience, and so I have kept(S) you from sinning against me.(T) That is why I did not let you touch her. 7 Now return the man’s wife, for he is a prophet,(U) and he will pray for you(V) and you will live. But if you do not return her, you may be sure that you and all who belong to you will die.”(W)
8 Early the next morning Abimelek summoned all his officials, and when he told them all that had happened, they were very much afraid. 9 Then Abimelek called Abraham in and said, “What have you done to us? How have I wronged you that you have brought such great guilt upon me and my kingdom? You have done things to me that should never be done.(X)” 10 And Abimelek asked Abraham, “What was your reason for doing this?”
11 Abraham replied, “I said to myself, ‘There is surely no fear of God(Y) in this place, and they will kill me because of my wife.’(Z) 12 Besides, she really is my sister,(AA) the daughter of my father though not of my mother; and she became my wife. 13 And when God had me wander(AB) from my father’s household,(AC) I said to her, ‘This is how you can show your love to me: Everywhere we go, say of me, “He is my brother.”’”
14 Then Abimelek(AD) brought sheep and cattle and male and female slaves and gave them to Abraham,(AE) and he returned Sarah his wife to him. 15 And Abimelek said, “My land is before you; live wherever you like.”(AF)
16 To Sarah he said, “I am giving your brother a thousand shekels[a] of silver. This is to cover the offense against you before all who are with you; you are completely vindicated.”
17 Then Abraham prayed to God,(AG) and God healed Abimelek, his wife and his female slaves so they could have children again, 18 for the Lord had kept all the women in Abimelek’s household from conceiving because of Abraham’s wife Sarah.(AH)
Footnotes
- Genesis 20:16 That is, about 25 pounds or about 12 kilograms
Chinese Contemporary Bible Copyright © 1979, 2005, 2007, 2011 by Biblica® Used by permission. All rights reserved worldwide.
The Word of God in Contemporary Chichewa Copyright © 2002, 2016 by Biblica, Inc.® Used by permission of Biblica, Inc.® All rights reserved worldwide. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Mwini © 2002, 2016 ndi Biblica, Inc.® Kugwiritsa ntchito mwachilolezo. Umwini ndi otetezedwa pa dziko lonse.
Copyright © 2011 by Global Bible Initiative
Holy Bible, New International Version®, NIV® Copyright ©1973, 1978, 1984, 2011 by Biblica, Inc.® Used by permission. All rights reserved worldwide.
NIV Reverse Interlinear Bible: English to Hebrew and English to Greek. Copyright © 2019 by Zondervan.
