Add parallel Print Page Options

勸人民誠心歸向 神

“來吧!讓我們回轉歸向耶和華;

因為,他雖然撕裂了我們,但必定醫治我們;

他雖然擊傷了我們,卻必替我們裹傷。

兩天以後,他要使我們復原;

第三天,他使我們起來,

我們就可以活在他的面前。

讓我們認識,竭力追求認識耶和華。

他必定出現,像晨光一樣,

他必臨到我們,如雨水一般,

又像滋潤大地的春雨。

指摘人民虛偽的行為

“以法蓮啊!我要怎樣待你呢?

猶大啊,我要怎樣待你呢?

你們的愛心像早晨的雲霧;

又像瞬即消逝的朝露。

因此,我藉眾先知砍碎他們,

用我口中的話殺戮他們;

我的審判必如光一般發出。

我喜愛憐恤,不喜愛祭祀;

我喜愛人認識 神的知識,勝過人獻的燔祭。

可是他們卻在亞當城背約,

在那裡向我行詭詐。

基列是作孽之人的城,

他們的腳蹤染滿了血漬。

在往示劍的路上,祭司結黨殺害人,

就像埋伏路旁的強盜;

他們行了邪惡的事。

10 在以色列家!我看見了可怕的事;

那裡有以法蓮的淫行,以色列被玷污了。

11 猶大啊!我使我的子民歸回的時候,

必有為你定下的一個收割時期。”

Kusalapa kwa Israeli

“Bwerani, tiyeni tibwerere kwa Yehova.
Iye watikhadzula,
    koma adzatichiritsa.
Iye wativulaza,
    koma adzamanga mabala athu.
Pakapita masiku awiri adzatitsitsimutsa;
    pa tsiku lachitatu Iye adzatiukitsa
    kuti tikhale ndi moyo pamaso pake.
Tiyeni timudziwe Yehova,
    tiyeni tilimbike kumudziwa Iye.
Adzabwera kwa ife mosakayikira konse
    ngati kutuluka kwa dzuwa;
adzabwera kwa ife ngati mvula ya mʼchilimwe,
    ngati mvula ya nthawi yamphukira imene imakhathamiritsa nthaka.”

Iwe Efereimu, kodi ndichite nawe chiyani?
    Kodi ndichite nawe chiyani, iwe Yuda?
Chikondi chanu chili ngati nkhungu yammawa,
    ngati mame a mmamawa amene amakamuka msanga.
Choncho ndakuwazani ngati nkhuni kudzera mwa aneneri anga,
    ndakuphani ndi mawu a pakamwa panga;
    chigamulo changa chinangʼanima ngati mphenzi pa inu.
Pakuti Ine ndimafuna chifundo osati nsembe,
    ndi kudziwa Mulungu kulekana ndi nsembe zopsereza.
Monga Adamu, anthuwa aphwanya pangano langa,
    iwo sanakhulupirike kwa Ine.
Giliyadi ndi mzinda wa anthu ochita zoyipa,
    okhala ndi zizindikiro za kuphana.
Monga momwe mbala zimadikirira anthu,
    magulu a ansembe amachitanso motero;
iwo amapha anthu pa njira yopita ku Sekemu,
    kupalamula milandu yochititsa manyazi.
10 Ndaona chinthu choopsa kwambiri
    mʼnyumba ya Israeli.
Kumeneko Efereimu akuchita zachiwerewere,
    ndipo Israeli wadzidetsa.

11 “Kunenanso za iwe Yuda,
    udzakolola chilango.

“Pamene ndiwabwezere anthu anga zinthu zabwino.”

Israel Unrepentant

“Come, let us return(A) to the Lord.
He has torn us to pieces(B)
    but he will heal us;(C)
he has injured us
    but he will bind up our wounds.(D)
After two days he will revive us;(E)
    on the third day(F) he will restore(G) us,
    that we may live in his presence.
Let us acknowledge the Lord;
    let us press on to acknowledge him.
As surely as the sun rises,
    he will appear;
he will come to us like the winter rains,(H)
    like the spring rains that water the earth.(I)

“What can I do with you, Ephraim?(J)
    What can I do with you, Judah?
Your love is like the morning mist,
    like the early dew that disappears.(K)
Therefore I cut you in pieces with my prophets,
    I killed you with the words of my mouth(L)
    then my judgments go forth like the sun.[a](M)
For I desire mercy, not sacrifice,(N)
    and acknowledgment(O) of God rather than burnt offerings.(P)
As at Adam,[b] they have broken the covenant;(Q)
    they were unfaithful(R) to me there.
Gilead is a city of evildoers,(S)
    stained with footprints of blood.
As marauders lie in ambush for a victim,(T)
    so do bands of priests;
they murder(U) on the road to Shechem,
    carrying out their wicked schemes.(V)
10 I have seen a horrible(W) thing in Israel:
    There Ephraim is given to prostitution,
    Israel is defiled.(X)

11 “Also for you, Judah,
    a harvest(Y) is appointed.

“Whenever I would restore the fortunes(Z) of my people,

Footnotes

  1. Hosea 6:5 The meaning of the Hebrew for this line is uncertain.
  2. Hosea 6:7 Or Like Adam; or Like human beings