Add parallel Print Page Options

古列王下旨建造聖殿

波斯王古列元年,耶和華為要應驗他藉耶利米的口所說的話,就激動波斯王古列的心靈,使他通令全國,傳達文告說: “波斯王古列這樣說:‘耶和華天上的 神已經把地上萬國賜給我。他指派我在猶大的耶路撒冷為他建造殿宇。 你們中間凡是他的子民,願 神與他同在的,都可以上猶大的耶路撒冷去,建造耶和華以色列的 神的殿,他是在耶路撒冷受敬拜的 神。 所有餘民,無論寄居在甚麼地方,那地方的人都要用金、銀、財物、牲畜幫助他,也要為在耶路撒冷 神的殿獻上甘心的禮物。’”

準備回歸

於是,猶大和便雅憫的族長、祭司、利未人和所有被 神激動了心靈的人,都起來要上去,重建在耶路撒冷耶和華的殿。 他們四圍的人都用銀器、金子、財物、牲畜和珍貴的禮物協助他們,另外還有各種甘心奉獻的禮物。 古列王把耶和華殿裡的器皿拿出來,就是從前尼布甲尼撒從耶路撒冷拿來放在自己的神廟裡的。 波斯王古列命令司庫官米提利達把這些器皿拿出來,按數交給猶大的領袖設巴薩。 器皿的數目是:金盤三十個、銀盤一千個、刀二十九把、 10 金碗三十個、次等銀碗四百一十個(“次等銀碗四百一十個”:本句意義難確定,或譯:“銀碗二千四百一十個”),其他的器皿一千件。 11 全部的金銀器皿共有五千四百件。被擄的人從巴比倫上耶路撒冷去的時候,設巴薩把這一切器皿都帶上去。

'以 斯 拉 記 1 ' not found for the version: Chinese New Testament: Easy-to-Read Version.

Koresi Athandiza Ayuda Kubwerera Kwawo

Mʼchaka choyamba cha ufumu wa Koresi mfumu ya Perisiya, pofuna kukwaniritsa zimene anayankhula kudzera mwa Yeremiya, Yehova anayika maganizo mu mtima mwa Koresi mfumu ya Perisiya kuti alengeze mʼdziko lake lonse ndi mawu apakamwa ngakhalenso ochita kulemba.

Iye anati, “Koresi mfumu ya Perisiya ikunena kuti,

“ ‘Yehova, Mulungu wakumwamba wandipatsa maufumu onse a dziko lapansi, ndipo wandipatsa udindo woti ndimumangire Nyumba ku Yerusalemu mʼdziko la Yuda. Aliyense wa inu amene ali wa Yehova, Mulungu wakeyo akhale naye. Tsono aliyense wa inu apite ku Yerusalemu, mʼdziko la Yuda kuti akamange Nyumba ya Yehova, Mulungu wa Israeli. Iyeyu ndi Mulungu amene ali mu Yerusalemu. Ndipo kumalo kulikonse kumene otsalawo akukhala, athandizidwe ndi eni dzikolo powapatsa siliva, golide, katundu ndi ziweto ndi zopereka za ufulu zoti akapereke ku Nyumba ya Yehova imene ili ku Yerusalemu.’ ”

Choncho atsogoleri a mabanja afuko la Yuda ndi la Benjamini komanso ansembe ndi Alevi, aliyense amene Mulungu anawutsa mtima wake, anayamba kukonzeka kupita kukamanga Nyumba ya Yehova imene ili ku Yerusalemu. Onse oyandikana nawo anawathandiza powapatsa ziwiya za siliva ndi zagolide, kuphatikizaponso katundu ndi ziweto, ndiponso mphatso zamtengo wapatali, kuwonjezera pa zopereka zaufulu zija. Nayenso mfumu Koresi anatulutsa ziwiya za mʼNyumba ya Yehova zimene Nebukadinezara anazitenga kuzichotsa ku Yerusalemu ndi kuziyika mʼnyumba ya milungu yake. Koresi, mfumu ya ku Perisiya inatulutsa ziwiyazi ndi kuzipereka kwa Miteridati, msungichuma amene anaziwerenga pamaso pa Sesibazara nduna yayikulu ya dziko la Yuda.

Chiwerengerochi chinali motere:

Mabeseni agolide30
mabeseni asiliva1,000
a zopereka29
10 timiphika tagolide230
timiphika tasiliva410
ziwiya zina1,000.

11 Ziwiya zonse zagolide ndi siliva pamodzi zinalipo 5,400. Zonsezi ndi zimene Sezi-Bazara anabwera nazo pamene otengedwa ukapolo aja ankabwerera ku Yerusalemu kuchokera ku Babuloni.

Cyrus Helps the Exiles to Return(A)

In the first year of Cyrus king of Persia, in order to fulfill the word of the Lord spoken by Jeremiah,(B) the Lord moved the heart(C) of Cyrus king of Persia to make a proclamation throughout his realm and also to put it in writing:

“This is what Cyrus king of Persia says:

“‘The Lord, the God of heaven, has given me all the kingdoms of the earth and he has appointed(D) me to build(E) a temple for him at Jerusalem in Judah. Any of his people among you may go up to Jerusalem in Judah and build the temple of the Lord, the God of Israel, the God who is in Jerusalem, and may their God be with them. And in any locality where survivors(F) may now be living, the people are to provide them with silver and gold,(G) with goods and livestock, and with freewill offerings(H) for the temple of God(I) in Jerusalem.’”(J)

Then the family heads of Judah and Benjamin,(K) and the priests and Levites—everyone whose heart God had moved(L)—prepared to go up and build the house(M) of the Lord in Jerusalem. All their neighbors assisted them with articles of silver and gold,(N) with goods and livestock, and with valuable gifts, in addition to all the freewill offerings.

Moreover, King Cyrus brought out the articles belonging to the temple of the Lord, which Nebuchadnezzar had carried away from Jerusalem and had placed in the temple of his god.[a](O) Cyrus king of Persia had them brought by Mithredath the treasurer, who counted them out to Sheshbazzar(P) the prince of Judah.

This was the inventory:

gold dishes30
silver dishes1,000
silver pans[b]29
10 gold bowls30
matching silver bowls410
other articles1,000

11 In all, there were 5,400 articles of gold and of silver. Sheshbazzar brought all these along with the exiles when they came up from Babylon to Jerusalem.

Footnotes

  1. Ezra 1:7 Or gods
  2. Ezra 1:9 The meaning of the Hebrew for this word is uncertain.