Add parallel Print Page Options

擊磐出水(A)

17 以色列全體會眾都照著耶和華的吩咐,一站一站,從汛的曠野起程,在利非訂安營。在那裡人民沒有水喝。 因此人民與摩西爭吵,說:“給我們水喝吧。”摩西對他們說:“你們為甚麼與我爭吵呢?你們為甚麼試探耶和華呢?” 人民在那裡渴望得水喝,就向摩西發怨言,說:“你為甚麼把我們從埃及領上來,使我們和我們的兒女,以及我們的牲畜都渴死呢?” 摩西向耶和華呼求,說:“我要怎樣對待這人民呢?他們幾乎要用石頭打死我了。” 耶和華回答摩西:“你要到人民的面前,要帶著以色列的幾個長老和你一起,手裡要拿著你先前擊打河水的杖。 看哪,我必在何烈山那裡的磐石上站在你面前;你要擊打磐石,就必有水從磐石流出來,使人民可以喝。”摩西就在以色列的長老眼前這樣行了。 他給那地方起名叫瑪撒,又叫米利巴,因為以色列人在那裡爭吵,又因為他們試探耶和華,說:“耶和華是不是在我們中間呢?”

與亞瑪力人作戰

那時亞瑪力人來了,在利非訂和以色列人爭戰。 摩西對約書亞說:“你要為我們選出人來,出去和亞瑪力人爭戰;明天我要站在山頂上,手裡拿著 神的杖。” 10 於是,約書亞照著摩西吩咐他的行了,去和亞瑪力人爭戰;摩西、亞倫和戶珥都上了山頂。 11 摩西舉起手來的時候,以色列人就得勝;摩西把手放下來的時候,亞瑪力人就得勝。 12 可是摩西的兩手疲乏了,他們就搬塊石頭來,放在摩西下面,他就坐在上面;亞倫和戶珥,一邊一個,扶著摩西的兩手;這樣,他的兩手就穩住,直到日落的時候。 13 約書亞用刀打敗了亞瑪力王和他的人民。

14 耶和華對摩西說:“我要把亞瑪力的名號從天下完全抹掉;你要把話寫在書上作記念,也要告訴約書亞。” 15 摩西築了一座祭壇,給它起名叫“耶和華尼西”。 16 摩西又說:“向耶和華的旌旗舉手,耶和華必世世代代和亞瑪力人爭戰。”

Madzi Otuluka Mʼthanthwe

17 Gulu lonse la Aisraeli linachoka ku chipululu cha Sini, ndi kumayenda malo ndi malo monga momwe anawalamulira Yehova. Iwo anamanga misasa yawo ku Refidimu koma kunalibe madzi woti anthu onse ndi kumwa. Kotero iwo anakangana ndi Mose nati, “Tipatse madzi akumwa.”

Mose anayankha kuti, “Chifukwa chiyani mukukangana ndi ine? Chifukwa chiyani mukumuyesa Yehova?”

Koma anthu anali ndi ludzu pamenepo ndipo anangʼungʼudza pamaso pa Mose namufunsa kuti, “Kodi nʼchifukwa chiyani unatitulutsa mʼdziko la Igupto kuti ife, ana athu pamodzi ndi ziweto zathu tife ndi ludzu?”

Ndipo Mose anapemphera kwa Yehova, “Kodi ndichite chiyani ndi anthu awa? Iwo atsala pangʼono kundigenda ndi miyala.”

Yehova anati kwa Mose, “Pita patsogolo pa anthuwo. Tenga ndodo imene unamenyera nyanja ya Nailo pamodzi ndi akuluakulu ena a Israeli ndi kunyamuka. Ine ndidzayima patsogolo pako pafupi ndi thanthwe la ku Horebu. Ukamenye thanthwelo, madzi adzatuluka kuti anthu amwe.” Motero Mose anachita zimenezi pamaso pa akuluakulu a Israeli. Ndipo iye anatcha malowo Masa ndi Meriba chifukwa Aisraeli anakangana ndi kuyesa Yehova ponena kuti, “Kodi pakati pathu pali Yehova kapena palibe?”

Aisraeli Agonjetsa Aamaleki

Amaleki anabwera ku Refidimu kudzamenyana ndi Aisraeli. Mose anati kwa Yoswa, “Sankha amuna amphamvu ndipo upite ukamenyane ndi Amaleki. Mawa ndidzayima pamwamba pa phiri nditagwira ndodo ya Mulungu.”

10 Ndipo Yoswa anachitadi monga Mose anamulamulira. Iye anapita kukamenyana ndi Aamaleki ndipo Mose, Aaroni ndi Huri anapita pamwamba pa phiri. 11 Mose ankati akakweza manja ake, Aisraeli amapambana, koma akatsitsa manja akewo Amaleki amapambana. 12 Manja a Mose atatopa, Aaroni ndi Huri anatenga mwala ndi kuyika pansi ndipo Mose anakhalapo. Aaroni ndi Huri anagwirizitsa manja a Mose wina mbali ina winanso mbali ina. Choncho manja a Mose analimba mpaka kulowa kwa dzuwa. 13 Kotero Yoswa anagonjetsa asilikali ankhondo a Amaleki ndi lupanga.

14 Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Lemba izi mʼbuku kuti zidzakumbukirike ndipo uwonetsetse kuti Yoswa amve zimenezi, chifukwa Ine ndidzafafaniziratu Amaleki pa dziko lapansi, kotero kuti palibe amene adzawakumbukire.”

15 Mose anamanga guwa lansembe ndipo analitcha Yehova Chipambano Changa (Yehova Nisi). 16 Ndipo anati, “Kwezani mbendera ya Yehova. Yehova adzachitabe nkhondo ndi mibado yonse ya Aamaleki.”

17 And all the congregation of the children of Israel journeyed from the wilderness of Sin, after their journeys, according to the commandment of the Lord, and pitched in Rephidim: and there was no water for the people to drink.

Wherefore the people did chide with Moses, and said, Give us water that we may drink. And Moses said unto them, Why chide ye with me? wherefore do ye tempt the Lord?

And the people thirsted there for water; and the people murmured against Moses, and said, Wherefore is this that thou hast brought us up out of Egypt, to kill us and our children and our cattle with thirst?

And Moses cried unto the Lord, saying, What shall I do unto this people? they be almost ready to stone me.

And the Lord said unto Moses, Go on before the people, and take with thee of the elders of Israel; and thy rod, wherewith thou smotest the river, take in thine hand, and go.

Behold, I will stand before thee there upon the rock in Horeb; and thou shalt smite the rock, and there shall come water out of it, that the people may drink. And Moses did so in the sight of the elders of Israel.

And he called the name of the place Massah, and Meribah, because of the chiding of the children of Israel, and because they tempted the Lord, saying, Is the Lord among us, or not?

Then came Amalek, and fought with Israel in Rephidim.

And Moses said unto Joshua, Choose us out men, and go out, fight with Amalek: to morrow I will stand on the top of the hill with the rod of God in mine hand.

10 So Joshua did as Moses had said to him, and fought with Amalek: and Moses, Aaron, and Hur went up to the top of the hill.

11 And it came to pass, when Moses held up his hand, that Israel prevailed: and when he let down his hand, Amalek prevailed.

12 But Moses hands were heavy; and they took a stone, and put it under him, and he sat thereon; and Aaron and Hur stayed up his hands, the one on the one side, and the other on the other side; and his hands were steady until the going down of the sun.

13 And Joshua discomfited Amalek and his people with the edge of the sword.

14 And the Lord said unto Moses, Write this for a memorial in a book, and rehearse it in the ears of Joshua: for I will utterly put out the remembrance of Amalek from under heaven.

15 And Moses built an altar, and called the name of it Jehovahnissi:

16 For he said, Because the Lord hath sworn that the Lord will have war with Amalek from generation to generation.

Water From the Rock

17 The whole Israelite community set out from the Desert of Sin,(A) traveling from place to place as the Lord commanded. They camped at Rephidim,(B) but there was no water(C) for the people to drink. So they quarreled with Moses and said, “Give us water(D) to drink.”(E)

Moses replied, “Why do you quarrel with me? Why do you put the Lord to the test?”(F)

But the people were thirsty(G) for water there, and they grumbled(H) against Moses. They said, “Why did you bring us up out of Egypt to make us and our children and livestock die(I) of thirst?”

Then Moses cried out to the Lord, “What am I to do with these people? They are almost ready to stone(J) me.”

The Lord answered Moses, “Go out in front of the people. Take with you some of the elders of Israel and take in your hand the staff(K) with which you struck the Nile,(L) and go. I will stand there before you by the rock at Horeb.(M) Strike(N) the rock, and water(O) will come out of it for the people to drink.” So Moses did this in the sight of the elders of Israel. And he called the place Massah[a](P) and Meribah[b](Q) because the Israelites quarreled and because they tested the Lord saying, “Is the Lord among us or not?”

The Amalekites Defeated

The Amalekites(R) came and attacked the Israelites at Rephidim.(S) Moses said to Joshua,(T) “Choose some of our men and go out to fight the Amalekites. Tomorrow I will stand on top of the hill with the staff(U) of God in my hands.”

10 So Joshua fought the Amalekites as Moses had ordered, and Moses, Aaron and Hur(V) went to the top of the hill. 11 As long as Moses held up his hands, the Israelites were winning,(W) but whenever he lowered his hands, the Amalekites were winning. 12 When Moses’ hands grew tired, they took a stone and put it under him and he sat on it. Aaron and Hur held his hands up—one on one side, one on the other—so that his hands remained steady till sunset.(X) 13 So Joshua overcame the Amalekite(Y) army with the sword.

14 Then the Lord said to Moses, “Write(Z) this on a scroll as something to be remembered and make sure that Joshua hears it, because I will completely blot out(AA) the name of Amalek(AB) from under heaven.”

15 Moses built an altar(AC) and called(AD) it The Lord is my Banner. 16 He said, “Because hands were lifted up against[c] the throne of the Lord,[d] the Lord will be at war against the Amalekites(AE) from generation to generation.”(AF)

Footnotes

  1. Exodus 17:7 Massah means testing.
  2. Exodus 17:7 Meribah means quarreling.
  3. Exodus 17:16 Or to
  4. Exodus 17:16 The meaning of the Hebrew for this clause is uncertain.